Chonchi cyclone athe ku Malawi, ka dziko kongozaza ndi anthu adyela opanda Chikondi Chilungamo mukuchiziwa kuti zinthu sizilibwino ku Malawi koma chifukwa choti akugawilani ndalama zakubazo basi Shame😭😭😭
Inu osaimba yanu nyimbo mulandileso bwa😂😂😂😂😂😂 Hypocrites people in Malawi mwachuluka... Even muzintchito mwanu mazoba inu mukuba imagine mutakhala nduna basitu mumaliza dzikoli.... Muzifufuze man ngati iweyo pawenkha you are a saint... Zoba