Mwanayo waphedwa ndi m c p zikanakhala kuti waphedwa ndi andalewo osakhala m c p bwedzi zitafufudzidwa ulamuliro wakupha kumphamvu ya mulungu ukuyenereka kutheratu. 😂😂😂😂😂
Anthu amaganiza kuti azakhala muyaya padziko pano,, Kamuzu used to call himself life president koma pano alikuti, Blessings Chimangeni anaimba kale zaizi. Pangatalike pangatani aliyese adzafa and this is the fact