Тёмный

Mtsogoleri Oyenela Ndi Chilima Basi - Samuel Lwara 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 29 тыс.
Просмотров 14 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says Right the Saulos Chilima Vice President of the Republic of Malawi is the only person qualified to be President of the Country.
Ku Nyasa Voicebox, Samuel Lwara wati Right the Saulos Chilima Vice President of the Republic of Malawi ndi munthu yekhayo amene ali woyenera kukhala mtsogoleri wa dziko.

Опубликовано:

 

5 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 107   
@AishaChibwana-b8o
@AishaChibwana-b8o 5 месяцев назад
That's true SKC my vote ❤❤kungoti anthu mumadana ndi chilungamo nkhani ndi mtima wa nkhwizi basi but Mr Rwara ndi munthu ozindikira❤❤
@carlossadimba595
@carlossadimba595 5 месяцев назад
He is the man of the match in this political arena.......and I love his courage yet MCP without CHILIMA they can not carry the day
@VenançioZocueza
@VenançioZocueza 5 месяцев назад
True, chilima he is intelligent one.from mozambique.
@DavidPhiri-o6w
@DavidPhiri-o6w 4 месяца назад
Vote for chilima. He is suitable to run Malawi
@PaulNgambi-ep4kt
@PaulNgambi-ep4kt 5 месяцев назад
Exactly Chilima must rule this countly
@EsnartNkhoma-m2c
@EsnartNkhoma-m2c 5 месяцев назад
Mr lwara mukuyimenyatu nkhondo,, tili mbuyo mwanu
@eliasMwamba-q5f
@eliasMwamba-q5f 5 месяцев назад
Nkulu iwenso Mutu wako sukugwila bwino ayi,chilima ndiye anaika a Malawi pamoto.amalawi si opusa sakumufunanso chilima
@WittinessBeza-cp5kf
@WittinessBeza-cp5kf 5 месяцев назад
Ndiye iweyo bwanji osalamulira ndi chipani chako cha mcp chankhanzachi
@DesmondKanguwe
@DesmondKanguwe 4 месяца назад
Akumena zoona ... Malawi ngti dziko singasuthe ndma leaders enawa ndiandale bas koma nzeru zoyendetsera chithu chilima kaya madana naye koma that guy is genius gv him a chance... Enawa mbola
@AishaChibwana-b8o
@AishaChibwana-b8o 5 месяцев назад
Chilima ayankhulatu nthawi ilipo paja munamusemera nyau nde akudikira chiweruzo koma ayankhulatu ndipo kwa munthu Wa mnzeru zake kupatula wa nkhwizi ufiti ukhutukumve chilima is a best kuyima utsogoleri wa bwino olo Chakwera amadziwa kuti mwanayu ndi machine komanso first year zinthu zina yenda bwino becoz of that man Mr Rwara never give up ❤❤❤❤❤
@BrunoMaphuza
@BrunoMaphuza 5 месяцев назад
I love Chilima and UTM❤
@PeterPhiri-di1ux
@PeterPhiri-di1ux 5 месяцев назад
tikuvutika chilima yo ali muboma wtat is he doing 2025 never apm my vote
@FunnyKatchenga
@FunnyKatchenga 5 месяцев назад
Amugulatu ameneyo.
