A person who has gone to school should be seen with his/her actions en fruitful.we salute for you chief.stay blessed with your wisdom so that we too can be blessed ❤
Thank you brother mwatisegula mutu. Only thing I discovered kumalawi Kuno kuli anthu a nzeru ndithu koma sapasidwa mpata muzotukula ziko chifukwa cha anthu andale. But this is powerful message thank you again brother
Thanks Mr we respect you and we just wanna give you respect about what you have said, you didn't just go to school without a reason. You speak truly congratulations Mr.
Mwayankhula modekha ndi motambasula simunagamule mwangotiunikira nkhani yachitikayi ikufanana kwambiri ndi zomwe zimachitika ku Mwanza munthawi ya ulamuliro wa kamuzu kumene kunafa anthu anai a Gadama a Sangala a Matenje komanso a Chimanga ananamizira ngozi ya galimoto lero anamizira ndege eish!!!!
Mcp imapha, ndi yadyera pa mphamvu za boma, ndi ya nkhanza kumbali ya ndale. Anapha anthu amene aja ndi mcp, mzimu wokupha sunawachokere, they are all murderers. Mcp yomweyo yaphanso vice president eeeeh