Тёмный

KULIRA KWA A MALAWI - MUZAMULIRA BWANJI CHILIMA? 

Nkhalango Multimedia
Подписаться 18 тыс.
Просмотров 27 тыс.
50% 1

KULIRA KWA A MALAWI
MUZAMULIRA BWANJI DR. SAULOS CHILIMA?

Развлечения

Опубликовано:

 

14 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 52   
@patrickkusailemp3769
@patrickkusailemp3769 Месяц назад
Kungotchula mawu okhao oti malemu,,ndagwesa misonzi 😢😢😢R.I .P
@StellaCharmer
@StellaCharmer 12 часов назад
Vengeance belongs to the Lord 🙏🙏
@Shannie-uw4wm5fn8k
@Shannie-uw4wm5fn8k Месяц назад
Ndipo ineyo mmmm nayenda wapansi kukafika ku city center koz of this man nditsiku losaiwalika pamoyo wanga😊sleep well mr king man we shall forever remember you
@isaacbwanali4699
@isaacbwanali4699 Месяц назад
Ine aChilima ndidzawakumbikila chifukwa chakudzipereka kwao potumikila dziko- komanso potumikira Yehova pamoyo wao. Mzimu wao ndi ena onse omwe adatayika, pangozi iyi yandege iwuse mumtendere waYesu ❤🎉
@user-bq5eu7xb8h
@user-bq5eu7xb8h Месяц назад
Anali munthu okonda kupephere koma anthu❤❤
@user-ql1fy2rc4t
@user-ql1fy2rc4t Месяц назад
Chitsime chija chinali chakuya now ic mmene madzi mulibemo chilima King of national unity
@ernestphiri5507
@ernestphiri5507 Месяц назад
Its a great loss to the nation he was a great man no wonder he was a threat to the leaders of Malawi RIP beloved leader
@dysonfysonchifundo2284
@dysonfysonchifundo2284 Месяц назад
Tidzakumbukila potipangitsa kukhulupilila Munthu olakwika nkango uli pa mpando, koma mzimu wawo uwuse mu ntendele, kungodandaula Moyo wake wapita ngati mwanapiye eish
@user-ln4de7ke4j
@user-ln4de7ke4j Месяц назад
Chilima was a good man than the one who is in power
@JohnMbola-yp7fr
@JohnMbola-yp7fr Месяц назад
We'll rimaid Mr chilima for everything
@samuelmanda6588
@samuelmanda6588 Месяц назад
Ndidzamukumbukira chifukwa cholimba mtima kuti dziko lino ndila wina aliyense, tikhale ndi chiyembekezo kuti zinthu zisintha ndipo tsogolo lathu ndi lowala tikakhala ndi masomphenya. Kudzichepetsa kunalu mwa akulu aja mmmmmmm ayi enafe titengeteko phunziro. Experience yawo pogwira ntchito ndi ma private sector he had results oriented mindset.
@DennmichSimb
@DennmichSimb Месяц назад
Mr Chilima was Genius man.The youth of Africa has lost the great leader.He had good visions for the country of Malawi.
@glorynkhata1185
@glorynkhata1185 Месяц назад
Kungot wamwarira imfa yosakhala bwino koma kudziko ayi amaba kwambili chitukuko amapanga ku family kwake ndi ku ma party ndi amene amamudziwa za ubwino wake ine kulibe kungot mariro sitimasekerera RIP TO ALL CRASHED IN THAT BAD ACCIDENT
@GoodsonLindani-gf8pn
@GoodsonLindani-gf8pn Месяц назад
Nkhani yosakhala bwino ndiyamoyo wachokawo,koma pa nkhani yachitukuko sanachite chilichose mmalawi muno . RIP SKC.
@user-xg2ks9nw5q
@user-xg2ks9nw5q Месяц назад
Palibe ku malawi angafane ndi chilima
@DianaChimseu
@DianaChimseu Месяц назад
😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢
@SarahMusama-eu7wt
@SarahMusama-eu7wt Месяц назад
Taluza anthu anzeru awili saulosi and bingu
@SarahMusama-eu7wt
@SarahMusama-eu7wt Месяц назад
Ndimaonamo future bingu mwa saulosi
@LindaKapito
@LindaKapito Месяц назад
Mmmh kulila ndikulila ine ndikulila chifukwa chot nd moyo wachokawo,zinazo akudziwa mulungu koma rest in peace
@dinganinedsontchongwe610
@dinganinedsontchongwe610 Месяц назад
Saulosi Chilima sitizamuiwala anali munthu amene anabwadwa munthu was mwayi munthu wokondweka country wide munthu wolimba mtima simple man no one like him
@RuthMazengera-yx8oh
@RuthMazengera-yx8oh Месяц назад
Ndizamukumbukila anali muthu olimba mtima wachikondi odekha mwa chilima munali chiyembekezo chaamalawife 😢😢
@LeendaDeborah2005
@LeendaDeborah2005 Месяц назад
Kwa ine he looked so brave nthawi ya campaign but I don’t know what happened to him when he got in power. Adangoyamba kukhala zii all of the sudden. I may have never liked him that much once he got in power koma ineyo ndikudana kwambiri ndi mtundu wa imfa yomwe yamutenga. Wafa imfa yosayembekezeleka ndipo yowawilatu. Ambuye mukatamandike