@DavidPhiri-o6w
@DavidPhiri-o6w 4 месяца назад
Chilima is right president of Malawi
@andrewchirwa2193
@andrewchirwa2193 5 месяцев назад
Vote saulosi chilima
@KellyHart-pi4hd
@KellyHart-pi4hd 5 месяцев назад
Inu mutirakwitsa kurankhura Ngati mutumo mulibe nzelu ingokharani muzizikanda ndi Chilima wanuyo
@phirimacdonald8638
@phirimacdonald8638 5 месяцев назад
Akulu awa ndiopusa, wakupasani zingat chilimayo munthu wakuba ngt amenewo lero tili pamoto chifukwa Cha ameneyo chilima,ndiye bola atupeletu kapena peter osati onamayo
@AlickMDayi
@AlickMDayi 5 месяцев назад
You can said that again brother Lerolino anthu akulira chifukwa chaboza la Chilima ndi mzake Chakwera anthu oyipa kwambiri amenewa Ndiponso akufunika adzamangindwe atizumza kwambiri
@KellyHart-pi4hd
@KellyHart-pi4hd 5 месяцев назад
Izizi ndiye mbwelera zenizeni mtsogoleli samafunika kuyanganira zoputsa Ngati Chilimayi ,Ameneyi ndimanyaka enieni osayesera gys tizalira Ameneyi azizangoramulidwa ndi Azungu Ngati Chakwera emweyi ,Ndiposo iyeyi akanakhara wanzelu sakanalora Kuti pamgwiluzano wawo iyeyi akhale otsatira wachakwera coz iyeyi anakharapo vaice Chakwera palibe chomwe amadziwa chilichonse Koma anakwanitsa kumupugsitsa iyeyi ndikutheka ndiye nzelu zake Za Ameneyi zilipati ?Osayesera mbwelera zimenezi kurankhura amatha Koma kuchita zinthu ndipanja penipeni
@user-lf6qf2tw5o
@user-lf6qf2tw5o 5 месяцев назад
Mkufuna ya ufa muuzen akupasen bas osataya nthawi yanu kumat chilima chilima
@JoyJere
@JoyJere 5 месяцев назад
Bola adad
@MuhammadSauzand
@MuhammadSauzand 5 месяцев назад
Umutenge chilimayo akakhale president ku family yakwanuko
@AishaChibwana-b8o
@AishaChibwana-b8o 5 месяцев назад
Aaaa opusa ndi inu nonse omwe mukunenazo za adad anali kuti?? Komanso agogo ngati amene aja mukufuna muziwapangira zochita lomwe paja ndi akhufu Kumve ndakhulupilira SKC my vote ❤❤❤❤❤
@HanifiYaumu
@HanifiYaumu 5 месяцев назад
Iweso machende ako ndichilima wako emweyo iwe sudziwa kuti chilima ndiamene adapangitsa kuti tidzivutika choteke mapazi ako galu wachabechabe
@BrunoMaphuza
@BrunoMaphuza 5 месяцев назад
That's true
@NathanielNthala
@NathanielNthala 5 месяцев назад
He is saying the truth.
@WakuMalawi
@WakuMalawi 5 месяцев назад
I have a tough time accepting Chilima as the next guy. He's been a part of Tonse Alliance for years. He is going to continue the mess Chakwera has started.
@carlossadimba595
@carlossadimba595 5 месяцев назад
He is just a sign post .....which shows Lilongwe 20 km but actually it doesn't go to the location .....achina mkaka they are digging holes there for him
@MjombaMjuba
@MjombaMjuba 5 месяцев назад
Mufune musafune, Saulos Chilima alamulira. A DPP ambiriwa akuwona kuti Mutharika wakula, akufuna adzidzamubela ngati m'mene mwana akamakhala ndi agogo, amangokwabela nanga simunthu wamkulu. Nawonso a DPP akufuna m'dalayu adzidzangomubela, plz Malawians be careful.
@greychizaka4088
@greychizaka4088 5 месяцев назад
SKC vote
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 5 месяцев назад
Inutu mukunama chilima ndi chakwela onse ndi wolephela balibe mungauze amalawi inunso ndi chitsilunso cha munthu mmulibe manyazi mmutumo mwazaza mamina mbuzi yamunthu mukutitenga ife amalawi ngati opusa agalu amenewa sitikwafuna inuyo pwala lanu chitsilu
@marryphili5419
@marryphili5419 5 месяцев назад
