Тёмный

KODI OIPAYO NDI MUTHARIKA KOMASO ATUPELE KAPENA ILI NDI BODZA? 

Malawi Trends TV
Подписаться 41 тыс.
Просмотров 8 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

7 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 91   
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
Musalimbane ndi peter komanso Atupele ...pakampeni paja amaneneratu poyera kut MUSAVOTERE MCP ...nde anthu sanamve akut umafuna change...This is the change..the change can be positive or negative....asiyeni a MCP alamulire chifukwa ndie zimene munavotera...tichimine kaye a malawi...Pena Mulungu amapanga zoti anthu aphunzire kwambiri
@user-rp9wy6rd1q
@user-rp9wy6rd1q Месяц назад
Zoonad anthu amageya mwano kwambiri akuti tisithe zithu ndie zasithaditu
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
Koma boss ndiiwe ozindikira koopsa keep it up, mavutowa tinachita kubwelesa tokha. Anatiuza ndipo anatilangiza koma kusanva ndipo ananena Peter Muntharika kuti mukupanga inuzi akubwerawo muona Nyekhwe. Lero ndiizi kaaah
@macrinenduna1024
@macrinenduna1024 Месяц назад
Good comment. Truly these two Gentlemen are real country men.
@JohnAsendi
@JohnAsendi Месяц назад
Zikomo amwene papani Mr pita ndi Tupele muzitikhululukila zoona vuto ndi ife ndithu🙏🙏🙏🙏🙏
@MonicaSteve-t5p
@MonicaSteve-t5p Месяц назад
Good correction sir ❤❤
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i Месяц назад
Zoona brother uyu walankhura odiyo iyi ndi mbudzi ya Mano kunsi, ndipo samadziwa chomwe amanena. I love you u ndipo mau anga mwandinenera ndinu❤❤
@user-ou9jz8pr4m
@user-ou9jz8pr4m Месяц назад
More fire mr D takunyadilani kwambiri mwalankhulabwino
@Freedomchennl47
@Freedomchennl47 Месяц назад
Kmaso number one ozikonda ndameneo akuyakhulayo waku mangochiyo ndamene ali adyela
@LeonardChinomba
@LeonardChinomba Месяц назад
Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi
@PetroMatias
@PetroMatias Месяц назад
Ase wayankhura bwino mmanja mwako 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🤝🤝🤝🤝🤝🤝
@JohnJohn-og8rt
@JohnJohn-og8rt Месяц назад
Ameen Iweyo mulungu akudalisene moyo ukuyangula zabwino mau amuna asitero amavuna dala athuwo
@HezekiahItz
@HezekiahItz Месяц назад
Zoona kuyankhur mosacheuka bwana komaso chilungamo anthuwa tithanenao tokha Peter and atupele asiyeni ananyozedwa ngat alibe mitu ngat alibe uzimu asiyen imfa ya saulosi chilima yaripweteka Ndye mikono yanthu tikutsamir kwa a2 awawa Ndye njara ikatikhaulitsa ndipamene tingapite pa mseu
@FisherAction
@FisherAction Месяц назад
Ndiye ngati akutero kut samatengapo gawo nkwabwino asayime asiye omwe angamathandizire kumamenyanawo nkhondo bcz we are in democracy no words kupembezana
@MaggieCement
@MaggieCement Месяц назад
Ndipo Muthu ndiobvuta ndithu tinya ndizomwe tinkafuna ngati ana akhanda oti nkhongelesiyo yabwela lero hahahahaha
@user-vn3ty1yg9l
@user-vn3ty1yg9l Месяц назад
Moti inu mwavotelaso mavuto aaaa zikozeni nokha kumeneko Peter atupele siwolakwa
@LovemoreSalima
@LovemoreSalima Месяц назад
Thanks D phiri Auzeni ana amahurewa, Ndiomwe atifikitsa pa manyiwa. Bu shit, anthu amanyi amenewa. Azimuloza Chala ntambo.
