That's our beloved president, president for the poor always guided and protected by the living God, long live our president, we poor citizens loves you more, the Dddddd Cccccc!!!!, the senior pangolin 🔥🔥🔥🔥
Komano Kodi anthu osawukawo mukumawauza kuti azipangako chani kuti mu umphawimo adzachokemo. Chifukwatu kulimbana ndi BOMA sizingasinthe status ya osawukawo koma zitha kusintha status yanu. Mukalimbana nalo BOMA chonde tilimbikitseniso kuchita ma business chifukwa chete chete sautsa nyama
Men ma business wo mupangira kutiko?dZiko silikuyenda bhoo amayenera kumadzuzula kut amalawi wo azikhala pabwino...ngongole Zama business mutenga kut?Amati mukonze chapansi kut chapamwamba chikhale bhoo...
Ngati Satan simumuziwa melowere ku state house Satan amakhala kumeneko pamodzi ndi Angelo ake azikhale ng'oma ,,kunkuyu ,,,mkaka ,,Monica,,chityola ,,nick amenewa nde Angelo asatana