Тёмный

Times Exclusive..A Nicholas Dausi kuwakana a APM as 2025 presidential Candidate 

Malawi Lovers 🇲🇼
Подписаться 23 тыс.
Просмотров 69 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

7 июл 2023

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 200   
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Год назад
Brian akuluwotu abwera ndi nfundo zosanveka Chifuwa akugwilitsa ntchito may oti, AKUTI, zikuonesa zokha adausi ndi ndioononga, Akuluwa ndi osusuka Msonda 2, Ukufuna uwauze Anthu chani😂😂😂 akuti akuti akuti Interview yonse yathera ndi mawu oti AKUTI kkkkk koma ndiye publicity secretory abambo Inu ndi ofuntha
@StevenPongolani-pp9by
@StevenPongolani-pp9by Год назад
Brian banda continue doing your good job
@patrickmsendema4982
@patrickmsendema4982 11 месяцев назад
The best interview
@chisomombeta6446
@chisomombeta6446 6 месяцев назад
Powerful interview.....koma nkhani ndiyakuti onse amene anasumira chipani no chance ....Ayambitse chao
@dominicmphepo-jk8lk
@dominicmphepo-jk8lk Год назад
Hie guys no politician in Malawi will come to save our interest, they will be saving their own interest with their families. Let's go out there and work hard and support our families these guys akupanga Michele yawo ife tizingovutika nazo chabe.
@Littlefair7
@Littlefair7 Год назад
Koma achinyamata ndi amene akumva kuwawa dziko, yet ndi amene Safuna kulowa ndale, dziko la malawi panopa likufunika andale atsopano.
@Asidibrahim
@Asidibrahim 11 месяцев назад
U are right
@patrickmubiana9505
@patrickmubiana9505 11 месяцев назад
Independence. Of Zambia. Was on 24. October. 1964. Not 1963. Thanks big Man. Following you from Zambia.
@ibrahimwezely-pn6te
@ibrahimwezely-pn6te Год назад
Komatu dpp isamale izizi sizingabweretse chipambano, chipanichi ndichamphanvu ngati onse ali limodzi united. Chiyembekezo cha amalawi chili ku dpp koma nd🎉immene zikuyenderamu kaya tiziziona. Koma asawadelere adausi ndi ena omwe akutsutsana ndi akuluakuluwa
@violetmanasecheonga4495
@violetmanasecheonga4495 11 месяцев назад
Amen 🙏
@user-fw8so5st6d
@user-fw8so5st6d 11 месяцев назад
I wish could understand language, but looking and listening at the clip shows that here is a serious thing going on
@frankkuluunde
@frankkuluunde 11 месяцев назад
You are doing good so not forget kuti these people read more people while Brian zidamukanika Ku State
@jonathanchirwa3297
@jonathanchirwa3297 Год назад
❤❤😂😂😂 Mr Banda you're super
@user-zc4wl5pc3m
@user-zc4wl5pc3m 5 месяцев назад
Politics devide and rule
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 11 месяцев назад
😂😂😂 big up Nic , i agree with you the party doesn't belong to a person .
@chipi892
@chipi892 Год назад
Yambani chipani chanu Mr Dausi to ease your pain
@lastonekaponya7675
@lastonekaponya7675 Год назад
A dausi ngati mukufuna kusiya chipani dzingopitani Ku MCP komwe munaliko sitikukudandaula wava
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Год назад
Nkhani koma imeneyo
@evansedgarmatope2463
@evansedgarmatope2463 Год назад
I have started to love Nicolas H.Dausi, he speaks the truth now....
@chesterdiquissone6063
@chesterdiquissone6063 Год назад
He understand politics very well.
