Anthu Inu palibe olamulira yemwe azapanga zifuna zanu palibe only Jehovah basi izi or mutalankhula bwanji or mutasintha bwanji muzalira mpaka kale mpaka ufumu wake ubwele basi mwana obadwa Kwa mkazi sangakoze zinthu kulibe
Nanunso simukutha kuwona Zoti Zinthu zidadokonekera? Nthawi ya ulamulilo winauja anthu amapanga blame? president like Mesa kutathaudza Nthawi imeneija zidali bwino than now. Ndi president waumbuliyo
@@ThokohKalonga-je9rx whether you like or not trust me zinthu sisizasinthapo mpaka kale may be your young you don't know where we were ndipo tikupita kuti just do your part kuti udye munthu sangathe mavuto Ako gwilantchito
Ndinabadwa mama 70 from 1994 up to now palibe Chaka katundu atsikapo momwe zinthu zinayambila kubwela nthawi ya Bakili sizinasinthepo tamawawuzani zolimbikitsa azigwila ntchito molimbikila osati kudalira munthu n0