Chilima ndi chakwera wose ndi amodzi ndi mbamva zokhazokha musatipusise ife ngati akupasani ndarama zingodyani Koma mission yanu siyigwira tatopa ndi mbamva zimenezi iesh 🤮🤮
@AmusedDimSum-hd5yp
@AmusedDimSum-hd5yp 5 месяцев назад
ntchito ya chilima inatha anali oyitanira bus itazaza ntchito yake inatha musataye nthawi yanu zachilima amene uja watha basi
@JusticeKawilira
@JusticeKawilira 5 месяцев назад
Chilima ndi amene anapangitsa kuti MCP ilowe m'boma tinada nawo kukhosi mukuchemerera yo zao ndi zimozi ndi MCP
@emmanuelmpenda2673
@emmanuelmpenda2673 5 месяцев назад
Massive
@Andrewmwamadi
@Andrewmwamadi 5 месяцев назад
Mbava zili mu dpp n mcp sizamasewera chilima akumuchitira nkhanza chonchi cz both mcp n dpp akudziwa kut he is the future of malawians and azawasosola bt aziwe kut mcp n dpp these two sangalowe m'boma without skc izi aziwe n dziwani kut dpp n mcp kwao kwatha
@MonicatimanyeShaba
@MonicatimanyeShaba 5 месяцев назад
Zoona zake ndizoti SKC amawona mwakuya kwambili Koma AMENE amakhala pachiwongolero amawona mozikundikila nichifukwa Chale zimawa vuta kuwongolelawazelu zikoli NDE osewo poti wakuwona mwakuya azingo khalila kulawa boma kulitaya kulawa boma kulitaya kamba ka mutima woti zosendipanga ndekha pawekha sungakhale munthu vayisi amamutenga Kuti alibe zelunthawizose komandamene angathe kukuwonesa pomwe Pali choipakuti usapitepo
@YoungMwacho
@YoungMwacho 5 месяцев назад
Zaziii
@MagdaraneChidamula
@MagdaraneChidamula 5 месяцев назад
Hehede uru kuno , malo mopemphera tikungolalata anzanutu zikavuta amapemphera ife maromopemphera tikungolalata God have mercy on us
@charlesdaisi616
@charlesdaisi616 5 месяцев назад
Koma nkulu iwenso kkk ziko lake liti ukuuza anthu okufaa kapena chani?
@0wenNkhambule
@0wenNkhambule 5 месяцев назад
Good Message ❤
@aubreytiyess
@aubreytiyess 5 месяцев назад
Aaaaa. UTEM2025❌❌❌
@chimwemwegama6143
@chimwemwegama6143 5 месяцев назад
Pantumbo panu nose zikoli lagwa chilimayo ali kuti,minyero zanu agalu,,,tikuzunzikaku ife pa ground pano
@Patrickmanyozoproperties
@Patrickmanyozoproperties 5 месяцев назад
Chilima emweyo basi ife taona kuti chilima amaopedwa that's why akumpangira maupo
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 5 месяцев назад
Chilima ndi chakwela akumadziwana ,akufuna azitipusitsa ifeyo
@ChristopherPhiri-xq7hv
@ChristopherPhiri-xq7hv 5 месяцев назад
Chilima mukunenayo mesa ndi part of government , and palibe chanzeru chomwe akuyankhula. Palibe chanzeru akuchitapo
@MatSecurity-gq3hr
@MatSecurity-gq3hr 5 месяцев назад
Timpatse mpata, Zoonadi onse tawayetsa uyu mfundo mzake sizinagwileko Ntchito payenkha, ubwino wake Ndi 5yrs, tizithothola
@WilfredMathews-yl6ij
@WilfredMathews-yl6ij 5 месяцев назад
Ndipo sukunama chilima alindikuthekera kolamulira coz iye ntchito zake sitidazione
@AishaChibwana-b8o
@AishaChibwana-b8o 5 месяцев назад
Ndiponso mudziwe akulamulira dziko lino si chilima nde akufunika ayesedwe basi
@MagdaraneChidamula
@MagdaraneChidamula 5 месяцев назад
Abale tisalire timatitu zinthu zisinthe oipatu ndi adadi abusa ajanso aipa lero kunokuno kumalawi zationekera kkkkk abusa abale musawatero mumawavotera nokha komanso munampanga chipongwe mwana wayeni komanso munampanga Peter chipongwe Mulungu wakwiya mulape apo bii tidakanzunzika.
@TrizaGeorge-q8w
@TrizaGeorge-q8w 5 месяцев назад
Ndilipo mulungu akhululukile ndithu
@DanielZunguza
@DanielZunguza 5 месяцев назад
A Samuel muli ndi misala,yanuyo singawine.
