@@MariamJohn-dg4em palitu kusiyana pakati pa UTM ndi Malemu SKC. CHILIMA anapeza mavote okwana 1 million pomwe UTM ngati Chipani inapeza Aphungu Anayi okha basi.Ngakhale Kaliati anakanidwa kwawo pa Udindo wa u MP kamba koimira utm ndiye kumachangamuka pochita zinthu. Fame ya Malemu SKC si fame ya UTM as a political party.
Well done my sister they is no way to keep on going with these monsters, we the followers shall never give up. UTM wozaaaa munya achule a mcp zombalangondo inu.
Migwirizano ikumapha tizipani ting'ono ting'ono.Mukaona kuti simungapambane imani mwanokha ndi cholinga chakuti mupeze ma MP. Chipani chimalimba ndi ma MP ku parliament. Ndi 50+1 adzakufunani nthawi imeneyo
Mmmh mau amai kaliyati sakundipatsa chilimbikiso , pali china chake chikubisidwa , but it's ok let's look the way forward . But remember l'am not politician .
Mwachita bwino kutuluka, koma ndikuuzeni kut musamachite kudikira kut pafe munthu kaye then nkumapanga chiganizo. Koma mukanatuluka nthawi yomwe Chilima anali moyo chikanavuta ndichani??? Padakafunda padadyiwitsa galu. I hope a lesson has been drawn.
U ar strong woman keep up mah don't afraid God will be with u akufuna moyo wanu ayamba ndiyeyo poti anazolowela kupha koma pano pokha tikumuwona ife aa