Тёмный

ZOMWE AYANKHULA PA MASO PA A PRESIDENT PA MWAMBO WA ZAKA 60 INDEPENDENT 🙌🙌 

HOT 265
Подписаться 81 тыс.
Просмотров 91 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

4 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 145   
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 3 месяца назад
Amen munthu wa Mulungu achakwera ndi nduna zanu a chimwemdo kunkuyu zikhale ng'omayo mukaka zisakhale ndwiii ziziva mawu a Mulungu ndizimene zikupangisa Malawi kukhala wawumphawi ndalama akuziononga basi.
@EmmanuelNauli
@EmmanuelNauli 2 месяца назад
😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😮😅😊
@MathewsChilota
@MathewsChilota 2 месяца назад
Powerful words. We don't need to curse our nation due to painful situations. God will heal our nation
@quoniemagalasi9123
@quoniemagalasi9123 3 месяца назад
This man is one of men sent by God to deliver ❤
@LeyahPhiri-sd9xj
@LeyahPhiri-sd9xj 2 месяца назад
Munthu wamulungu wayankhula, wakumva amve zomwe Mulungu akuyankhula. ❤❤❤
@EmilyKamzoole
@EmilyKamzoole 2 месяца назад
Amen, very powerful message. God bless you, God bless Malawi.
@FelistaChiwalo
@FelistaChiwalo 2 месяца назад
Amen Abusa, Yehova ndithandizeni kuti ndizipanga zomwe chi Khristu chimanena, Amen.
@CharlesPhiri-ds1rk
@CharlesPhiri-ds1rk 3 месяца назад
Munthu wankulu....powerful massage Glory to Jesus🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
@HildaKumwenda-ho8vz
@HildaKumwenda-ho8vz 3 месяца назад
Powerful message God bless you pastor ❤
@SaamSaaam-g2n
@SaamSaaam-g2n 3 месяца назад
ABUSA alalikira osati zomwe ayankhula ndipo ndi phunziro kwa tonse osati a President okha Tiyeni tisiye zonse mmanja mwa Mulungu popeza Iyeyo adziwa zonse bwino koposa mmene tidziwira❤❤❤
@DalitsoDjimo
@DalitsoDjimo 2 месяца назад
Mwayamba bwino zedi mbale. Anthu tonse tikanamaganiza choncho tikabakhala nidziko lantendere
@chimwemwendalama6260
@chimwemwendalama6260 2 месяца назад
Yes, inenso ndimmene ndavela ulalikiwu ukupita kwa aliyese ndipo ukumpuzitsa kuti tizikhala okhulupilila koma ma comment ndikuwaona ine apa eeee pakuti kumalawi kuno mmodzi atagoyamba ndi negative comment aliyense alemba zomwezo
@HevenChiwaya
@HevenChiwaya 3 месяца назад
Strong massage this is a lesson to the politicians who pushed a Malaysian people who's dying with hunger poverty
@odalachimphepo5257
@odalachimphepo5257 2 месяца назад
For the first time seeing a preacher without recognizing POLITICIANS 😂😂
@tomasvinkhumbu7487
@tomasvinkhumbu7487 2 месяца назад
Greatest message pastor God bless you
@wonganilungu6352
@wonganilungu6352 3 месяца назад
Abale ndi alongo timaseva zithu zopanda pake mmafoni athu. Zichotsenimo zoipazo komatu sevani uthengawu waphamvu muziwubwereza×10 kuposa zinazo. Tidzapeza mpumulo woyankhidwa kwa Yehova tonsefe tikawutsatira ndi kuwupempherera uthengawu patokha patokha
@VungaQueen
@VungaQueen 3 месяца назад
Mawu uphudzitsa ndipo achilimbikitso tingavutike motani titsataye chinkhulupiro yehovah ndiye zotse zanthu👏👏👏👏
@DalitsoDjimo
@DalitsoDjimo 2 месяца назад
Zoona m bale mulungu ndiye yanko tisanyozane pamene takumana nimavuto
@HestingsZiba-d6k
@HestingsZiba-d6k 3 месяца назад
Chakwela yekha ndamene akutikhomelela Malawi siziko losauka chakwela must go
@ElizaMagombo
@ElizaMagombo 3 месяца назад
1q
@TruthMalawi
@TruthMalawi 2 месяца назад
​@@ElizaMagombo very low
@nathannbanda3345
@nathannbanda3345 2 месяца назад
This eas beautiful and powerful sermon, great 👍💯
@HildaKamfose
@HildaKamfose 2 месяца назад
Powerful massage amen
@WILFREDBANDA-o3r
@WILFREDBANDA-o3r 3 месяца назад
