Munthu amene anapanga kuti chilima ayende pa ndege akhale munthu oyamba kupereka umboni chifukwa iyeyo ndiamene ali ndi nkhani yonse ya imfa ya chilima ndipo akuziwa chilichose chomwe chinachitika ndipo ndiyemwe anapanga plan yonse ya mmene chilima amayenera kuyendera
Well said but kwathu kuno chilungamo chimabisala when people in power, rich and highly trained and educated are involved coz they influence the outcome of the investigations
Well spoken, keep on giving better and good advice to the nation of Malawi, only God knows what really happened the day our beloved deputy president passed on, let only the investigation reveal the truth