@EdsonKamwendo
@EdsonKamwendo Месяц назад
Mai woputsa iwe umafuna azingoyenda wamba iweyo siukuziwa kuti mcp ili ndi chiwembu chachikulu kodi mcp yakutuma ? Ugaluwako
@user-bq8gb7tb1l
@user-bq8gb7tb1l Месяц назад
D.phiri wanena zoona,,,ife tinalakwisa
@chifundocharles2348
@chifundocharles2348 Месяц назад
This is true boss,, atupere or munthalika asiyeni mavutowa ndiifeyo amalawi kusamva lero ndi izi
@mozesaine6677
@mozesaine6677 Месяц назад
Pure answer
@MrsNankhumwa
@MrsNankhumwa Месяц назад
Ndipo APM anatiuza kut mukavotera MCP muzalira, lero nzimenezi munkafuna anyamata paja, ulemu wanu akulu mwayankhula bwino kwabas,
@shazirahJafali
@shazirahJafali Месяц назад
Izi nde ndizoonad osapanga complain pa anthu awa ayi vuto ndamene anachotsa dpp kukavotela mcp
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Akulu inu mulibe zelu ndipo zomwe mukunenazo chipani cha dpp udf ngati akhala ndimaganizo akowo basi dpp yapita sizalowaso boma ndiwe chisilu basi dpp ndaituluka kuli zitsilu ndichifukwa chake mukongoluza zisakho shupit
@JuuuKomba
@JuuuKomba Месяц назад
Ndipo Apm ndi atupele 2025 anatisiya tikhaule tinapanga chipongwe tokha
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Peter wakalamba sangathamange osazemba ai ndipotu inuyo mukakakamila peter ndiye zolowa boma iwalani ndithu
@IshumaerWazakile-u5d
@IshumaerWazakile-u5d Месяц назад
Chachikulu ife amalawi sitikufuna kukhutitsi pazimene Dr piter amatipangira ndiye anthu athira kuwiri
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Mcp 2025 boma cadet akhaula ndipo iwe cadet ukanalila musobva😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅
@IsaacMusa-py2jm
@IsaacMusa-py2jm Месяц назад
Powerful 👊
@AlliSaiti
@AlliSaiti Месяц назад
Uku nde kuyakhura mopanda nzeru😅😅😅😅😅😅 kod adpp abalalika eti
@user-jc5tf8jl1m
@user-jc5tf8jl1m Месяц назад
Musiyeni uyo wadya banzi walandila ndalama.Mangochi singavotele mcp ai
@FisherAction
@FisherAction Месяц назад
Ayi ndizakale zomwezija ndikwabwino azilankhulapo asakhale zii
@zaidimussa
@zaidimussa Месяц назад
Muiyu afuna kukoza mbili yachakwela kodi Apm sadanene kuti mudzaona nyenkhwe atupele ndi apm sindikuwapeza ndi mulandu ovulala ife bandi akamange atupele ndi apm ndizoona
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt Месяц назад
Good correction
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw Месяц назад
Mr phiri .mwandizizilitsa mtima mwarankhura bwino kwambiri.nditamva vn yonyodza ija ineyo mtima unawawa
@HassanMbalaka-gb5sv
@HassanMbalaka-gb5sv Месяц назад
Sitinva ife Anthony awa Antananarivo don't vote ❎ theme ife makan
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Mungobvutika boma ndilomweli ndipo sitikusintha apa mungotaya nthawi kulongolola palibe chomwe mungachite
@ShearstonNyirenda
@ShearstonNyirenda Месяц назад
Kagwileni ntchito mupeza nalondalama boma lachakwera koma mulesi alipamavuto
@user-el8to1te3l
@user-el8to1te3l Месяц назад
Wa mcp ameneyo akufuna kut a peter ndi atupele atuluke akawaphe a mcp wabunya
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Alomwe muli patchito chakwela ndukuzani pano simungamuchotse mulakhula mutopa chitsazo ma by election mukungoluza daily
@user-qk2hw4ex3c
@user-qk2hw4ex3c Месяц назад
Peter amapanga kampeni
@lutfieabrahams1465
@lutfieabrahams1465 Месяц назад
Ndpo zoona bro mwayankhula bwino
@user-lk8kj9zv6x
@user-lk8kj9zv6x Месяц назад
Bodza len leni ifetu sitikupanga complain chifukwa chilungamo tikuchidziwa inu izi mukuzitenga kut
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Tsono mukuona ngati mcp ingachoke boma ndi kutukwana kwa ma akitivisinu anthu muli ndichibwana kwabwasi tiye nazoni mukhala ku kotsutsa konko
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
Iwe usabvutike anthu sangabvoteleso dpp kulibe ndipo ndukuuza pano dpp sizabwelelasi boma pezani zina zochita izi mutayanazo nthawi
@MalungaSteven-i2o
@MalungaSteven-i2o Месяц назад
Mau akulu akoma akagonela
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Месяц назад
Kusankha kwanu a Malawi , muziwona konko. Iwowo analemela kale awa ,mabvuto ndife
@LindaMakalani
@LindaMakalani Месяц назад
Chisilu ndamene anavotela mcp yo ine ndinavotela my lovely dad Mr p ndiposo pano it's my vote no matter wat
@CassimMbalaka
@CassimMbalaka Месяц назад
Walandira ndarama za mcp amenyo
@francebanda-du9yk
@francebanda-du9yk Месяц назад
Zonadi. Zimenez O
@Mahamudu-q6b
@Mahamudu-q6b Месяц назад
❤❤❤
@user-qk2hw4ex3c
@user-qk2hw4ex3c Месяц назад
Choka ukuyankha zosaveka azako akuti kampeni osati zimene mukuyankha ndizina zimene akunena aazanu ndi kampeni
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q Месяц назад
Ndare za nepotism ku Malawi we need federal system of government otherwise no change to people that's why Malawi is the poorest country in the world.