Powerful message ❤God bless Malawi
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 3 месяца назад
Indeed powerful preaching God bless you
@NellieMbisa
@NellieMbisa 2 месяца назад
Great message Pastor.......God bless you
@PETERSINKADZIWA
@PETERSINKADZIWA 3 месяца назад
Amene akukondwera ndi utsogoleri wa Mr Chikangawa ndiye kuti Mutu wake suyenda bwino
@serakillo8668
@serakillo8668 2 месяца назад
Ayi zkm man of god thank for good msg ❤❤❤
@florence500
@florence500 2 месяца назад
My favorite scripture... book of Job
@SalatielMathews
@SalatielMathews 3 месяца назад
Rev Yasinami Gamma,Mwatiphuzitsa Ambuye akudalitseni kwambiri,
@BerthaManyika
@BerthaManyika 2 месяца назад
Powerful man of God, uthenga wamveka
@Albertngwira-vy3th
@Albertngwira-vy3th 3 месяца назад
Amen i love this man of God 🇿🇲🇿🇲
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 3 месяца назад
Kuyakhula mopanda matha respect abusa a Gama
@phelantunikapikule4624
@phelantunikapikule4624 2 месяца назад
Amene ali ndi khutu la uzimu uthengawu wawuva koma amene ali ndikhutu koma osamava, ndiwo ma comment ambiri tikuwawonawa. Amen pastor
@feywellkapala7093
@feywellkapala7093 3 месяца назад
Powerful message man of GOd
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад
Koma azanga mbusa uyu mulungu amupatse moyo wautali
@gomesavirgo3987
@gomesavirgo3987 2 месяца назад
Y.G is the greatest Reverend of all time
@kubengovender6996
@kubengovender6996 2 месяца назад
Big up brother man!!
@Zeka46
@Zeka46 2 месяца назад
🤣😂 God bless you Gama
@LytonMfuni
@LytonMfuni 2 месяца назад
I knew my rev: never go wrong.🇿🇲
@KennyTchapo
@KennyTchapo 3 месяца назад
Wat a wonderful preaching
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 3 месяца назад
May God bless His Word through you moderator and may He also plant a heart of philanthropy and patriotism in all political,traditional religious, and legal authorities in Malawi to be once again a Godfearing nation. Amen
@RaphaelLudaviko
@RaphaelLudaviko 3 месяца назад
malawi wathu ndipamene takhalapo. Amen abusa
@vukanifracksonchinkonde7324
@vukanifracksonchinkonde7324 2 месяца назад
Wonderful preaching
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 3 месяца назад
Powerful message ❤❤❤❤❤😊
@khamakhwiliro4093
@khamakhwiliro4093 3 месяца назад
Powerful Preaching
@chipiesato-ut7hx
@chipiesato-ut7hx 3 месяца назад
Powerful message ❤❤❤amen and amen
@MikeMakaww
@MikeMakaww 3 месяца назад
Great great great apstor of the year
@RobertCosmas-bo1uo
@RobertCosmas-bo1uo 2 месяца назад
Ulaliki mbambande yobu mwayenkha munali kulimba mtima ndkukhala nacho chikhulupiriro chozama amen
@hajisonzanditha1246
@hajisonzanditha1246 2 месяца назад
Great preaching
@bernadettechoma
@bernadettechoma 3 месяца назад
Hallelujah!🎉🎉🎉🎉🎉
@richardarmittage1693
@richardarmittage1693 3 месяца назад
Amen and Amen !!!!! Mau omveka bwino kwabasi
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад
Chonde amalawi tisatembelele dziko lathu chonde mau akulu ochokela mkamwa mwa abusa yasini gama amen
@SkevaMustapher
@SkevaMustapher 3 месяца назад
Amen amen kuying'alula abusa
@LinessStafordsauti
@LinessStafordsauti 2 месяца назад
Amen man of God
@eunicesaiti
@eunicesaiti 3 месяца назад
Happy 60th independence Malawi and Long live.❤
@SafariBvumbwe
@SafariBvumbwe 2 месяца назад
Akulu mwati happy chani kkkkk kumalawi kulibe za happy mganize bwino
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 2 месяца назад
Eeee zako zili.pabwino Pali malawipa nkumati happy kakaka
@eunicesaiti
@eunicesaiti 2 месяца назад
60th independence and ufulu.
