Тёмный

Chakwera Apangisa Mkulu Wina Kuzuzula Achewa 

Mukuziwa?
Подписаться 18 тыс.
Просмотров 15 тыс.
50% 1

#chilima #chakwera #news ##malawi #trending #viral

Опубликовано:

 

27 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 103   
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Месяц назад
Uku ndiye kulankhula, munthu ozindikila ameneyu. Zoona zokha zokha ❤
@IbrahimPhiri-ky5jk
@IbrahimPhiri-ky5jk Месяц назад
❤❤❤ ukuoneka nkhati unayendako pang,ono amwene mchifukwa chake mulungu akusegulako manso mulungu apitilize kukuonensa manso phenya
@kaungabondera892
@kaungabondera892 Месяц назад
That's true
@MphatsoMwale-it4xd
@MphatsoMwale-it4xd Месяц назад
Inu akulu mulungu apitilize kukuoneserani
@user-kx3en7hy5j
@user-kx3en7hy5j Месяц назад
Thanks for mentioning my Tribe Yao Watching from Meka Saudi Arabia
@BENSONRANGWANI
@BENSONRANGWANI Месяц назад
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o Месяц назад
Odhala Inu ndi oganiza bhoo
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Ine ndine Mchewa, koma Chakwera ayi.
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt Месяц назад
Iwe wayankhula zenizeni mwana reality yeniyeni
@user-mi2xf3sw1i
@user-mi2xf3sw1i Месяц назад
Umunthu uwu kumayankhula mmeene zilili
@Yungjoe786
@Yungjoe786 Месяц назад
Muyao to the world#proudlyndinemuyao
@JamesOsman-cz9cw
@JamesOsman-cz9cw Месяц назад
From south Africa
@user-fx2xw2bn4d
@user-fx2xw2bn4d Месяц назад
Chakwela bulutu la muthu kkkkk akuti tichotse katundu ameneyu waola akununkha
@AlexMthunziChimpeni
@AlexMthunziChimpeni Месяц назад
Inuyo mumayitha chilungamo chokhachokha.🎉🎉🎉🎉
@MustaphaCassim
@MustaphaCassim Месяц назад
Odala inu ndi olikonda dziko lanu komaso ndiinu munthu odzindikila ife tabadwila mu mtandile achewa amakonda tea lero sugat ndi 5000 from 500
@AmosKalembo
@AmosKalembo Месяц назад
Iweyondiozindikila kwambili mall fire
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Месяц назад
Amalawi MCP yawonongadi dzedi iiii dzomvutsa chitsoni anthu akulila pankhani chuma ndikuphatso chilima inu a MCP agalu kwabasi
@AlexManuelMisomali-sv1vn
@AlexManuelMisomali-sv1vn Месяц назад
Mdala iwe ndiwe number one komanso chitsanzo chabwino cha mtundu wako
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Месяц назад
Zoona big man
@SolomonMbewe
@SolomonMbewe Месяц назад
Achewa koma gule wamkulu basi....
@HallimaMakwinja
@HallimaMakwinja Месяц назад
Zoonadi ife ochewa mvitsirutu kkkk ulemu wanu wakulu
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe Месяц назад
Oputsa sitonse ochewaa olipo wena Openya nithu ah yayi dala mwatiyankhulila chamuna
@MikeMerecah
@MikeMerecah Месяц назад
Mwatiimirira Dara ngati mumaganiza choncho ndinumamuna weniweni,
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d Месяц назад
Ndipo mchewa ndichitsiru kwambiri mapeto
@louismagongwa
@louismagongwa Месяц назад
kkkkk kk😅😅😅 mavuto alipo ndipo sanat nanga akadzawinas kape ameneyu
@AlexManuelMisomali-sv1vn
@AlexManuelMisomali-sv1vn Месяц назад
😂😂😂 mkulu iwe achewa anzakowo akuphatu
@user-ui4ux5kc8d
@user-ui4ux5kc8d Месяц назад
Ambuye akhale nawe mdala iwe waonetsa mtima wachikondi osati anthu adyerawa akungomunamiza presedent kumaombera fiti mmanja mzothekanso presedent kukhala wabwino koma atidye nawowa akumulakwitsa mmauphungu awoo
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx Месяц назад
Ndipo chilungamo a chewa ndife zitsiru koipa timangovetsera zopusa kuti ndife a mcp basi ma gofer za zii koma osatukuka mchewa basi mangovina nyau basi tayambitsa nda chewa kusankhana kwa mbiri chitikuko mwangopanga Central Region koma a chewa sitikuona eti toll gate ikapezeka kwathu kwa chatata ndi ku mchezi
