Keep it up my brother for standing and show the Nation that Tonse Alliance is usiless Government and let me warn Kumkuyu for playing with the Malawians.
Chitukuko chomwe abwelesa a chakwela kumpoto ndi kumanga kamulepo kaluwa basi osati zinazo bro palibe chomwe angapange let's wait will judge them better pa 2025. Osawopa, osafooka, osatopa.. Big up bro
Mabugwe kunja amapeleka ndalama koma zonse zimabedwa ndi chakwela ndi chifukwa chache anapha zake cholinga azibabe galu amenei zakoma ndalama mbava ndalama anavomeledzana Kale ku parliament zili kuti galu chakwela
Minister of transport Jacob hara akulephera kwawo kumzimba kulibetuu mseu, kumzimba kuliseu unayamba nthawi ya bingu mpaka pano amapangilapo kampeni bas alipheee. Mseu wa mzimba eswatini mzalangwe kudutsa kafukule kufika ekwendeni thakhala tikunamizidwa mpaka pano ma contractor anochoka kalekale. Komaso mavuto onsewa ndi mafumu athu sakutithandiza ai, Pepa mubale wanga zativuta bas miseu ikupangidwa komwe ku Lilongwe northern region zero pa 10
Koditu ngat kumangako akumanga ku Lilongwe kokhako kwawo amanama za msewu wa mangochi makanjira km ndi boza proper gander ikumaveka pa MBC ija kulibeko makanjira road sakumanga
Nduna ndi ma MP akumamupusisa president kumamunamiza kuti zimthu zimuyenda pomwe palibe chikuyenda nduna zones sizimamufunila zabwino president wawo akumunamiza
Kubwele a anyamata ndi atsikana'aku Kenya ngati muli ndi mantha kumeneko.apo,bi.kusa, anyamata ndi atsikana'kumangotibula, aliyese ngati uli pafupi ndi ma office.