Yes, inenso ndimmene ndavela ulalikiwu ukupita kwa aliyese ndipo ukumpuzitsa kuti tizikhala okhulupilila koma ma comment ndikuwaona ine apa eeee pakuti kumalawi kuno mmodzi atagoyamba ndi negative comment aliyense alemba zomwezo
May God bless His Word through you moderator and may He also plant a heart of philanthropy and patriotism in all political,traditional religious, and legal authorities in Malawi to be once again a Godfearing nation. Amen
A malawi sindimakumvetsani koma zowona after all what MCp has done to you in 3 weeks ago mwayiwala kale, kukuyitanani ku msinkhano inu nkupita,, mumati mukamvako chani chatsopano,,a oposition you guys are sleeping to much 😮h munayenela kukana osapezeka nawo pa chikondwelerochi,a MCP akukondelera their successful mission of killing chilima and the other 9, nchifukwa chake lero ali wokondwa,a malawi ndinu anthu osawona,how can you be invited for prayes to pray for the lives lost in chikangawa by the same man who orchestrated their death😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 Malawians are you nomal ⁉️⁉️⁉️⁉️⁉️
Amene akunyoza Chakwera tsoka Kwa iye.uli ndi tsoka iwe onyoza munthu osalakwa, ngati ndi ulesi wakowo ongofuna kulandira go to page House khalamba yanu ikakupasani za ulele. Agalu inu