@eliasmpaso2978
@eliasmpaso2978 3 месяца назад
Powerful massage
@NDIZOTHEKABANDA
@NDIZOTHEKABANDA 3 месяца назад
Amen paste!!!!
@mablemathuso3903
@mablemathuso3903 3 месяца назад
Powerful message
@gabiembuhagondwe3629
@gabiembuhagondwe3629 2 месяца назад
Yassin gama ndiwaku 49 mama ccap church nt ku 25
@RalphZambezi
@RalphZambezi 2 месяца назад
Ndipo zobvuta Zambiri zikubwela sakunama
@HendrinaWalani
@HendrinaWalani 2 месяца назад
Amen so powerful
@kadongolakadongola
@kadongolakadongola 2 месяца назад
My reverend
@georgealabih8979
@georgealabih8979 3 месяца назад
True facts in life, ndaukonda uthengawu
@BerthaChisoni2
@BerthaChisoni2 3 месяца назад
Man of God
@BornwellChipango-s9m
@BornwellChipango-s9m 3 месяца назад
Koma anthu amalalika
@engieberlmaguaire5473
@engieberlmaguaire5473 2 месяца назад
Powerful
@ChikumbutsoTsalangu
@ChikumbutsoTsalangu 3 месяца назад
Awa nde anadalitsika ndinthu
@AtnessBanda
@AtnessBanda 2 месяца назад
Amen amen
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 3 месяца назад
Osayelekeza kuwapha awa ,taneneratu
@GiboTakondwa
@GiboTakondwa 3 месяца назад
Nkazi wopusa Ngati Mayi gotani hara
@desiremlewa
@desiremlewa 2 месяца назад
Kutumikila mulungu mwachindinje, pamalawi panga pano palibwanj?🎉 Hellooooooo
@RobertChikawonda
@RobertChikawonda 3 месяца назад
Eeeeeee ulaliki ogwila mtima
@MarthaChaima
@MarthaChaima 2 месяца назад
Amen
@StevenBwanausi
@StevenBwanausi 2 месяца назад
Ameen Abusa
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад
Amalawi bvuto ulesi ndichikwa chake mtsoleli aliyese akakhala paudindo timati ndioipa akachoka wabwino kodi zooona atsogoleli onse. alamulilandziko linowa angakhale oipa ?
@chipi892
@chipi892 2 месяца назад
U might not mean what you want to say
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 2 месяца назад
Uthenga wabwino koma amaopako pangono a kambiri munthawi ngati iyi anaungalura uthenga .😂😂 a pule osawafunanso kkk.
@HusseinMoffatt-mi1fl
@HusseinMoffatt-mi1fl 3 месяца назад
Ayasin ndi mbambandetu ndi weniweni
@ShidaMfune
@ShidaMfune 3 месяца назад
Amen ❤❤
@chiletsobisweck5007
@chiletsobisweck5007 2 месяца назад
Mwangozi
@MikeMerecah
@MikeMerecah 3 месяца назад
Shehe uja amatinamiza koma uyu,
@chifundocharles2348
@chifundocharles2348 3 месяца назад
Chakwera akuzinyoza yekha aise😂😂 and inuyo mukugwira ntchito yanji if I may ask😂😂😂
@hastingsnamasasu8071
@hastingsnamasasu8071 3 месяца назад
Amen!