@pasterPatrickGNsulupi
@pasterPatrickGNsulupi 11 месяцев назад
Ai ndiotsokonedza bwanji tsakulankhula ena onwe anali kumenekowo? Ndi wa MCP mkuluyu
@Chief-Phungwako
@Chief-Phungwako 8 месяцев назад
He is grown now
@KenkingsChidumula-pc3oj
@KenkingsChidumula-pc3oj 11 месяцев назад
Mr Brian
@teddienamabande671
@teddienamabande671 Год назад
Dausi ndiosokoneza.
@user-og4oe5yp4w
@user-og4oe5yp4w Год назад
A Brian inunso ndi munthu osokoneza adausi ku nsonkhano sadapite zimenezo azitenga kuti ? Adausi zawavuta chifukwa zofuna zawo sizidatheke akatengane ndi nankhumwa akaone kopita
@esthergweje4038
@esthergweje4038 11 месяцев назад
Munthalika akumufunatu ndi anthu mmamidzimu ndi nkona amzanu anaona kuti azangoimira Munthalika yemweyo bwanji a Dausi mungoyambitsa chipani chanu at least mukamasuke musawasokoneze anthu tikuvutika ndi ifeyo osati inu ovuta ndi ife amalawi osati inu
@victoryganizanimwale9046
@victoryganizanimwale9046 Год назад
Brian Banda you are very good in this field of interviewing people..Keep it up good work sir
@user-tx7ms9xs9q
@user-tx7ms9xs9q Год назад
Akuti akuti akuti akuti akuti,akutiyo ndani
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk Год назад
Dausi ndiwa MCP palibe chanzeru chimene anganene chomanga chipani chathu cha DPP
@user-xd7kw4ze6h
@user-xd7kw4ze6h 11 месяцев назад
Anthu awa ndi ma brothers😂😂😂
@TrysonChimenya4-fm8nt
@TrysonChimenya4-fm8nt 11 месяцев назад
Dausi is showing signs ,of going back to MCP, Politics indeed is a dirty game, Never trust these recycled politicians.
@joyceellis9045
@joyceellis9045 Год назад
Anthu awiri awa tsiku lina adzagwirana pa manja 😂. Koma they are like Tom and Jerry. They need each other's presence 😅.
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Год назад
Brain mumawaitanila chiani amenewa. Nthawi Yao inatha. Tinatopa nazo nzeru zao zoononga dziko
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 11 месяцев назад
Heated interview
@walusungukayange8759
@walusungukayange8759 11 месяцев назад
This is one of the best interview. I always like the interaction between Brian and Dausi.... You're really democrats. ❤❤❤❤❤
@user-pq5bo5ch3m
@user-pq5bo5ch3m Год назад
😅😅😅😅😅 woza nazo,bring it on
@user-wp2bp4hx5g
@user-wp2bp4hx5g Год назад
Koma mukungoona kuwada a Dausi,Munthuyu akulankhula zoona mmene multiparty imakhalira
@kondwaninicholas2933
@kondwaninicholas2933 11 месяцев назад
Nicholas dausi ndiwe osokonezeka ndiwe was mcp
@joemlelemba6572
@joemlelemba6572 Год назад
Mr dausi we don't like you, zizungu zanuzo sizingati thandize kulibe oti tongamubvotere ku dpp apart from Peter mutharika , age is just the number , we need matured people like him , inuyo a dausi mwapanga chani ku chipani , Inu ndi wa mcp tonse tikudziwa ndipo we know you mumkayenda wapansi mukupanga driving school yanu mu Blantyre mu , kukambisana satero program siyanu , musadzawaitanenso awa , palibepo chamzeru
@frankkuluunde
@frankkuluunde 11 месяцев назад
That's political science
@user-cq5zb4lb4d
@user-cq5zb4lb4d Год назад
i love this dausi mpaka ndayamba chifuwa ndikuseka kkk
@edwardmusamba8173
@edwardmusamba8173 11 месяцев назад
Hon Dausi were u there ? If u were not there I will appreciate u investigate properly B4 u comment. U hv a very good base for your argument but u were suppose to attend that meeting so that u tell them your opinion.
