kodi athu amenewa akuyakhulawa ndi akuti,,, koma pano ali kutiko pano anthu amenewa?????????????????????? may almighty true living GOD FORGIVE THEM JUST BECAUSE OF THEIR SPEECH
Anthu awa ndiye ndi abodza enieni komanso abodza Eni Eni.Abakili munkawanyoza aja ndi amene anatimvetsa kukoma kukoma dziko lathu la Malawi.inu agalu mukupanga chani chiyambireni cha boma lanu
Atupele Ali ndi experience than them u can see they're destroying our country instead of kuli kwedza dzikoli. Atupele anali Nduna Koma sanabe what if atakhala president obvious sangabe