Тёмный
No video :(

MCP yatengesedwa ndi nyamata wa ku Ntheu. Chakwera alibe mtendere wamtima 

Jay Kawere TV
Подписаться 19 тыс.
Просмотров 26 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

5 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 146   
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana Месяц назад
Zoona zake Zenizeni koma osadera nkhawa chaka chamawa kuvuta am from Ntcheu kwataine village koma mlungu adzatiyakha osaopa osafooka osatopa❤
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 Месяц назад
@@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba
@FrankSimfukwe-w1s
@FrankSimfukwe-w1s Месяц назад
Ndipo sitikuopa izisitikungokamba chabe km sitikuopa ife tikufuna chilima wathu chomuphela ndichani atiuze chomwe anawalakwila iwowo
@austenbushiri-cx1kh
@austenbushiri-cx1kh Месяц назад
Mawu! mawu! 🎉 big man
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
Amalawi tonse timadziwa kut Chakwera anapha chilima mosogozedwa ndi Michael usi
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 Месяц назад
@@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
@@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe Chikhulupiliro sagula Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu Mark 14:48 (Yesu sanamugwire ) Mark 15:21 (Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo) Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka
@EdwinHowardmkandawire
@EdwinHowardmkandawire Месяц назад
Iweso kapolo ndege ija ankayendesa ndi chakwera?
@EdwinHowardmkandawire
@EdwinHowardmkandawire Месяц назад
​@@yowasschitsosa5348kuswa zonene anthuwa
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
@@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools
@rashidadan2533
@rashidadan2533 Месяц назад
Komanso kufatsakwina ndikopweteketsa , Kufatsakwina ndikopusanako , Amalawi ndife anthu ofatsa mopusa
@VeronicaChirwa-ct4os
@VeronicaChirwa-ct4os Месяц назад
Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole Месяц назад
100%facts brother mcp ndi zigawenga mbiri safuta lero taziona yalembedwaso ina apa.
@PIYASSFKGCHIWAYA
@PIYASSFKGCHIWAYA Месяц назад
Ulemu wanu brother
@MeriaMasinga
@MeriaMasinga Месяц назад
Olo Monica akuziwa kt amunanga apha chilima
@AdamYas-ec9oc
@AdamYas-ec9oc Месяц назад
Mukunena dzona brather m c p kwake kuba ndi kupha
@AjibuTwalibu
@AjibuTwalibu Месяц назад
Mmmm man mwalankhura zoona ok
@bamusmajawa1619
@bamusmajawa1619 Месяц назад
Iye uja mpaka azafa akuzuzika
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 Месяц назад
@@bamusmajawa1619 munamatu simulungu ameneo and palibe munthu ali ndi mphavu yotembelera mzake,
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Месяц назад
Bg ulemu wanuw mulungu adalise inuyyo nkwamasinku osse tiutseni soona sandege bg mn ashankwela angompedwa nawosso sikut wawaw kobas skc anashita nkumupha ndi ashankwela yemwyyo mfiti yyamundu😮😢
@Martha-m6e
@Martha-m6e Месяц назад
Ndipo zowonadi zake. Ulemu umasowa.
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona Месяц назад
Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi
@hamiltonsolomon3756
@hamiltonsolomon3756 Месяц назад
Brother More Fire 🔥....Auza Amenewo....Nthawi zonse chilungamo chimamphweteka muona mufa nd ma BP. MCP yakumpha
@user-yv3jp3it2t
@user-yv3jp3it2t Месяц назад
Osaopa man chakwela anapha chilima sibodzatso ayi
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl Месяц назад
Mau amenewo mulungu akudalisa mcp ndi yakupha auzeni ndi mbusi za anthu awa
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Месяц назад
Komaso kuyakhula chilungamo MCP sikanawina kapanda chilima olo akamayakhula mwamatama akhala dzaka zingati osawina
@RafiqueChibwana
@RafiqueChibwana Месяц назад
Inuyo mwalankhuladiii boss ulemu wanu
@mollymasangano473
@mollymasangano473 Месяц назад
Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Месяц назад
Osatopa osafooka osawopa 💪💪💪 chakwera machende Ako aise
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e Месяц назад
Kuyakhula kwachilungamo chakwera anapha chilima
@StevoZimba
@StevoZimba Месяц назад
Wa Bakili Muluzi VT amanena zoona😊
@WilliamLimwalwo
@WilliamLimwalwo Месяц назад
Zoonadi dzake, more fire,the truth will prevail 😂😂😂😂😂😂.
