Тёмный

ABITI WILLIAM DAWOOD kusosombetsa NEC ya UTM...zimvere mtolo kachilungamo kalimo umu👐👐👐 

LIKI-LIKI Ladies
Подписаться 50 тыс.
Просмотров 16 тыс.
0% 0

Опубликовано:

 

28 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 82   
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 Месяц назад
Chilima was a threat, that's why panopa MCP yayamba kumasuka, u can even see kusankhidwa kwa Micheal Usi akusangalala kwambiri.
@matiasncalaila4003
@matiasncalaila4003 Месяц назад
Watching from Mozambique, ln fact Our SADC countries are in chaotic. Presidentes and ministers in SADC are different in coulors but are the one pessonal. Hospitals and Schools in their own countries always become useless when they are on top they tataly forget their background. My dear Sister , You are speaking and talking about the things that also is happening in my country. We need prayers for SADC leadership.
@NthambiInvestment
@NthambiInvestment Месяц назад
Amati nkhondo ndi anasi judas sikaliyoti anapeleka Yesu,, chilima anapelekedwa ndi omuzungulila koma ambuye salakwisa amalola zowawa zichitike kuti ukulu wake uonekele may his soul of skc Rsst in Peace
@williamdaka79
@williamdaka79 Месяц назад
Thanks good message,watching from Jeneva Switzerland 🇨🇭
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 Месяц назад
Ya mantha ndi yowona. Amalawi tapusadi kugoyakhula uva uli ndi roya. Aaaa zowona tiwope kufa Ngati alipo wamuyaya bwanji
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Месяц назад
Ine ndiye sindiopa waudindo aliyense Chakwera anapha CHILIMA
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Chakwera.Zikhale Ng'oma ndi Kunkuyu anapha Chilima.
@vivianmkwate8536
@vivianmkwate8536 Месяц назад
keep it up Abiti 👏🏾👏🏾👏🏾
@user-gd2kl1fx1q
@user-gd2kl1fx1q Месяц назад
Aunt God be with you, with ur wise words I wish ku chipan chathuchi ku takhala anthu 10 ngat inu please let's accomplish what our president started for his soul to continue resting in peace though the pain still exist bt God is all over tsogolo lowala lija litheka in jesus name
@MilikaKilion-tn1bn
@MilikaKilion-tn1bn Месяц назад
Ifa ya chilima usi alimomo asamatinamize kufupika ngati ntchimba wa nkhoswe
@nafejonga972
@nafejonga972 Месяц назад
My fellow nurse wowww😂😂😂
@nafejonga972
@nafejonga972 Месяц назад
I love you mama😢😢
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Месяц назад
Mwayankhula mama ambuye akudalitseni..
@nafejonga972
@nafejonga972 Месяц назад
I have started loving you too, am a utm member too
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 Месяц назад
It's so sad ndege kugwa mpaka the whole Day no results,
@HameedahMasambuka
@HameedahMasambuka Месяц назад
Mukhalike mama l love you ❤
@coastersRob
@coastersRob Месяц назад
Ayi muziti kudambwe airport
@AlbertDuke-of9nn
@AlbertDuke-of9nn Месяц назад
kuyakhura kwabwanji uku😂😂😂😂😂😂
@sparkdymon3429
@sparkdymon3429 Месяц назад
Ccta ulindizeru zoveka ❤
@jamesgama5489
@jamesgama5489 Месяц назад
Powerful speech
@ManyambaInnocent-x8i
@ManyambaInnocent-x8i Месяц назад
Chilungamo sichipotsa apa mkadzi wayankhula moveka
@user-ui4ux5kc8d
@user-ui4ux5kc8d Месяц назад
Chilungamo mchoti amalawi. Tiri ndimantha ndipo mantha amenewa ali ngakhale ku tsogolo komweku mmalo modzimenyera mkhondo tokha timadzifinya tokha ndithu ndiye Mai viuseni kwambiri
@user-te7xx8jg3k
@user-te7xx8jg3k Месяц назад
Tupikene awechete yakuona
@peterjoshua2595
@peterjoshua2595 Месяц назад
What a emotional ending malawi sad
@wonganikaunda
@wonganikaunda Месяц назад
More fire mum
@tarkuesamson8838
@tarkuesamson8838 Месяц назад
Amayiwa ndiosokoneza zedi ndakhala ndikwapangako follow, inu ndiena mumanyoza kwambiri kunyoza Author Mutharika munapangitsa astray Amalawi kuvotela Mcp lero ndiizi!palibe chanzeru mungatiuze inu.
