Andale ndi athu oipa ndizoona ,,koma ndale za tonse alliance ulendo una akutionjeza,,,zinazi this current government akuyenera afufuze nkhope yamulungu,,,azidziwatu pena kuti izi ndizachabechabe Iwo eni adzafasotu!!!
Km ndalama mukuonongaz mukudziwa kt eni ake aMalawi akuvutika?........bwanji ngat zachuluka tamapatsan ma company kt bread atsike ndi soap bwanji just mention a few..
Kodi nzotheka kuti tikhale ndi silent special forces Ku Malawi kuno tingopanga za MCP iyi basi chifukwa campaign nde sapangatu akapangila ground yake iti yoti akhale ndi chikhulupiliro kuti a Malawi akawamvetsera nyasi zawo mapeto Ake akachoka ataphwanyidwa ndi miyala ngati sakudziwa savage people
Usi amaoneka maso mwa mwa mwa kuchenjelesa. Ka snake kenikeni. Blood in their hands, angobwelesa matemberero to their generations to come. Anawo zizukulu zawo mapemphero awo azakhala abomination before God. Peace will be their enemy.
We Love you our junior pangolin no matter what they can't find you chifukwa inuyo Muli mumapapiko a mwini moyo wanu Chauta, Namalenga chisumphi. Ndeno angotaya nthawi azingodya basi
Usi or akanapanda kuwauza a mcp zoti akuthetsa chibale koma Chilima akanafabe chifukwa chipani cha mcp sichimafuna chilima kut adzaimile pa president so osaloza chala usi ayi mcp ndiyakupha basi tiyeni pa ten tichotse pampando chakwela basi , Chakwera ananena yekha kut adzaimaso kusonyeza kut mpando amkaufuna and anakapezabe njira yophela Chilima
Mr Mtanyiwa End Mr Kalindo , mulungu sakutayani tikukuikizani m,mmanja mwa mulungu azikutetezani nthawi ndinthawi mukutiimilira ambuye akusungeni maka kukutetezani Kwa adani a MSP
Ambuye azikutetezerani a ntanyiwa ,amene akulimbana ndi Inu akulimbana ndi Mulungu kumene amene akulimbana ndi a rwara akulimbana ndi Mulungu kumene anthu a Mcp opanda nzeru mmalo mopangira chitukuko ndarama akupangira kuti achotse mutiti ya anthu heeedee tawaonani eti anthu opanda manyazi ngati awo timakhnyadirani a ntanyiwa may God bless you all the time
This is very sad. Chili kwa nzako chigwile nyanga zoona? This is evil at its highest peak. Wafa wafa! zoona....the real photocopy of the devil himself. Ambuye atikhululukile. Komanso mu Bible mulibe this Quote or the phrase “to err is human, to forgive is divine” is not a biblical quote, but some Bible verses support the idea: Colossians 1:14: Says that in Christ, people have redemption and forgiveness of sins Ephesians 4:32: Says that people should be kind, compassionate, and forgiving to one another, just as God has forgiven them in Christ
People are sleeping literally without food yet they can spend all this huge amounts of monies just to protect themselves.May God honestly judge them.God bless you in and may he always protect you