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 22 дня назад
Why am I seeing this now Sindidaonepo nchewa oganiza ngati uyu.... Ine achewa amandisowesa chonena ndithu
@user-zt7hy5lh4r
@user-zt7hy5lh4r Месяц назад
😂😂😂😂😂😂😂😂 kkkkk koma abale ai kuli zinthu 😅😅😅😅😅😅
@samchibenene4458
@samchibenene4458 Месяц назад
😂😂😂😂😂achewa dzukani wayankhuladi muchewa iwe
@MarcosDjussa
@MarcosDjussa Месяц назад
Koma amalawi akanat azinganiza ngati mndala uyu Malawi 🇲🇼tikusimbalokoma kulakhula chilungamo mulungu akuendele ukhalise
@AufiThera
@AufiThera Месяц назад
Live Bola ulamulilo uzipita Ku mpoto or kumwela not agaluwa mmmmm timwat magaz chakachino kusiya tiyi😪😪
@ChifundoChiwanda-ru3pg
@ChifundoChiwanda-ru3pg Месяц назад
Zosayenda
@IshmaelJohn-iz1ej
@IshmaelJohn-iz1ej Месяц назад
Chakwela ndi ng'ona ya munthu
@AufiThera
@AufiThera Месяц назад
Kkkkkkkkkk muchimina zonantoza pa president Aku mwera
@user-rd4ft9nd8t
@user-rd4ft9nd8t Месяц назад
GOD HAVE MERCY ON US
@bysongeorge3243
@bysongeorge3243 Месяц назад
Uyu weniweni m'Chewa kulankhula chilungamo.. MCP eni wake ndi mizwanya yoganiza bho ya ku Mpoto ya nthawi imeneyo yomwe inayambitsa chipanichi, komabe ndale zathu zinasokonera ndi azitsogoleri ndikubwera kwa matipate..dziko linagawikana patatu ndipo timavotera kuti uyu wakwathu . Zinalakwika kwambiri ndipo tinadzala mbewu yoipa ..
@BillySimkonda
@BillySimkonda Месяц назад
Kachilungamo kabwanji aka??????
@zayedmitawa8345
@zayedmitawa8345 Месяц назад
Kulankhura tchutchutchu
@JohnNdau-bl4op
@JohnNdau-bl4op Месяц назад
Kkkk
@user-bu7ut2gb7o
@user-bu7ut2gb7o Месяц назад
Iwe ndiwe mbuzi kwabasi. Utsogoleli sutengela mtundu ayi koma chikhalidwe cha umunthuyo. Iwe ndi mbunde.
@user-it5zv2nz7f
@user-it5zv2nz7f Месяц назад
Mchewa wakuzindikila uyuyu ulemu wanu
@EdisonNakulenga
@EdisonNakulenga Месяц назад
Kkkkkkkkkk
@martinnyirongo2892
@martinnyirongo2892 Месяц назад
Mchewa ntchito yake ndikuba bas, not kuyendetsa dziko ai koma amalawi ee mistake tinaipanga Kaya tiyikoza bwanji
@user-tb9ib4mu7c
@user-tb9ib4mu7c Месяц назад
Mmanyang'watu 😂😂before
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w Месяц назад
Exatly
@marryphili5419
@marryphili5419 29 дней назад
Bora pamenepo achewa ena Ali ndi zeru ndimaganiza ngati azathu simukuzuzika ndiyetu mavuto Ali posepose sure MCP yinobwera kuzawononga dziko la Malawi
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Месяц назад
Ndilo zoona muwalangize ochewa anzanuwo kuti akavote moganiza bwino bwino wa nyauyo achoke basi antu apeze mdendele
@LastenWesele-wq8jh
@LastenWesele-wq8jh Месяц назад
Izi ndizowona achewa ndi mbuzi zimafela ichi Chipani chagogo anthu
@DanielJuwawo
@DanielJuwawo 22 дня назад
Nanga choncho ochewa ozindikira zedi
@user-bu7ut2gb7o
@user-bu7ut2gb7o Месяц назад
Mawu awa ndiwodzetsa mpatuko pa mitundu ya anthu. Tiyeni tizinena za ukapolo tilimowu osati za mitunduyi. Galu iwe undinvetse
@user-kr1tf2tu7s
@user-kr1tf2tu7s Месяц назад
Kodi iwe pulezident wake uti mbuzi yamuthu iwe.akumwera kwake kuti anakupNgira chiyani
@omaligeorge4296
@omaligeorge4296 Месяц назад
Koma guys eeeh
@HanifaTabia
@HanifaTabia Месяц назад
Kkkk bola mukuziwa
@user-ke7ii6ip4s
@user-ke7ii6ip4s Месяц назад
😂😂😂😂❤❤
@rashidadan2533
@rashidadan2533 Месяц назад
Paja chakwela ndi nyau 😂😂😂
@user-ww9rj2wx8d
@user-ww9rj2wx8d Месяц назад
Zikomo poti mwazindikila nokha achewa
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili Месяц назад
Koma mchewa wanzeru ngati uyuyu sindinamuone walankhulatu wakumva wamva