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Месяц назад
Malawi ngakhale wuyifele ,aaa ,chilima anapita ,nkhani yake kufera Malawi . Malawi si woufela
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o Месяц назад
Peter muthalika ndi nkhalamba munthu oti akuziyipitsira yekha pomwe akhala angapange kampen
@HUMPHREYBALANGWE
@HUMPHREYBALANGWE Месяц назад
Tiyeni tingoyang'ana kutsogolo Munthu amadikira chopereka church kuti akhale ndi ndalama ndie mumaganiza kuti angalamulire dziko Lero ndi izi dziko latsala masanza okhaokha
@YusufuUsumani
@YusufuUsumani Месяц назад
Chakwela ndi wamizala wamanyi
@MustapherLino
@MustapherLino Месяц назад
Zoona man, mai awa ndi hule wachabe
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
Sanayankhule di bwino bambo amene aja Peter ndi atupere komanso former president Bakili Muluzi anayankhula po za mcp koma anthu kusambva lero ndi izi nde akamayankhula aziyamba aganuza kaye osamangobwebwetuka
@SellinaSanena
@SellinaSanena Месяц назад
Kusamva kwathu. Don't put the blame on Peter and Atupele. Tinavota tokha
@MarthaMbewe-uk5nn
@MarthaMbewe-uk5nn Месяц назад
Iyeyo akuona ngati a opposition angokhala? A Peter ndi atupele TU siopusa akumuwelenga kaye chakwela yu AKUFUNA amlize kaye uchitsiru wakewo kenako adzuke koditu campaign sinayambe kukhala zinthu a opposition mukuwanyozawo simuwafuna
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
Tinalakwisa tinavotela ena ndiyekuti tisadzudzule? Usanena kuti musakonze ayi ,,wa Aodio sanalakwise,,,tisawagwadile Oro kuwachonderela,,Iwo nde azamwe mkaka,,
@GiftJulius-ro9ev
@GiftJulius-ro9ev Месяц назад
Choka mboliyako...mkamwa mopindikamo...
@VarietyNkhata
@VarietyNkhata Месяц назад
Kma iwe ngati ndiwe mukazi ndiwe hule wangoifuna Boro yaminthuyo asa😊
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
Ulemu wanu guys mwayakhula bwino kwambili mulungu adzikhala nanu thawi zose onyazao asiyeni azinyoza amachita kutumidwa ndi chakwela kuti adzisusa athu akayakhula chilungamo chachikulu tiyeni tiike zise m, manja mwa chauta akuva kulila kwathu chakwela akadapanda kulamulila dzikoli mukanakhala khondo yoopsa kwambili koma mulungu adalola kuti kutelo kuti ukulu wake uonekele 🙏🙏
@EsnartMartin
@EsnartMartin Месяц назад
Amene uja machende ake ndipo ozikonda ndi iye uja ndi chakwera wakeyo
@ChiefJustin-cl8jl
@ChiefJustin-cl8jl Месяц назад
Ndi mbuzi imeneyo mutharika ndi atupele ndi sogolo la dziko lamalawi
@ThulaniPrince
@ThulaniPrince Месяц назад
Koma amalawi tilindimavito, chonyasa chija chayamba kuoneka chabwino kkkkk akangolowa adadi. Muzayambe kunenaso kuti bora chakwera
@SlindiryLoveness
@SlindiryLoveness Месяц назад
Tinawakana amapha ma albino amenewo asiye akalamba panopa sitikumvako kuti agwira ziwaro za anthu boma la peter linalibe security ndiposo wakalamba wapume zina mumangonama mulizambiri mu malawi panopa tikuwona zachilendo kale kunalibe ngati ndikukwera kwazinthu si malawi yekha ife tikufuna chitukuko basi zimene mukulankhurazo sizikumveka bora chakwera ndi anthu anuwo
@MohammedAriesa-j4x
@MohammedAriesa-j4x Месяц назад
Opusa
@LovemoreSalima
@LovemoreSalima Месяц назад