@JowasiMasina-fy8ji
@JowasiMasina-fy8ji Месяц назад
Ndi chipani chakupha chimenecho Cha MCP ndikukuba ndiye chitukuko chawo cha MCP basi
@Lingstone-r3z
@Lingstone-r3z Месяц назад
To stand on the bright side with truth and faith for all Malawian ❤
@peterlowole7841
@peterlowole7841 Месяц назад
Malawi ife ndife amantha ausilu , big mwalankhula ngamo Amen
@KaungaYawaka
@KaungaYawaka Месяц назад
Chakwera ndiwakupha vuto anzathu achewa kuberekana nde chimene chikumlimbisani mtima mumadya naye
@AchinaKellz
@AchinaKellz Месяц назад
mcp tidakwilira limodzi ndi chilima zimu uwakwatha Wina ayelekeze kuyimila ku ntcheu mcp timpha timuyatsira nyumba osatiseweletsa😢
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 Месяц назад
Zoona mcpbinapha chilima zoona chakwera akuziwa ndipo ife ku mwera tizailowerela amaona ngati amalawi ndiopusa
@ChisomoMsiska-oi2vg
@ChisomoMsiska-oi2vg Месяц назад
Koma nkulu uyu wayankhula za nzeru kwambiri
@user-cn3gi2vf5n
@user-cn3gi2vf5n Месяц назад
Catholic bishops are very sharp amaima pa chilungamo Mcp ndi yokupha
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 Месяц назад
Auze aise,
@ElphinaChirwa-qk3cy
@ElphinaChirwa-qk3cy Месяц назад
Straight talk eeeee anthu munatipweteka kwabasi imfa iyiyiyi Ndipo mabala akupweteka
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v Месяц назад
Chilungamo aise Chakwera ndiyemwe anapha Chilima chifukwa cha udindo
@MrBone-zj1wq
@MrBone-zj1wq Месяц назад
Zitsiru zimenezo zimene zikuti zalowawa ndale,mbole zawo kwambiri
@corretabanda7685
@corretabanda7685 Месяц назад
Walankhula bwino brother
@user-wl4nd7ic1s
@user-wl4nd7ic1s Месяц назад
Kwambliii Mr your talking the truethhh
@user-gg9hw4oj2v
@user-gg9hw4oj2v Месяц назад
Zoona chakwera anamupha chilima
@marthansaliwa7732
@marthansaliwa7732 Месяц назад
Zoona zokhazoka ndithu. Mulungu Ali pampando
@JumaJuma-i9t
@JumaJuma-i9t Месяц назад
Ndipo kumeneko ndiye kuyankhula
@UsenLashid
@UsenLashid Месяц назад
Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi
@user-vu4cz1mt4f
@user-vu4cz1mt4f Месяц назад
Chakwera wakupha tonse tikuzwa
@lysonkaselema7321
@lysonkaselema7321 Месяц назад
Ntcheu ndimaiziwa ndiimeneyi
@SandlessWakhuluma-ns1io
@SandlessWakhuluma-ns1io Месяц назад
Mau ndiwo mweo ayakhula munthu.