@user-rf4br1fv2z
@user-rf4br1fv2z Месяц назад
Iweyo anthu aku mwela akulamulila tanena chomwe chinachitika ku lilongwe iweyo za kwanu osati zopusazo nyawu zo nvuto ndichiyani zoti amakuyuzani anthu sumadziwa kodi anthu akukugulani mala nfi anthu akut mbuzi yamuthu
@henryhenry6632
@henryhenry6632 Месяц назад
Panyini pamako iwe wava kapolo wachabe chabe
@omaligeorge4296
@omaligeorge4296 Месяц назад
Koma he is fact guys mnthuyi inu data mukutsitsayo ipindura chani kwa mnthu waku mudxi tamaganizani please
@fannyzimba149
@fannyzimba149 Месяц назад
😂😂😂😂kalikose tikanva ndi kukaona chaka chino
@alicehananiya
@alicehananiya Месяц назад
😂😂😂😂😂 katundu ameneyi achokedi
@ChristopherKabanga
@ChristopherKabanga Месяц назад
ukuyenda osavara chifukwa cha uchitsilu wakowo ukufuna chakwera akupitise kwamereka mchewa wanji galuu lwe
@user-ix7pb6hk2w
@user-ix7pb6hk2w Месяц назад
Uchisilu wake mmalo mokonza dziko akulimbana ndi activist mpa kumaononga ndalama zambili chifukwa chofunafuna anthu awili pali nzeru or okamakhala alibe manyazi or chikumbu mtima
@isaaczuze
@isaaczuze Месяц назад
Kuyankhula chilungamo uku
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb Месяц назад
Anyamata aku danbwe amenewo .
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe Месяц назад
Nakondwa nawe nzedi
@StewartGoma
@StewartGoma Месяц назад
Soon malawi will be like kenya Malawian are suffering living is so expensive
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Месяц назад
Ka mtundu kopusa!!!
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад
Ndipo live sekulan maso Achewa thaw yatha
@oscarnamirecah5386
@oscarnamirecah5386 Месяц назад
😂😂😂😂😂😂😂😅😅😅
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
Inu ndi munthu woganiza bwino kwambiri ndipo muli ndi nzeru auzeni ndithu
@TerryNac
@TerryNac Месяц назад
Chitsilu ndi chimodzi osati a chewa onse Loma chitsilu chikuoneka
@EmmanuelKaziyenda
@EmmanuelKaziyenda Месяц назад
Ukunana iwe ndekuti umangokhala manja kotsa iwe udikira za ulele ubwere kuno kumponela udzawone mmmene anthu akugulira fertilizer wa cash iweyo ndiwe chitsiru not chakwera
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Месяц назад
Ndinudi dzisilu dzokonda kupha anthu machende anu achewa😂😂
@user-tm3zh5zk4t
@user-tm3zh5zk4t Месяц назад
Iwe si chewa ayi iwe ukayelekeze ndianthu akumwela samalima ndiye apa akuwona kuti boma lapana alibe mweya
@jamesgama5489
@jamesgama5489 Месяц назад
Koma iwe nde mchewa weni weni wapa phata mchewa koma ufumu kuvina gule ndipo sazatheka kusintha
@DavidMtambo-zm8ne
@DavidMtambo-zm8ne Месяц назад
Zoona atiranga
@user-iz1qi3db2g
@user-iz1qi3db2g Месяц назад
😂😂😂
@user-rg4du4vu9r
@user-rg4du4vu9r Месяц назад
Ndizowonadi km inetu ndinkadabwa kt ku marawiko kukangot kwagwa njara achewa onse amakazaza kwathu kumpoto chaka ndicha nde kumazifusa kt kodi osayesako njira zina bwanji pot akat chakudya sikut ndi nsima yokha ayi kkkkkkk wandiwaza aise mitu izigwira ntchito osamango swana ayi achewa mwanva
@samdiverson9733
@samdiverson9733 Месяц назад
Mposo kobasi 😢
@TawongaGSMwale-cc2vm
@TawongaGSMwale-cc2vm Месяц назад
Apo mwayakhuladi Baba katundu uyu Kut alowe mu boma adalowa ndima demo kuzatulusaso katundu ameneyu pakufunikiraso pazakhale ma demo
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl Месяц назад
Ndi mbusi zachabe chabe mcp
@chitchohistorical1036
@chitchohistorical1036 Месяц назад
😂😂😂😂😂😂😂
@LidasoniManual
@LidasoniManual Месяц назад
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
Chilungamo koopsa zedi apapa ndikoyambadi ndikomaliza 2025 kwanu kwatha guys.
