Nanga akakuonetsani ma video akalekale ndiye mudzatani kapena achitenga chimangacho ndikumangoyenda nacho koma osagawa nanso mudzikhala ngati boma lanu la mcp mumaliziwa bwino bwino simwanena kale kuti makolo anu ndi a mcp
What happening in malawi is not good The best way is to change president who can change the life of Malawian to a better life Chakwela is surrounded with stupidly advisers Let's change leadership new president like Burkina Faso president who care more about his people
Ena kumati boma ndi la chakwela kusaganizira moyo umene uli kunza chifukwa tikamuvotela chakwela ndithu kuli Mavuto kutsogoloku lero zili bwino si mukulandila ti 2000 sindikudana ndi chakwela ayi koma zintchito zake iiiiiiiiii Amalawi chonde tikavote mwanzeru anthu chomwe akudziwa ndi kuba