@stevielee5404
@stevielee5404 Месяц назад
Ause mumtendele adatisinthitsa kaganizidwe
@DavieMakwecha
@DavieMakwecha Месяц назад
Ndidzawakumbukira chifukwa sanadwale ena apanga naye njiru ndi nzeru zomwe anali nazo osati zambuli zili ku mcp ko akuuzeni tanthauzo ya democracy mchiwewa sizophana ngati nthawi ya kamuzu ayi sithani a mco ino ndi nthawi ina zosiilana za dziko izi
@usumanidaudi
@usumanidaudi Месяц назад
Chirima anari munthu wabwino kwambiri ine ndikudandawura kwambiri 😢😢
@mosesphiri8563
@mosesphiri8563 Месяц назад
Chitsime chimaera chakuya chikaphwa😢😢
@henrychikuse1543
@henrychikuse1543 Месяц назад
Masiku omaliza ana amulungu adzakhala akuphedwa
@MevisiWalani
@MevisiWalani Месяц назад
Tizamukumbukila chilima chifukwa chakudekha kwake komaso kuopa Mulungu zachisoni wafa imfa yowawa imene dziko la Malawi silizayiwala
@charitykambola
@charitykambola Месяц назад
Ndidzamukumbukila ndimiyambi R.I.P
@ZaneleKhoza-cp1hi
@ZaneleKhoza-cp1hi Месяц назад
Malawi 😅😅
@GriffinaziziSoko
@GriffinaziziSoko Месяц назад
Rip my big man palibeso
@PatrequeFanuelKaussiwa-nq9ou
@PatrequeFanuelKaussiwa-nq9ou Месяц назад
Mkulu ameneyi tidandaula kwambiri ngati munthu koma pa chitukuko anaika Malawi pa ma vuto polowetsa mcp mboma
@user-ep6ro8uk6e
@user-ep6ro8uk6e Месяц назад
Zosayenda koma kunena mwachilungamo chilima ndamene anapeleka dziko lino mwadani kut anthu aziwona nyekhwe achinyamata akungokhala pano kusowa zochita zitchito kulibe
@georgephiri4181
@georgephiri4181 Месяц назад
Wayifeladi mbendela ya Malawi koma Chakwela ambuye amuwone
@BrianAmbeswa
@BrianAmbeswa Месяц назад
Tizawakumbukira chifukwa anali munthu ozichepatse mzimu wawo uuse mutendela
@bubakaramidu
@bubakaramidu Месяц назад
Ndizawakumbukila Achilima chifucha msso phenya aeo apita nawo
@nkosikhonasiphiwemdlalose227
@nkosikhonasiphiwemdlalose227 Месяц назад
Ine siwandale ndipo kumalawi ndinachoka ndili wachichepele komano nkhani ya Chilima yandikhunza ndipo ndalira ndikulirabe kuona mmene afela atagwila colona manja Mulungu wa moyo tichitileni chifundo nkhondo iyiyi ndinu nokha mungaikwanitse palibe chinsisi panziko
@user-ol1hf7ru1v
@user-ol1hf7ru1v Месяц назад
Amen 🙌
@MIMIEZenga
@MIMIEZenga Месяц назад
RIP BIG
@saidiBerason
@saidiBerason Месяц назад
Miyambi yake monga njoka saweta
@HeriqueJulias
@HeriqueJulias 5 дней назад
Why Malawian? Why Malawian? Why Malawian???
@ZaneleKhoza-cp1hi
@ZaneleKhoza-cp1hi Месяц назад
😅
@MIMIEZenga
@MIMIEZenga Месяц назад
Will meet other side of the life 😢😢😢
@MorrisMapiri
@MorrisMapiri Месяц назад
Watichotsa Mantha moti even gun point mmalawi sazanjenjemera
@PatrickMailos
@PatrickMailos Месяц назад
Amatilimbikisa kuti tizikhala ogwirizana komaso kitilimbikisa achinyamatafe pakhani yachitukuko
@KalipentalaJamu
@KalipentalaJamu Месяц назад
Ndidzamukumbukila chifukwa chamiyambi chamudimadima mwana wambuzi anayamwa tonde
@user-yl3lg5fk8f
@user-yl3lg5fk8f Месяц назад
Harry suliyani my classmate at nayizi primary bangwe good job bro
@user-xg2ks9nw5q
@user-xg2ks9nw5q Месяц назад
Malawi talusa munthu ofunikira kwambiri palibe wina ofana ndi chilima
@PatrequeFanuelKaussiwa-nq9ou
@PatrequeFanuelKaussiwa-nq9ou Месяц назад
Zikomo kwambiri
@Zulupauljq2dz
@Zulupauljq2dz Месяц назад
Ntchito zabwino monga kuyimira dziko
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q Месяц назад
Koma chakwera kumutenga zako kukamuphera kumupoto komwe iweyo umadako kumupoto chakwera iwe sataniki wakulu chakwera
Далее
The lightweights ended Round One with a BANG 💪
00:10
What is going on? 😂 (via haechii_br/IG) #shorts
00:15
TONDE WADULA DRAMA SERIES EPISODE 114
28:51
Просмотров 12 тыс.
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Просмотров 138 тыс.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Просмотров 111 тыс.
Магия вне Хогвартса
0:11
Просмотров 2,6 млн