Hie guys no politician in Malawi will come to save our interest, they will be saving their own interest with their families. Let's go out there and work hard and support our families these guys akupanga Michele yawo ife tizingovutika nazo chabe.
Komatu dpp isamale izizi sizingabweretse chipambano, chipanichi ndichamphanvu ngati onse ali limodzi united. Chiyembekezo cha amalawi chili ku dpp koma nd🎉immene zikuyenderamu kaya tiziziona. Koma asawadelere adausi ndi ena omwe akutsutsana ndi akuluakuluwa
A Brian inunso ndi munthu osokoneza adausi ku nsonkhano sadapite zimenezo azitenga kuti ? Adausi zawavuta chifukwa zofuna zawo sizidatheke akatengane ndi nankhumwa akaone kopita
Munthalika akumufunatu ndi anthu mmamidzimu ndi nkona amzanu anaona kuti azangoimira Munthalika yemweyo bwanji a Dausi mungoyambitsa chipani chanu at least mukamasuke musawasokoneze anthu tikuvutika ndi ifeyo osati inu ovuta ndi ife amalawi osati inu
Mr dausi we don't like you, zizungu zanuzo sizingati thandize kulibe oti tongamubvotere ku dpp apart from Peter mutharika , age is just the number , we need matured people like him , inuyo a dausi mwapanga chani ku chipani , Inu ndi wa mcp tonse tikudziwa ndipo we know you mumkayenda wapansi mukupanga driving school yanu mu Blantyre mu , kukambisana satero program siyanu , musadzawaitanenso awa , palibepo chamzeru
Hon Dausi were u there ? If u were not there I will appreciate u investigate properly B4 u comment. U hv a very good base for your argument but u were suppose to attend that meeting so that u tell them your opinion.
I think B ans D should get married..they really get along well...they understand each others political language and share a great sense of humour ...bless them 😂😂😂😂😂🎉🎉🎉uluuuuuu
Iwe Nicolas Dausi usatenge ngati Amalawi opepera which party you're belongs D P P kapena M C P ? Ndiwe gwape kwabasi ukuwasokoneza Amalawi maganizo ngati ulj wanzeru bwanji sunapite ku meeting??????
Akulankhulatu zomveka koma nkuluyu ngati chipani ichi sichisamala chitha ngati ma katani, Munthu wanzeru mamayenera kumva maganizo a ena ndikupereka maganizo ako then kupanga chiganizo chabwino chokomera anthu onse.
awa kumvetsetsa kwangowavuta. ineyo sindikuona vuto iliyonse. komanso is this the right proceedures yonenera zinthu? bwanji iwowa a dausi sanapite kwa a president awo mkukakamba nawo? kukula mtima akuruwa. kkkk