Father Elizeo mtalika ndi wansembe opanda mantha and amalarika za uzimu komanso zochitika mu dziko lathu la Malawi,, Ngati Chakwera akufuna kuti apenge Misala ayelekeze kumugunda.
Ndipo ine ndinamudziwa thawi ya covid anauza a bishop kut ine ndimatumikira mulungu osati muthu ndipo adakana utseka church adat akatseka church matendawo atha bwanji pot tisiya upephera
Si iye amene akuyankhula koma ndi mphamvu ya Mulungu imene ikuyankhula iye wangokhala chinkuza mau komanso sanatchure dzina la munthu ayi iye akungolalika ❤❤❤❤❤
I think Malawi was blessed with people of intelligent kuposa charakwe wen weniyo,,,, this is bravo Sir your good Lord protect you and okunva wanva osanva asanve your mwana mlomwe wakwathu wen wen😊
Zoona apa ayaluka achakwera amasileni anon kalindo ndi a Mr kamlepo kalua mukumva mau amulaliki mnzanu Koma inu basi kutengera mphamvu mukugwilitsa.apolice kukhala chida chanu phepani
koma chilungamo ndiye chimenechi zovala agawana kale chakwera alibe chisoni ndi infa ya chilima koma aziwe infa yilibe kuti ndine president dziko lilibe mwiniwache
Manganya ndi yudas yemwe.anapereka yesu sidzikusiyana lero iye wapereka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ambuye akuyendere manganya ndipo mzimu wa cakwera ukukathe
Tell them the truth man of god baibo rimati muzaziwa ndi zipaso zawo paziko rapansi pano pari ana amurungu nde parinso anthu amurungu osama sokoneza apapa
Kuthamanga kusankha Vice President ku ndikufuna kuti tiiwale mwachangu indeeee.....look at how social media is plastered with the Vice President dramas...hmmmmmmm