Bvuto ndiloti onse a mcp mitu sikugwira aii president akudwala ndipo izi ndizoona that's why mnaona dzuro a Richard komanso nkukuyu analiko okha ku Rally ya dzuro ija, kodi amalawi enafe tikanagonabe mpaka lero dzukani sinthawi yogona inu amalawi
Dzikomo kwambiri Limpopo fm muchimve kuti timakunyadirani kwambiri Kubwera kwa inu pa Malawi palibe chisinsi kani akungozikola kola okha kusowa chogwirika choti angakambe kwa a Malawi Inu akuti a Kunkuyu komanso ati a Chimunthu Banda chitani manyanzi sitimakusowani ndi ma rally anu ongotukwana ndikunena anthu mm'alo mowanamiza kachikena aMalawi enanso otemberedwa kt azakuvitereni mfundo za chitukuko, mukhalike Ife Limpomp fm, Bakili Muluzi tv, the DC ndi onse amaimira a Malawi pa chilungamo tili nawo ngangangaaaaa bco akuulura nyatsi zobisika
@@KingDavedNkhata muziti amayimila DPP osati amalawi osasokoneza pakati pa DPP NDI amalawi amalawi it's everyone pamene DPP it's a specific party nde anthuwo amayimila DPP as party not as a country.
Akulepheratu kuishura ladio yomwe imanenayo koma chifukwa limpopo ndi bakili muluzi TV samapuma nayo bwino that's why mmmm ndale za ku Malawi zotukwanana
@@RuthUnderson nde or zoti akudwalazo ndizaboza zokha zokha zo Mesa alimpopo or what ever you call it amanena Kut chakwera akudwala ndipo mwakaya Kaya Moti Ali Ku chipatala cha garden city Ku south Africa chonsecho zaboza inu or mtanyiwayo he is there just to let chakwera down but let me mind you come September 2025 chakwera will still be president mark my words.
Ngakhale kubwezela kuli keamwini Yehova koma achakwela adwale ndithu mpaka alape mizimu yaanthu 9 it's not easy magazi awo akumuzunguza mutu chaona nzako chapita mawa chili kwa iwe imfa imapita palipose
Iwe wa Limpopo poti unaona ndi diso lako lapamphumi kuti anali serious ya kayakaya tumiza video yaku garden city clinic ko Ukalephera ndiye kuti ndiwe satana
Chimwendo ndiye saziwa kuyankhula mbuli kwambuli ndiye chimwendo omangochemelela mcp akuziwa kut palibe chimene akuchita akut kufuna akuwoneka wabwino tamangokudya ndalamazo koma azizindikila kut one is one day mulungu ndiamene akakulangen inuyo a mcp nose
Aaaaaaaaaa mcp palibe amene akuifuna or muone mmene anasangalila amalawi no one need mcp and kungomwalila kuzakhala ma patty akuziwa a mcp kut amalawi sakwafuna that's why akulimbana ndi limpopo