@CharityChikomo-hl1gz
@CharityChikomo-hl1gz 5 месяцев назад
alibe funding yet boma likungogawa ndalama ma 150 &700wat nonsense
@GodfreyMphaya
@GodfreyMphaya 5 месяцев назад
Ngati malawiyi ili ikuona mavuto ali panowa nchifukwa cha ameneyi
@AustinZidanaNessam
@AustinZidanaNessam 5 месяцев назад
Go to Limbe eeesh town yayipa mikodzo yokhayokha , pple are building in drain filing drainage , minibus parking everywhere aaaaaa zinthu zachita katondo
@dinchisale
@dinchisale 5 месяцев назад
Wakupatsa zingati chilimayo, galuiwe
@YoungMwacho
@YoungMwacho 5 месяцев назад
Kkkkkkk kusauka ndi ukapolo
@user-lf6qf2tw5o
@user-lf6qf2tw5o 5 месяцев назад
Analikut nthawi Yonsei Mesa anali ku Malawi komweko ndikumaona mmene anthu akufera ndi njara
@DanielZunguza
@DanielZunguza 5 месяцев назад
Mbava ngati amene
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 5 месяцев назад
Iwe choka ndi chilima wakoyo ngati wamudyera udzabweza
@JonathanMtambo-w6e
@JonathanMtambo-w6e 5 месяцев назад
Our economy collapsed sometime back I don't know how malawians are failing to see that
@LukaTonkhwe
@LukaTonkhwe 5 месяцев назад
😢Osafooka thawi ilipo
@ChikondiChauma-ib9pg
@ChikondiChauma-ib9pg 5 месяцев назад
Uyu ndichophwisi chencheni iyaaaaa mesa akulakwisira limodzi
@WysonMpatama-cv1mc
@WysonMpatama-cv1mc 5 месяцев назад
Eeeti akuononga onse palinso nkhani ap
@mphatsobonongwe8131
@mphatsobonongwe8131 5 месяцев назад
Dzina lanthu lioneni sitiopa , chilima patsogolo
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 5 месяцев назад
I do understand anthu amene akumamulakhulira chilima ngati iyeyondimwana bwanji if chilima is not happy where's he should come out and speak out himself and I'm not support any of these guys ndikati ndadya ndimayenela ndigwiletchito ndekha
@AishaChibwana-b8o
@AishaChibwana-b8o 4 месяца назад
Iwenso agogo kunyumba kwako
@uchizJoelMumba
@uchizJoelMumba 5 месяцев назад
Misala imayamba chotcho ndiye chonde abale ake amunthu uyu pitanayeni kuchipatala munthuyu ndiwodwala
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 5 месяцев назад
Zachilimaso pano sitikufuna ochenjela mwautsilu
@MiddayDeleza
@MiddayDeleza 5 месяцев назад
Nde chilima mukuona ngati angayendetse dziko? Popeza zawo ndi dzimodzi nda pule ngati akuzengedwa mulandu okuba ndalama nde angatsogolere dziko ameneyo? Kaya mwina
@DanielnachanzaBanda
@DanielnachanzaBanda 5 месяцев назад
Ukunena iwe
@HurryBeston
@HurryBeston 5 месяцев назад
Icho ndie chilungamo baasi nkhakhale anthu ena saavomereza
@AmoniNicholas
@AmoniNicholas 5 месяцев назад
Mmmm Abwezi mtsogoleri akhoza kukhala ochilimika, koma ngati ifeyo Amalawi azanga tangokhala manja lere, ukhozakukhala iweyo wazeru ukuyakhulawe koma patsogolo pano uzachititsa manyazi Amalawi ife ngati mmene anachitila bon kalindo iwe, ndiwe wabodza kwambir
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 5 месяцев назад
Anatiponya pa moto pano wangoti ziii
@Mavuto-b4f
@Mavuto-b4f 5 месяцев назад
What you are talking it's not true ,chilima ndi mmodzi mwaiwo amene Waikato pamavuto malawi chifukwa cha bodza lalikulu,kunamiza mtundu wa a malawi,anakakhala kuti tili ndi mwayi ife amalawi Olira kuno ku south Africa ndinakalanda ndalama zonse za chilima mkugulira chakudya ,mankhwala,komanso kupeleka ndalama kwa mahakazi kuti atsegule ma computer mmene muli information yonse why mukuikila kumbuyo munthu amene Waikato pamavuto amalawi,komanso a Mtambo anthu amene mwathandizila kuika amalwi pamavuto,timakudandaulani kwambiri.
@tasmania527
@tasmania527 5 месяцев назад
Ngati kuli mtundu wasankho ku Malawi ndi Alomwe, oh ya. Ali ndi unjustified hatred ndi Chilima for no reason. By the way, Lwara walakwa chani?