@user-sx7fg1NEDG
@user-sx7fg1NEDG 3 месяца назад
Amen 🙏
@HarryMakwale
@HarryMakwale 3 месяца назад
Amen 🙏 🙏 🙏
@MosesKhobiri-pr4hg
@MosesKhobiri-pr4hg 2 месяца назад
Ndiyitana padzina lanu yenkhova
@TwalikiWisiki
@TwalikiWisiki 3 месяца назад
A malawi sindimakumvetsani koma zowona after all what MCp has done to you in 3 weeks ago mwayiwala kale, kukuyitanani ku msinkhano inu nkupita,, mumati mukamvako chani chatsopano,,a oposition you guys are sleeping to much 😮h munayenela kukana osapezeka nawo pa chikondwelerochi,a MCP akukondelera their successful mission of killing chilima and the other 9, nchifukwa chake lero ali wokondwa,a malawi ndinu anthu osawona,how can you be invited for prayes to pray for the lives lost in chikangawa by the same man who orchestrated their death😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 Malawians are you nomal ⁉️⁉️⁉️⁉️⁉️
@EllinaBitto
@EllinaBitto 3 месяца назад
Ndipo inu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@NatashaBema
@NatashaBema 2 месяца назад
Zosayenda
@SanhedrinMasauli
@SanhedrinMasauli 2 месяца назад
M'busa ameneyu ndi wandale, ananyozapo zipani zina ndikuyamikila mcp,
@DalitsoDjimo
@DalitsoDjimo 2 месяца назад
Wuthenga wabwino ambuye akudakitseni.
@PempheroAlufandika
@PempheroAlufandika 3 месяца назад
Ayasini inu ndi munthu wa mulungu ndipo ndinu mlangizi
@VincentAndrew-jz2gf
@VincentAndrew-jz2gf 2 месяца назад
Khaniyotu ndiyona
@PempheroAlufandika
@PempheroAlufandika 3 месяца назад
Ayasini inu zitigairani mau amulungu anthu munawasitha
@HamanjaManyela
@HamanjaManyela 3 месяца назад
Malawi is not poor country
@DevisonHala
@DevisonHala 3 месяца назад
Muzeni zoona aleke kupha anthu
@RedsonKambwiri
@RedsonKambwiri 3 месяца назад
Koma Uyudi anadzonzedwa zedi
@JosephEthan-l6u
@JosephEthan-l6u 2 месяца назад
Koma abusa Bible munalimvesadi ambuye akudaliseni
@dysonmakhwira2394
@dysonmakhwira2394 2 месяца назад
Kugunda kugwesa
@OweniMalokooweni-es9qx
@OweniMalokooweni-es9qx 3 месяца назад
Chinyora
@lusekeronyasulu8610
@lusekeronyasulu8610 2 месяца назад
Abusa aku 25?
@lexsonlanjesi2050
@lexsonlanjesi2050 3 месяца назад
Nde mwati ABUSA aku 25 eti???😂😂😂😂😂😂😂
@LovemoreUlayazulu-ne3id
@LovemoreUlayazulu-ne3id 2 месяца назад
Abusa a ku 49 ku nvama ccap church fumbi gheeto
@calvinmalinga1774
@calvinmalinga1774 2 месяца назад
kumalawi Kuno kulibe akazi opusa
@chiefmitengo
@chiefmitengo 3 месяца назад
Amene akunyoza Chakwera tsoka Kwa iye.uli ndi tsoka iwe onyoza munthu osalakwa, ngati ndi ulesi wakowo ongofuna kulandira go to page House khalamba yanu ikakupasani za ulele. Agalu inu
@HamanjaManyela
@HamanjaManyela 3 месяца назад
Iwe ndikape kwambiri
@SamsonshimokaSteven
@SamsonshimokaSteven 2 месяца назад
No the guy knows
@AmosPhilemon-y5e
@AmosPhilemon-y5e 3 месяца назад
Abusa ndye alalika kut amva tikunena kut zikoli timuchokeramo zikhale
@Crysis25
@Crysis25 3 месяца назад
Koma azungu akumva?
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 3 месяца назад
Aimbileni phone muwafuse
@mablemathuso3903
@mablemathuso3903 3 месяца назад
Mulibvumbulotso mu ulaliki uwu,tiyeni timvetsere bwino ndi khutu la uzimu.Ambuye apitilize kukugwiritsani ntchito abusa.
Далее
LOLLIPOP-SCHUTZ-GADGET 🍭 DAS BRAUCHST DU!
00:28
Просмотров 10 млн
CCAPYUM SERVICE
42:33
Просмотров 238 тыс.
CYCLONE FREDDY FUNDRAISING DRAMA #malawi
1:31:45
Просмотров 493 тыс.
LOLLIPOP-SCHUTZ-GADGET 🍭 DAS BRAUCHST DU!
00:28
Просмотров 10 млн