Ndinaganidza izi tsiku limene Achilima anatisiya kuti Marry ngati amamukonda mwamuna wake kuchokera pansi pa mtima akuyenera kuimira u President now am so happy to hear that Osatopa osatopa Mary Ambuye akutsogolerani mu zonse chifukwa chipanichi mukapatsa munthu wina ndithu kutha kukhala komweko chikadzawina azatsintha zina Ndiye Ife sitikufuna kutichipani Cha UTM chinthe chonse Mah musafooke maso patsogolo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
It's not good idea at all because we all know that there is vise president of UTM, that person he is the one who suppose to be incharge despite everything.
Maganizo anga ndikuona kuti asankhe wina osati Mary ndare zotani zimenedzi munthu akayambisa chipani basi akamwarila or retirement chizikhara cha family aaaa amalawi this is another generation let's change gyz
Maganizo anga ndamenewo since day one SKC atatisiya, mmene nduonera mu UTM atsogoleri omwe angapitise UTM patsogolo ndi Mayi Chilima kapena Che Kaliati apo ayi atenga wakunja ngati achina Dalitso Mpinganjira or Kabambe ndekuti chikhara cha mphamvu nkuzawinaso
Wachiwili wa malemu a Chilima ku chipani cha UTM amene ali Manganya anatuluka kalekale mu chipani cha UTM analowa malawi congress party. ndiye nkhani ya maudindo a ku UTM Manganya zisamukhudze ai chifukwa iyeyu ndi mpeni wa nsengwa wakuthwa konse konse. Madam Mary Chilima go ahead. inuyo a UTM musanvele maganizo a wanthu amene ali kunja kwa chipani chanu
Noooo,leave her alone and let her grieve her husband bwino bwino. N I don't think politics is her thing. Akweni bwanji? That woman is a firecracker,she can make it.
Kodi Mayiwa atawina koma akuziwa zoti president sayenda opanda mamuna nde mufuna kunena kuti akwatira popano palibe chikondi akaimira alire bwino bwino mamuna wake apo bii anali kale ndi chibwedzi cha nseli
Inu Inu VC wake uti Manganya asakupusitseni si wa UTM uyu anakakhala ndi wa UTM sanakora kukhala Vice chifukwa Chilima wafa imfa yowawa inu uyu ndi MCP mkuthekanso plan yopha Chilima inachokera kwa Maiko usi cholinga akhalepo Iyeyo musamale nae maiko Usi
Even Patricia must not contest..Civil service suffered too much when Madam Joyce Banda was rolling Malawi .she hated civil servants and she grossly stole Malawi funds in her cash gate. So Malawi don't need women to be rulers OK notre women them are become so proud and pompous.. mpaka ife ma civil servants tinawapangirq mademo. Nkuwaika mbokosi ngqti amwalira.kkkk