@patriciondadzela2869
@patriciondadzela2869 Год назад
Dausi is just ranting? He has a court case to answer so seeking sympathy of MCP .
@edwardmusamba8173
@edwardmusamba8173 11 месяцев назад
Brian I love and enjoy your interview. Keep it going u are are too genius.
@patiencetebulo
@patiencetebulo 11 месяцев назад
Dausi ndiwe chitsiru bas ok
@greychizaka4088
@greychizaka4088 Год назад
this is again one of the best interviews. Dausi ndi Brian amayakitsa moto ahahahaha
@ThoccoBondo-mx7vt
@ThoccoBondo-mx7vt 11 месяцев назад
Dausi bwinotu osazimangilira muyankha bwanji zithu zoti inu kunalibe kkkkkkkkk
@jameboy3924
@jameboy3924 Год назад
Uyu ndi wa mcp
@norabanda3891
@norabanda3891 11 месяцев назад
I think B ans D should get married..they really get along well...they understand each others political language and share a great sense of humour ...bless them 😂😂😂😂😂🎉🎉🎉uluuuuuu
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Год назад
Kodi adausi mukuona ngati boma liri pa Times Radio abambo inu mulibe chopanga ndithu pitani ku konko ku MCP
@towellabanda2218
@towellabanda2218 Год назад
Dausi have learned his lessons I support him 😂😂😂😂
@promisemakawa1556
@promisemakawa1556 Год назад
Brian ndi Dausi😅😅 mumamvana Kwambiri, mumandiwaza😂😂
@biza4111
@biza4111 Год назад
kkkkkk eish ngati ndiibwereze
@kondwanichiweza4101
@kondwanichiweza4101 Год назад
mpakana chakhumi ???
@frezarphiri3480
@frezarphiri3480 Год назад
Brain ndi Dausi aphana 😂😂
@WinnerChisambi
@WinnerChisambi 4 месяца назад
Koma Brian ma video Anu ambiri sakutha bwino why amangoyima basi kumapitirila ndimau okha bas why
@DanielJuly-dj2ji
@DanielJuly-dj2ji 11 месяцев назад
Brian ndi Dausi 🤣🤣🤣🙌
@user-sx7fg1NEDG
@user-sx7fg1NEDG 11 месяцев назад
Waku ngona uyu kkkk
@ussimasi2458
@ussimasi2458 Год назад
Dausi ndi brian aaa anthu inu mukakumana ayi 🤣🤣🤣🤣ndimaseka
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Год назад
Dausi wa kwathu ku Mwanza koma zochita zanu mulibe chitukuko and zokamba zanu mmmmmm manyaka
@robertrichman9376
@robertrichman9376 Год назад
Nduona ngati akutumidwa ndi MCP galu uyu kuti ayipite DPP, komaso akufuna kuti milandu yake ikhululukidwe
@edsonnyirenda-uv3sb
@edsonnyirenda-uv3sb Год назад
Pena muzingokara chete basi,osamangoyankhira zili zonse
@user-og4oe5yp4w
@user-og4oe5yp4w Год назад
Inu adausi ku dpp amene asakufuna achoke zipani ndi zambili mukonza kukajoina
@frezarphiri3480
@frezarphiri3480 Год назад
Ine Dausi ndi Brain mumandiwaza muzipanga izi deile kkkkk😅😅
@user-yt2op5rl2q
@user-yt2op5rl2q Год назад
Daus ndiwa nankhumwa akulankhulira nankhumwa team yanankhumwa mbuzizawanthu
@user-ij6nq4dr3s
@user-ij6nq4dr3s 11 месяцев назад
Awatu alindimbali yawo Mr Dausi mukwaziwa sanganene zabwino ku Dpp
@user-kq8rb9jj7s
@user-kq8rb9jj7s 11 месяцев назад
😂😂😂😂 Braan ndi Dausi umandiwaza