@UlemuChimembe
@UlemuChimembe 5 месяцев назад
Nonsense
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 5 месяцев назад
Samuel Lwara Pachiphwisi Pamako Mwana Wa Hule iwe, Chilima wapanga chani? Zomwe analonjeza zikuchitika? Pantumbo pako, Chilimayoso Pantumbo pake, Zitsilu
@WysonMpatama-cv1mc
@WysonMpatama-cv1mc 5 месяцев назад
Alwara kupole moto ndachilima anuwo
@arnoldchikopa2611
@arnoldchikopa2611 5 месяцев назад
Chilungamo ichichi
@andykunyenje529
@andykunyenje529 5 месяцев назад
Lwala umwa chani aise
@samdiverson9733
@samdiverson9733 5 месяцев назад
bodza chilima yo bola APM bola
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 5 месяцев назад
Chilimayo akalamulire kunyumba kwa iweyo Lwara
@NathanielNthala
@NathanielNthala 5 месяцев назад
Khokhokho
@RICHARDENIFANT
@RICHARDENIFANT 5 месяцев назад
Zoonadi
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 5 месяцев назад
Born kalindo wayamba mantha kuyankhula koma enafe sitikuopa
@ZelinaKisswell
@ZelinaKisswell 5 месяцев назад
Alankhula bwanji munthu Ali mndende 😮
@NelsonNyasulu
@NelsonNyasulu 5 месяцев назад
Kkkkkkkkkkkk
@AubreyHara-lh9md
@AubreyHara-lh9md 5 месяцев назад
You are talking too much because you were booted from the current government
@EstherJamesChipembere
@EstherJamesChipembere 5 месяцев назад
Achilima tili pambuyo pawo koma aime paokha achoke ku mcp
@ShadreckKusani-vi5ki
@ShadreckKusani-vi5ki 5 месяцев назад
Zoooonazake Dr chilima akufunika bomali atsogolele zisintha,,umboni ndili nawo,tonse italowa chilima anayamba kuyende ekha mdzipatala ku MRA koma zitamveka anamuletsa, atalamulila zitha kusinthadi
@KellyHart-pi4hd
@KellyHart-pi4hd 5 месяцев назад
Inuso inu musamangomvera zilizonse Kuvotera Chilima ndiye bora kumutsiya razalo emweyi ndiagalu awa saziwa chilichonse
@AleksaWilliams
@AleksaWilliams 5 месяцев назад
Chilima ndi Chàkwera ndi olephera okhaokha
@AmusedDimSum-hd5yp
@AmusedDimSum-hd5yp 5 месяцев назад
zaziii chilimayo akawinira kunyumba kwako iwe mbulundi
@PheladiMafologela-ii3vd
@PheladiMafologela-ii3vd 5 месяцев назад
Khala chete ukutisokotsera
@arnoldchikopa2611
@arnoldchikopa2611 5 месяцев назад
Skc mote
@AshrafuKalimula
@AshrafuKalimula 5 месяцев назад
Zake izo bola ali kunja
@SamuelBoma-p1m
@SamuelBoma-p1m 5 месяцев назад
Mukutaya nthaw wakubayi sangawine😢
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 5 месяцев назад
Keep it up Lwara, boma la chakwera ili latikwana, walepherela.
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 5 месяцев назад
Za nzii
@MagdaraneChidamula
@MagdaraneChidamula 5 месяцев назад
Hehede bora adadi ikaora modzi zonse zaora onena amati ,not again😅😅😅😅😅 lero tikukanika malo mopita kukanani tikupita kwapharaoh kkkk
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 5 месяцев назад
Kulankhula sikuvota ovata ndi amalawi zachilima wanuyo munyera sua
@JonathanMtambo-w6e
@JonathanMtambo-w6e 5 месяцев назад
Yes Peter is just too old let him rest
@ShadreckNgozo-ng6ll
@ShadreckNgozo-ng6ll 5 месяцев назад
Kunyumba kwa makotu
@FunnyKatchenga
@FunnyKatchenga 5 месяцев назад
Zaziii
Далее
Chakwera Will Not Win The Elections - Samuel Lwara
22:19
Ku MCP Kuli Nkhanza - Samuel Lwara
25:39
Просмотров 10 тыс.
Mumanga Anthu Angati? - Samuel Lwara
13:34
Просмотров 9 тыс.
TIMES EXCLUSIVE - 30 MARCH 2019 with Saulos Chilima
59:49