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
Achewa ndi athu oipa ndipo ndi athu ozikindikila achewa ndi wadziwa ndichifukwa ineyo sinamuvotele chakwela mulungu atithandize ku Malawi
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
@@user-eh1mg3ww6d Ndipo ndi anthu achabechabe, umadziwa Nyau ineee kuvotatu sindinavoterepo chipani china chilichonse kuposa DPP Ndipo family yakwathu yonse ndiife a DPP Mpakana kale Tri
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
@@user-uc1pd1tc2x koma tiphele kwambili kuti m,busa ameneu mulungu atichitile mmm ayi ndithu athu tazuzika kwambili
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h Месяц назад
Kuyanhula monga mmalawi weweni
@giftdavie240
@giftdavie240 Месяц назад
What is democracy important for if it incourages tribalism. We're the people of the same nation but we're being divided because of democracy. Someone who's brain function properly will realize that the route cause of these all sources of drama is democracy
@HassanJameskananjie
@HassanJameskananjie Месяц назад
Iwe talemba nchichewa
@MikeMerecah
@MikeMerecah Месяц назад
Or English take no fundo,
@dalitson3558
@dalitson3558 Месяц назад
Anthu ofoiladi osangolemba chichewa bwanji?
@JIMMYWATSON-ph5jg
@JIMMYWATSON-ph5jg Месяц назад
Mandenga wako iwe bulutu siwe mchewa chakwera sanakulakwire adakulakwila ndi abambo ndi amako kukhala osauka iwe galu kwa basi
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Ndiwe galu chitsilu mbuzi yamunthu choka usatinyase
@MikeMerecah
@MikeMerecah Месяц назад
Manyazi bwa ifeso ndi achewa koma munthuyi wanena zoona mpaka kuphana chifukwa Cha mipando nafe zikutiwawa,
@Aisha-db6ds
@Aisha-db6ds Месяц назад
Chakwela wationesatu zinthu
@NovassTambala
@NovassTambala Месяц назад
Koma mr mwalankhulatu ndi gonthi lamuthu chakwela mbudzi akulu hmmmm inuyo mwayedadi ndipo
@ClaudiaarmandoMafunga
@ClaudiaarmandoMafunga Месяц назад
Zoona ife achewa tili ndi vuto
@user-bu7ut2gb7o
@user-bu7ut2gb7o Месяц назад
Vuto lanji? Mukuona ngati vuto limadza kamba ka mtundu wa munthu? Musapuse gayezi ufiti wa chakwela usakhudze achewa tonseyi
Далее
Все сезоны бравл пассов…!!!😨
00:59
Smart Sigma Kid #funny #sigma #memes
00:26
Просмотров 8 млн
Пиратские котики
00:50
Просмотров 180 тыс.
Nkhanga zaona Chakwera. Mzimu wa Chilima ukwazuza
31:56
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH MICHAEL USI (MANGANYA) Part 2
58:38
Tikuferanji 08 June 2024
26:08
Просмотров 33 тыс.
Latest on African States' conference in Malawi
1:48
Просмотров 135 тыс.
Все сезоны бравл пассов…!!!😨
00:59