@rachidermak8827
@rachidermak8827 11 месяцев назад
Munagulisa buluku ia polisi pá ntengo WA 2000000
@nkhwalamkwala6483
@nkhwalamkwala6483 Год назад
😅 Dausi amaziwa ndale
@PeterKhumbilaZimba-ql9ue
@PeterKhumbilaZimba-ql9ue Год назад
Aki and popo
@user-om9de3hr2x
@user-om9de3hr2x 4 месяца назад
Munthu ndi uncle ake
@MitengoFrancis-sp9ox
@MitengoFrancis-sp9ox Год назад
MR DAUSI. Chimenene. Mwayankhula APA ndi zosamveka Ngati inu mukufuna kubwelera Ku. MCP tangopitani musachuluse zokamba APA
@bonexboney
@bonexboney Год назад
Yo kumba mbewa ngati iweyo 😂😂😂😂
@darrenduisel3683
@darrenduisel3683 8 месяцев назад
Iwe Nicolas Dausi usatenge ngati Amalawi opepera which party you're belongs D P P kapena M C P ? Ndiwe gwape kwabasi ukuwasokoneza Amalawi maganizo ngati ulj wanzeru bwanji sunapite ku meeting??????
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Год назад
Chisiyeni Chipani cha DPP a Dausi chifukwa mukugwira ntchito ndi MCP
@francischalamendo9084
@francischalamendo9084 Год назад
Koma awa kkkkkkkk
@user-jw3rs2fr9v
@user-jw3rs2fr9v Год назад
Zachisoni nzeru za MP
@user-kq1pb8yl7f
@user-kq1pb8yl7f Год назад
Owononga uyu
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Год назад
A Dausi ndinu a MCP tonse timadziwa kuyambira kalekale ndiye za DPP zisiyeni eni wake agwilizana
@user-og4oe5yp4w
@user-og4oe5yp4w Год назад
Adausi ingochokani ku dpp mulibe phindu ku chipaniko tazingopitani ku mcp komweko
@Littlefair7
@Littlefair7 Год назад
Mr. Dausi akunena zoona koma, APM should step aside and pave way for new blood. DPP ikuonetsa poyera kupusa kwa amalawi.
@yusufsadic2930
@yusufsadic2930 Год назад
Mwayamb kunyozan nokh nokha odya mbewanu kumasulir kt odya mbewa ndi Anthu opanda nzer? Mwatimasulat yapa
@patriciakaombe
@patriciakaombe 11 месяцев назад
Hon Dausi😂😂😂😂
@nelsonnkhambule6292
@nelsonnkhambule6292 Год назад
Hon dausi ndi a yes bwana awo amangosusa chilichose
@rachidermak8827
@rachidermak8827 11 месяцев назад
Mupite,kuchipani kuano. Nanga pamenepo mulankhula ni ndani inuwo kukula mtima basi
@tracymantchichi8347
@tracymantchichi8347 Год назад
Muzaphana Inu😂😂
@jamessaiti
@jamessaiti Год назад
Uyu ndiosokoneza komaso ndi wa mcp
@osmanhassan8466
@osmanhassan8466 Год назад
Interview ya Dausi ndi Brian simalongisoka,kumachuluka kucheza
@SamsonGood-cw7pp
@SamsonGood-cw7pp 11 месяцев назад
Zonse mchabe wabwino ndi yesu yekha basi
@blessingskaliasi4956
@blessingskaliasi4956 11 месяцев назад
Phanani bas 🤣🤣
@chrispeter5256
@chrispeter5256 11 месяцев назад
and i quote "iweyo usanabadwe 1992 - 1993"......kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
@merviselias6230
@merviselias6230 Год назад
Iwe dausi unayamba kale ndale, ngati ulindi mzeru osayambisa chipani chako bwanji,munthu osokoneza,adausi inuyo mulingati hule, kumene mungaone Kuti zikuyenda mumathamangira komweko, tikufuna APM ndiifeyo anthu akumudzi amene tiliamphawi osati inuyo Adausi