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q Месяц назад
Mama.uyu amadziwa kubeleka nkowawa ndithu akudziwa kumwalira koti amadwala ndi kwina koma kumwalira kwa Chilima kunawaw
@WanangwaTauzie
@WanangwaTauzie Месяц назад
Ndakumvani mama
@Leonilde-wn4le
@Leonilde-wn4le Месяц назад
Fazem a escolha certa,no dia das eleições
@MaeCuinhane-gq7ub
@MaeCuinhane-gq7ub Месяц назад
mom ulemu wanu, mkazi olimba mtima komanso wachilungamo ambuye azikudalitsa komanso apitilize kukupatsani mzeru
@isaacchipatala1618
@isaacchipatala1618 Месяц назад
Very truly sisi
@mwaiwaobanda2691
@mwaiwaobanda2691 Месяц назад
Ine nde ndinalidi supporter wa skc ....osati wa utm...mama mwandigwira mtima ndi mau awa....ngati kuli kopuma pumani mwa Ambuye bwana skc..😭😭
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 Месяц назад
Chilima kusamva ,nanunso mungobwerera ku dpp otherwise mutha ngati makatani
@user-ee8og2mb5r
@user-ee8og2mb5r Месяц назад
Wacthing from zambia madam
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Месяц назад
Chakwela the killer 💔
@noliachelewani2208
@noliachelewani2208 Месяц назад
Kodi mamawa Ali Kuti Apapa Ali NDI nzelu kwabasi yooh
@user-zp8hv7bq3o
@user-zp8hv7bq3o Месяц назад
A chemwa muku bandula bwino, a Malawi ndife a Tulo, Mantha ndi uchitsiru. Pitirizani kutilankhulira, zikomo mayi athu.
@jameshuwanzulu
@jameshuwanzulu Месяц назад
Akunene zoona ka
@BandaSpeak-bg3ev
@BandaSpeak-bg3ev Месяц назад
Listening madam
@CorneliousKaliat-od3un
@CorneliousKaliat-od3un Месяц назад
Khani ndiyoona mama
@lame8
@lame8 Месяц назад
Komatu mavutowa anachokela iye mwini alimoyo. Ndikumatha kuona zinazake zimamjchiyikila amaopsezedwa munthu uja 😢 koma zambiri akuzidziwa miniwake. Kalindo anayesetsa kumuuza chokako chokako zinakanika. Anayankhula za mngwilizano anamuyankha popo popo a mcp kuti sakuzidziwa 😢 nanga manganya ndindani kuti asaopsezedwe muzitionela patali guys.
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Месяц назад
Nthawi yakwana yokha anthu a dyera muaone ku UTM omwe akufuna kugulitsa chipani chanu walira mwana mkazi kuchililira chipani chake cha UTM zili kwa aKaliat, Fredox a Jawala ndi ena kulandira ndalama kuchokera kwa YUDASI MANGANYA
@isaacchipatala1618
@isaacchipatala1618 Месяц назад
MCP blood
@user-ky2fs3zr8y
@user-ky2fs3zr8y Месяц назад
Manese chitedze mdala mwakongolako ku USA.ubwera liti kwaSafarao kkkkkk
@alexsumani6823
@alexsumani6823 Месяц назад
Ulemu wanu mama
@tracybennie7783
@tracybennie7783 Месяц назад
Yomweyo
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Anapha Sadik Mia kunamira covid
@user-zm9nl8zn2b
@user-zm9nl8zn2b Месяц назад
Komatu iwe nabanda iwe yaaaa
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Anthu amvere interview ya Brian Banda ndi Manganya
@Martha-m6e
@Martha-m6e Месяц назад
Zowonadi matha kutenga za chipani cha uku kupiti nazo uku. Mulungu awaranga onse.
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 Месяц назад
Eeee koma or a Patricia kaliyati akanangoganiza or kulingalira ngat iweyo mama,mmm anthu ndiye anawakonda ndipo akanaima popanda opikisana nawo,koma akuoneka kut ayamba kale kudya bans.koma nzomvesa chison anthu anali ndi hope pa mai wa,now amalawi ndiamasiye pano.ngatbndikunama tamverani speach yao yapamaliro a Lucius Banda.nokha muziyankha popanda fuso.
@WellingtonKoko
@WellingtonKoko Месяц назад
Iweyo ndi 1 😊 phasaphase
@user-mx7oj1vx3l
@user-mx7oj1vx3l Месяц назад
Every face tells a story mukawawona anthu powapatsa ma udindo,ngati wothandiza pomwe bolanso mfiti nthawi Zina ingakuwuze Kuti ndikuloza koma yawa ankawoneka ngakhale interview yawo inali pa dziwe TV two weeks back ,lilime lawo lidawonetsa Kuti mhu! ngogulitsana yawa😢😞
