I don't support any idea of making Alliances with Dpp because both Dpp and MCP is ruled by people of same ideology of the one party system. I think the good think UTM can do is to rebuild party with its new ideology but for the coming 10 years. It should have the long term goals by encouraging and promoting new ideas among youths who will be more voters in 2030 while expanding their presence in the parliament.
Ine si mzika ya Malawi, koma ndinkakhala zaka 13 mu dziko, ndipo ndidzahkalanso. Ndinkamuuza anthu poyambira chaka cha dzana kuti njira imodzi yokutithandiza kugonjetsa ndiye ndi yomweyi. UTM atengane ndi DPP, komwe a Chilima anachokera. Maso anga amanyowa ndikamameera zinkhani zikuchitika. Mlengi wathu atitsogolere mu nkhondoyi. Zikamatentha kumenya zitadzakoma kugonjetsa. Without confidence one and ones are twice defeated in this race of life(Marcus Garvey). Moto iyake basi. Kusengezeratu mwa kathithi. Love an peace. Best wishes 11 thousand km away from you my people. Ndimakunyadirani kwambiri❤❤❤
Koma kalindo anakonza ifetinkaona Kuti awa awa analindi cholinga because munthu amalandila malangizo aabwana ke Koma uyu Mmmm anati escariot uyu😂😂😂 aziona next step
Bon Kalindo alibe mbali that's one thing about him I like amangotulutsa mabvuto wambalizonse ndiku ng'alula iye wautali azabweranso ndiina. Mumisala yakeyi mulinso mfundozina zabwino andalenu tolanimo zothandizazo wamisalatu adaona nkhondo the dddd cccc 😂
To be honest Malawian the government is no longer existed there's no government to rule Malawi how is going to be the Parliament without the alliance of the government because that government was formed because of alliance
Tsogolo lathu lowala ili mmanja wathu, Mlengi wathu atitsogolere . Kwacha dzukani, tulo ndi lokama, koma ufulu ndi mtendere ndi zithu za mtengo wa patali.
Ine phee kumastand no more recycled politicians be it UDF, MCP, AFORD, DPP, PP, PDP, UTM. We want achinyamata tilamule tokha. NRC for the prosperous Malawi
Politics is a game that needs proper strategy. In politics there is no permanent enemy. In my personal opinion, it can be wise enough to gang with DPP if DPP can accept it. Otherwise united we stand divided we fall.
The only way for utm is to unite with DPP afford and udf , ldont think among this for partys can make alliance with mcp , most malawians want the alliance of DPP utm afford and udf
Aaa amalawi nsitilalola kuti voti opanda ma ID ansadzalembetse voti PAPO BOLANI IDZALEPHELEKE VOTE TIDZAWONE MENE AWONONGELA ZA ID IDZI OSUTSA WADZELU.ANGALOLE ABOMA KULENGEDZA KUTI OPANDA ID ASALEMBETSE VOTE OTSUSA NDIKUMVUMELA AKUDZIWA KUTI KUMWELA NDI KU POTO ANTHU AMBILI ALIBE MA ID DZIZAPANGA DZIWONETSELO ZA DZIKO LOSE KAYA AKUDALILA MAI YOLAMU TIDZAKOMANA KUTSEWU KOKO MCP IDZACHOKE NASI 2025 za ID ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii TAKANA A MALAWI
Ayi koma mcp is too much they failed what development has mcp done, devaluation fertilizer in dpp time was at 25000 now 95000 can't to see the different killing and intimidation. Sankakwanitsa zonse koma awawa angokwanitsa ma speech koma pa ground 0 pa 100