@LouisAndrew-jr1yj
@LouisAndrew-jr1yj Месяц назад
Ukavomereza kuti Yesu ndi Ambuye, udzapulumuka🙏🙏
@user-my4gr1pv8h
@user-my4gr1pv8h Месяц назад
Tizamusinja amweneo big ngamo
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Месяц назад
Chakwela achoke and ngati Pali munthu woti akuyenela kumangidwa ndi chakwela ndi nduna zake
@user-gr5zt6kw3s
@user-gr5zt6kw3s Месяц назад
Well said bro
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Месяц назад
Chakwera Mutu Ngati machende amkango
@FrankSimfukwe-w1s
@FrankSimfukwe-w1s Месяц назад
Kkkkkkkkkk km
@BlessingsTembenu
@BlessingsTembenu Месяц назад
Zoona bro,ndipo anthu awawa ndi oyipa ndiposo ineyo amandinyasa heavy ndipo moyo wanga sindifuna kumawona,ndimava kuphweteka ndipo ineyo ndikanakha nfiti tikanaphweteka ndithu
@OwamiSimeon
@OwamiSimeon Месяц назад
😂😂😂😂 amati wina ludo kkkkkkk😅😅😅😅
@KhonzoBlose-wq7zm
@KhonzoBlose-wq7zm Месяц назад
Mau amphavu bro MCP ndiyakupha idapha anthu ambiri
@user-xt2gu9yt9q
@user-xt2gu9yt9q Месяц назад
Mawu oveka chakwela dzelu alive mamuna ndi wabakili muluzi tv ameneuja amaganiza hsve
@CHIWSABINYAMBOSE
@CHIWSABINYAMBOSE Месяц назад
Kunoso ku mzimba ndife okwiya kwambiri
@ErnestChansa
@ErnestChansa Месяц назад
Sindinu nokha akuntchewu ai even boma lakhotakota ndife okwita big pafupi ziko lose nyani chakwela mbuzi akupha
@misoMoyo
@misoMoyo Месяц назад
Sindikuona chifukwa chopangidwira remove nkhani aliense akuona yekha Mene zinaendera Kodi chilungamo mukufuna chotani kuchita kuoneka zokha kuti anamupha mukufunanso chani Chakwera ngoipa anatiphera mngoni wathu Rip skc
@Patricklichakala
@Patricklichakala Месяц назад
Thanksyou big
@MarcosDjussa
@MarcosDjussa Месяц назад
Zoonad brother umakwana
@JosephChikabadwa
@JosephChikabadwa Месяц назад
Ngakhale Mulungu Kumwambako akuwona Lingatalike bwanji Tsiku Lina Oyipayo Adzagonja Ndithu Mulungu Wathu Ndiwam'kulu Ali ndi NTHAWI YAKEEE AYANKHA M'mapemphero Athu
@LinesiKanzota-fw7sj
@LinesiKanzota-fw7sj Месяц назад
Zowonadi ndi zowawadi chakwera ndi Muthu oyipa
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Месяц назад
Well spoken my brother ❤❤❤
@AliceChipeta-pc3nb
@AliceChipeta-pc3nb Месяц назад
Chilungamo chimawawa
@ElizabethMajiga
@ElizabethMajiga Месяц назад
Ndimwana yemwe akuziwa kuti chakwela anampha VP wake basi
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v Месяц назад
Zoona big palibenso munthu oganiza bwino angazavotere Chikangawa mcp anthu panopa ndiokwiya
@EdwinHowardmkandawire
@EdwinHowardmkandawire Месяц назад
Inuyo chikhala mmaziwa kusaka ndege munkalekelanji kupita kusaka ndege a kapolo a anthu
@kondwamlungu8384
@kondwamlungu8384 Месяц назад
Ukuteta yayi àuze zowona
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад
Ndipo live zoona zake tikuziwa bwino lomwe
@ErnestChansa
@ErnestChansa Месяц назад
Zowona sikunama ai mcp ndi akupha anthu zisiru za mcp mafiti
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 Месяц назад
Usawope muphwanga chilungamo chake nchakuti chilima anachita kupha a mcp ndichakwera
@EdwinHowardmkandawire
@EdwinHowardmkandawire Месяц назад
Fotseki chikwera sangasowe ntendele ndipo mutaya nthawi
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Tiphe zinyau zinayi kuti tibwenze zomwe chipani cha nyau chimachita.