@tronygiftmitengo
@tronygiftmitengo 11 месяцев назад
Akuwatuma ndi a mcp
@Mbwanaayami-hp3xk
@Mbwanaayami-hp3xk 11 месяцев назад
Dausi libe nzeru tsogoleri ndi APM omwewo kagwere uko iwee
@derekkolopo1300
@derekkolopo1300 11 месяцев назад
Anthu omwe akusaukitsa dziko ndi amenewa
@user-di4om7sh8w
@user-di4om7sh8w Год назад
Daus ndikatundu mmadzi ndipo akunena zoona ndipo APM ngt sasamala chipanichi chikutha
@louisgolden
@louisgolden 11 месяцев назад
Dausi akuopa mafuso😂😂😂
@MilikaKilion-tn1bn
@MilikaKilion-tn1bn 11 месяцев назад
Brian ndi a Daus chonde thiti zanga zikuwawa mkuseka😂😂😂
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 11 месяцев назад
😂😂😂😂😂😂 ...dausi ndi ndi waboza eeich
@samuelsergio5343
@samuelsergio5343 Год назад
A Dausi ali mugulu lofuna kuti amalawi adzivutika.president ndi muthalika yemweyo
@user-xt3rh9ob6y
@user-xt3rh9ob6y 11 месяцев назад
Nice😂
@Phaless-ur6en
@Phaless-ur6en 11 месяцев назад
Dpp ithelalimodzi ndi amuthalika
@user-bc1zi6hz7g
@user-bc1zi6hz7g 10 месяцев назад
Daus ndikachan
@emmanuelkenneth4768
@emmanuelkenneth4768 Год назад
Akulankhulatu zomveka koma nkuluyu ngati chipani ichi sichisamala chitha ngati ma katani, Munthu wanzeru mamayenera kumva maganizo a ena ndikupereka maganizo ako then kupanga chiganizo chabwino chokomera anthu onse.
@robertrichman9376
@robertrichman9376 Год назад
Don't trust Dausi, don't forget ali ndi milandu yoopsa yomwe akuyankha, nde don't expect kupanga zinthu zokomera DPP, akufuna MCP izinva zoipa za DPP kuti akhululukidwe milandu yake
@alfredbanda1693
@alfredbanda1693 Год назад
​@@robertrichman9376inuso nde abodzatu dausi akuyakha milandu iti muli mumalawi inu koma
@user-gn1xn3js4l
@user-gn1xn3js4l 11 месяцев назад
Adawusi ndi galu alibe fundo kodi sakupitilanji ku m c p ko bwanji kodi amasetenga ngati aliyeka
@peterchilewa380
@peterchilewa380 11 месяцев назад
Asatinyase dausi wa mcp
@crementnkhoma7735
@crementnkhoma7735 Год назад
Daus choka mchipan usatisokoneze
@kamwendoderek6567
@kamwendoderek6567 11 месяцев назад
adausi ngati mufuna upuresident ingonenani
@user-kj8kj1kr9t
@user-kj8kj1kr9t 11 месяцев назад
awa kumvetsetsa kwangowavuta. ineyo sindikuona vuto iliyonse. komanso is this the right proceedures yonenera zinthu? bwanji iwowa a dausi sanapite kwa a president awo mkukakamba nawo? kukula mtima akuruwa. kkkk
Далее
Masomphenya Anga with Napoleon Dzombe
30:05
Просмотров 44 тыс.
Nancy vs Che Nkope - Impi Biyeni Ause Muntendere
26:03
ARRIVAL OF LUCIUS BANDA'S REMAINS😢
1:22:27
Просмотров 65 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH ENOCK CHIHANA
56:27
Просмотров 52 тыс.
hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba
1:14:23
Просмотров 39 тыс.