On Nyasa VoiceBox Billy Malata says it is perfectly ok for a Cabinet minister to spend money on party delegates in order to win a seat at the party's convention. Being a minister and competing in a party convention is not a reason to subject the individual to smear campaign.
Pa Nyasa VoiceBox Billy Malata wati sizachilendo kuti nduna ya boma iwononge ndalama kukopa nthumwi za chipanichi kuti apexe mpando kumsonkhano wa chipanichi. Kukhala nudna ndikupikisana nawo pa msonkhano wa chipani si chifukwa chomuyipitsira munthu mbiri pa kampeni.
#malawi
29 авг 2024