Gulu la mahure opanda mzeru ndimanena aja ndi m'modzi mwaiwo ndiweyo. Hule
@AlexManuelMisomali-sv1vn
@AlexManuelMisomali-sv1vn Месяц назад
Ndi munthu opepera iyeyo ngati wapatsidwa ndalama azingodya
@StellaCharles-dq8db
@StellaCharles-dq8db Месяц назад
Amai amene aja atumidwa inu satipusise ife eetu ndpo alikomweko kwachakwerako
@shazirahJafali
@shazirahJafali Месяц назад
Kma ndiye akuchita kuonekadi kuti awapatsa kenakake chifukwa nde akulubwalubwatu
@MaikNkhoma
@MaikNkhoma Месяц назад
Ndiwekape munya 2025 bomasitokusintha
@patassonelucaszovuta3431
@patassonelucaszovuta3431 Месяц назад
Ndie ngati ali ndi mantha asiye ndale kuti akhale moyo wautali umene akuufunao
@user-pv2xx3lu8b
@user-pv2xx3lu8b Месяц назад
Watiyakhulila mwene
@user-ev6bi7jr7g
@user-ev6bi7jr7g Месяц назад
Mwayankhula bwino kwambiri
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 Месяц назад
Zoona Peter atupele si ozikonda vuto ndife amalawi ovota mitu inawuma mtanyiwa kalindo bakili TV Peter atupere ndi ena ofunila Malawi zabwino alankhula za mcp koma sitinave. Panopa mukuona mcp ikugwirisa ngongole and ikugawa ndala and amalawi tawona mumene wafera chilima ndi abale athu koma still tikusapota bomalo amalawi tili ndivuto loganiza bwino. Munthu kuti mumuziwe kuti zeru alibe boma kuyakhula mwamatama kuzikona kupereka ndalama kuti anthu amuvotere
@yotamumahomed1313
@yotamumahomed1313 Месяц назад
Komanso umuuze kut watikwana
@user-lw4hw9ce4w
@user-lw4hw9ce4w Месяц назад
Muuze chimbuzi chimenechi mmesa amakuuzani kusamva kwani
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
Ndipo big amai amenewa ndi chimbuzidi zedi Amai opanda nzeru
@yassinn5634
@yassinn5634 Месяц назад
Zaka 84 angathamange.? Anthu osazindikira inu Peter akanangotuluka tsiku limodzi mukuganiza khansala wa DPP akanaluza? Tulo basi
@user-jb5yb9wq3y
@user-jb5yb9wq3y Месяц назад
Nzeru ulibe
@yassinn5634
@yassinn5634 Месяц назад
Iwe ukuyankhulawe ndi Peter muthalika kapena Atupele akupatsa chani chitsiru iwe kagwade wekha kupepera eti kuzolowera kunyambita nsapato .Khala pansi asiyire anthu ozindikira aziyankhula. IWE SINNENERI WA ANTHU AWIRIWA
@yassinn5634
@yassinn5634 Месяц назад
Asiye ayankhe okha
@KestonNGUBO
@KestonNGUBO Месяц назад
A dpp mbuzi yagalu iwe ukuyakha
@JackMvura-ik2td
@JackMvura-ik2td Месяц назад
Tsono iwe wadya banzi ya pitala munthu wadyewa uku one kuziro 2025 mukunya chakwera bomaaa iwe mulomwe mwachepa achewa ndayao atumbuka simuwatha komaso ozindikila alomwe ena Asari Ngati iwe samuvotera pitila DPP yatha Palibe akuifuna tanganizani Mangochi zikumvekanso Kuti mwina pitala akhoza Ku votela chakwera😂😂😂😂😂😂
@LeonardChinomba
@LeonardChinomba Месяц назад
Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi
@LovemoreSalima
@LovemoreSalima Месяц назад
Inutu ndiye munyee, mukhaule agaluu Inu.
Далее
Bike Challenge
00:20
Просмотров 17 млн
BON KALINDO KUNG'ALULA MWA NYOO!! 5 September 2024
43:54
BON KALINDO WABWERANSO NDIIZI TAMVERANI 05/09/2024
16:42
THE  COURT (Malawi)
24:40
Просмотров 53 тыс.
KUYANKHULA KWA JOYCE BANDA
21:25
Просмотров 19 тыс.
Interview ndi Norman Chisale
1:05:22
Просмотров 240 тыс.
Bike Challenge
00:20
Просмотров 17 млн