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i Месяц назад
Mwakhwana brother uko ndiko kukamba
@LilianMbaisa
@LilianMbaisa Месяц назад
Ndipo asabweredi
@TimexKaufa
@TimexKaufa 27 дней назад
Chilima adakwera mundenge ndi dzigawenga ndi chifukwa a mcp adakana kukweranao
@FrankSimfukwe-w1s
@FrankSimfukwe-w1s Месяц назад
Ife tikudziwa bwino kt anapha chilima
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc Месяц назад
Ndukugwirizana nazo mbale zoonadi zimenezo mcp chipani chongokhalira kupha
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Месяц назад
Fire
@user-ld8gb9xm7v
@user-ld8gb9xm7v Месяц назад
Thanks brother
@MaritaBanda-p4z
@MaritaBanda-p4z Месяц назад
amenewa akufunika azasinjidwe kumene komas kunena zona palibe wa mcp angapite ku ntcheu azikalakhula mbwelera
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe Месяц назад
Palibe zandale apa Koma choonadi
@isaaczuze
@isaaczuze Месяц назад
Chakwera ndi munthu yemwe anapha chilima ....kuyipa mtima
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt Месяц назад
Ulemu waanu brother. Osawanyengelela a MCP ndi makape opanda ntchito.
@SimeonAbraham-u2j
@SimeonAbraham-u2j Месяц назад
Lero mutenthedwa ndi message yoti inaperekedwa kale kale mukanakhala ozindikila a MCP bwenzi siku lomwe uthengawu inaperekedwa mutaumva
@patassonelucaszovuta3431
@patassonelucaszovuta3431 Месяц назад
Koma olo zitalowa ndale palibe vuto chifukwa anthu adafawa ndi andale ndie sindikuona vuto
@RitaKainga
@RitaKainga Месяц назад
Komanso ndege inagwera poyeratu eehh
@UsenLashid
@UsenLashid Месяц назад
Zaphabvu brother
@Marymahendra
@Marymahendra Месяц назад
That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .
@chipiesato-ut7hx
@chipiesato-ut7hx Месяц назад
Osaopa osatopa osafooka mcp yakupha ndizoona
@user-ec4jo9cu4d
@user-ec4jo9cu4d Месяц назад
Izi nde zoona ine okhara mchewa km imfa iyi yokha idandipweteka😭😭😭😭💔💔💔
@spargomw
@spargomw Месяц назад
😭😭😭😭😭😭😭
@user-ww9rj2wx8d
@user-ww9rj2wx8d Месяц назад
Zowonadi brother
@AndrewMagombo
@AndrewMagombo Месяц назад
Zoona anthu a mcp okumpha
@AlexPhiri-in1re
@AlexPhiri-in1re Месяц назад
Zoona bro
@moseskapelekeza8849
@moseskapelekeza8849 Месяц назад
Kodi muli joz
@ELLENKANJERE
@ELLENKANJERE Месяц назад
Zimawawa kwambiri ighowa ngati anali amai ake or achimwene mhu akhoza kumva motani akaona muthu akangwa pamseu anthu mosachendwa akufika pamalo ngati anali pafupi koma mmmm za chisoni
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko Месяц назад
Mudzayese ngat inuso elazi mudzayipomde
@shadreckphiri1799
@shadreckphiri1799 Месяц назад
This is the truth
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
Auzeni chilungamo afitiwo
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e Месяц назад
Asakuopyeze mchimwene auzeni chilungamo
@CorneliusSande
@CorneliusSande Месяц назад
Eeeee koma Mulungu yekha adzamenya nkhondo
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
Chizaone chipande powomola
Далее
BON KALINDO WABWERANSO NDIIZI TAMVERANI 05/09/2024
16:42
ПРИКОЛЫ НАД БРАТОМ #shorts
00:23
Просмотров 562 тыс.
NKHANI ZALERO KU TIMES 4 September 2024
19:35
Просмотров 17 тыс.
Zathu Band - Zimatere Zimatere (Chichewa) HD
7:06
Просмотров 127 тыс.
GWEDEGWEDE LERO PA 5 SEPTEMBER  2024 |
30:28
Просмотров 6 тыс.
A MOSES KUNKUYU KU PROGRAM YA KULINJI
39:13
Просмотров 17 тыс.
ACHAKWERA KU DOWA PA MTENGO WANTHENGA 🤔🤔🤔
17:04
ПРИКОЛЫ НАД БРАТОМ #shorts
00:23
Просмотров 562 тыс.