Koma Chakwera ndi achina Chimwendo Banda akuti boma likuyenda bwino kwambiri. Eeeeeeeee! Anthu awa sadabwere kuthandiza dziko, koma kudzadya. It's a shame. Achoke basi
Bwezi akulandidwa katundu ndi ndalama zomwe akubawa bwezi kubaku kutatha koma from 1964 up to now palibe ndi modzi yemwe adalandidwapo katundu ndiye chifukwa chake kubaku zikukutha kumawalanda katundu ndi ndalama zomwe basi
kumudzi kwathu kuno ku Malawi ndimadabwa kuti kodi bungwe limeneli la ACB likutani komanso why do we say that we have ACB yet corruption instead of coming down komano ili pa makwerelo kupita mmmwamba. mwachitsanzo passport ya MK50,000 kuti ifike mmanja mwa M'Malawi nde kuti akhala atagwiritsa ntchito makobiri opyola mk200,000. ngati otsogolera ali serious to deal with this nde kuti all juniors will be afraid. ndizovuta kuti katangale athe ngati otsogolera akupanga nawo.
Ndimbamva zokha zokha zimenezo mcp anthu onse anali alimi ndie atani anthuwo akhala ali pa ulimi kwa zaka za mbili ndie asabe Mesa khotse mu mteza simukuona pamenepo kuti mbuzi aimangilila pa mbale ndie mumati ingatani Mesa kungodya mbaleyo mowonongaso ka kuti mwai umenewu suuzapezekaso ka 😂😂😂😂
Katangale kuthi athe ndi mopweka vuto mukumasakaniza ndi school opezeka wapanga katangale asamangidwe koma amenyedwe paulu kumumangilila pa bwalo athu akuona athu atha kusiya
Katenga okhoza kutha ndinthu komano anthu akupanga dala chifukwa choti malamulo anthu Ali so week let's we say titati tipange lamulo loti aliyense ogwira ntchito m,boma akapezeka ndi mulandu wakatangale azipatsidwa ban kuti sazagwiranso ntchito m,boma mpaka kalekale. Ndithu vuto limeneli likhoza kutha ndithu