@wonganimoyoh2535
@wonganimoyoh2535 Месяц назад
wise saying sister
@user-rm2xv8ys1i
@user-rm2xv8ys1i Месяц назад
❤❤❤❤❤
@RobertMvina
@RobertMvina Месяц назад
Tiuzeni titani
@MakandeMpambalika
@MakandeMpambalika Месяц назад
Ndikumasulani yes go deeper mum
@ElliottBelon
@ElliottBelon Месяц назад
Mau amphamvu mama
@clocksigns9755
@clocksigns9755 Месяц назад
Nambo niwakutakata
@anthonynkhoma4265
@anthonynkhoma4265 Месяц назад
Wasowa chokamba uyu. Ngati anthu akufalitsa zabodza aziwaombera mmanja? Undunawo akanapatsa iwe ungakane?
@MakandeMpambalika
@MakandeMpambalika Месяц назад
Mmm ndiwe mzimayi wochenjera ka bandle kanga kathela pompo
@user-yk5qd6sk8e
@user-yk5qd6sk8e Месяц назад
usi akuymila kabula
@GraciamChopih
@GraciamChopih Месяц назад
Chemwali mwalankhuladi zoona zeni zeni,zonse mwalankhulazo palibe chomwe mwalakwitsapo bt chilungamo basi😂😂😂
@ritchardchakuma5725
@ritchardchakuma5725 Месяц назад
Mama Uyo gwenembe Uyu mumusiye timuwonela 2025 tasanduka zisilu Koma mufufuze kuafilika kose ndife zisilu uphawi njala kukwala kwazithu gwenembe chakwera maikousi mutayeni ndiwamisala bambo asikono mutunjasiugwila
@Leonilde-wn4le
@Leonilde-wn4le Месяц назад
Amalawi mantha achuluka kwambili,chilima wafera dziko😢
@AndrewInnocent-he8gs
@AndrewInnocent-he8gs Месяц назад
Fasefase yomweyo
@user-be1zt6xl3f
@user-be1zt6xl3f Месяц назад
Mayakhura mau abwino kwambiri sister
@TonyOkoibedi
@TonyOkoibedi Месяц назад
Mama ukukambazo ndizoona ndikukutsatila kuno Ku South Africa
@AmaliYahaya
@AmaliYahaya Месяц назад
😢😢😢😢😢
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 Месяц назад
A ccta inu muli ndi zeru kwabasi mwina pa akazi akumalawi azeru inu muli panambala yabwino. Ndege ija si imafunika anthu ena ochokera kunja kuzafufuza ayi. Even mwana wa standard one kuti afufuze za ndege ija atha kupeza kuti boma ndilolakwa vuto Malawi mantha komaso kutenga atsogoleri ngati ndi Mulungu. Pazina kumalawi tinakula molakwika. Manganya tinanena kale kuti si wa utm. Manganya ali mu cabinet ya president chilima bwana wake wasowa 10 o'clock analola bwanji kuti president awuze mutundu wa Malawi 11 o'clock usiku. Pali zimasache zina za utm zopanda zeru ife sitikufuna banja limozi kulemera ayi tikufuna Malawi aliyese aziva kukoma ccta inu mukufunika mukhale president wamalawi
@WeziKamanga
@WeziKamanga Месяц назад
Talking
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb Месяц назад
Zonsezi nchifukwa chakusanva kwa kwanu tinakuuzani ku MCP mukafako anthu aja ndi afisi .
@user-gd7xm7xr9v
@user-gd7xm7xr9v Месяц назад
Ungokhala president wa UTM ndiwe
@GeorgeLipengaphiri
@GeorgeLipengaphiri Месяц назад
Your a strong woman mama in politics
@RobertMvina
@RobertMvina Месяц назад
Too much examples
@user-un8yq1gg2i
@user-un8yq1gg2i Месяц назад
Kamkazi kokongolatu, koma eti kakuyankhuranso chichawa eti akuti fasafase Kaya ndiyekuti chiyani? Kkkkkkkkk pachilungamo chake ukunena zoona mchemwari.
@user-lg2ws2ki3d
@user-lg2ws2ki3d Месяц назад
Zaziii
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 Месяц назад
Za ziii Za ufiti,nyau?dyera magazi mmanja???
@isaacchipatala1618
@isaacchipatala1618 Месяц назад
MCP blood part
@lewisdicksonmlozi130
@lewisdicksonmlozi130 Месяц назад
Powerful speech
@SteveTebulo
@SteveTebulo Месяц назад
Tikufuna anthu olimba mtina choncho usi siwa utm limbikani mayi kulankhula tchaya tchaya
@immaculatechitsakamile252
@immaculatechitsakamile252 Месяц назад
akut anali a Ussi😢😅😅
Далее
I Took a LUNCHBAR OFF A Poster 🤯 #shorts
00:17
Просмотров 8 млн
Asad arimaheena rer hagio qabiilkooda saxda ah
6:35
Просмотров 1,2 тыс.
TAMVANI ZA IMFA YA CHILIMA IJA
10:10
Просмотров 240 тыс.