Тёмный

KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌 

HOT 265
Подписаться 65 тыс.
Просмотров 166 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

5 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 391   
@RiannahKaliat
@RiannahKaliat 6 дней назад
Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe
@RiannahKaliat
@RiannahKaliat 6 дней назад
Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend
@mayesohenry
@mayesohenry 6 дней назад
😢😢😢😢😢
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 3 дня назад
Nanenso
@mirriamnyongolo-vf6cn
@mirriamnyongolo-vf6cn 3 дня назад
I still don't believe
@user-fd1tu6ku1r
@user-fd1tu6ku1r 6 дней назад
The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.
@sithandanechirwa6376
@sithandanechirwa6376 6 дней назад
I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands
@HamiltonwaNamuwah
@HamiltonwaNamuwah 6 дней назад
Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo
@MarthaJafali
@MarthaJafali 6 дней назад
Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu
@user-nw6ie3xx8b
@user-nw6ie3xx8b 6 дней назад
I love this brother but dyela
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 6 дней назад
Zikomo mtambo
@emmanuelmukondia3568
@emmanuelmukondia3568 6 дней назад
THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.
@jamesgondwe6669
@jamesgondwe6669 5 дней назад
God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 6 дней назад
That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess
@AbelSinoya
@AbelSinoya 6 дней назад
Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂
@jogechawa6192
@jogechawa6192 6 дней назад
For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma
@EdoJohn46
@EdoJohn46 6 дней назад
Antambo 😂😂😂 ndikukutengeni ngati ndinu amene mudasongezera dzikuni dzamoto kuti tipse Malawi muno ndiwe galu kwabasi
@ThomasShuga
@ThomasShuga 5 дней назад
Very true 😢😢
@MatiasMbaula
@MatiasMbaula 4 дня назад
Very true
@MaggieCement
@MaggieCement 3 дня назад
Ndipo Inu alibe umuthu uyu za ziiii mesa iye emweyi ndiamene anapangitsa kuti tilowe mudima akuonapanowo galu zedi
@wakisamsukwa9918
@wakisamsukwa9918 2 дня назад
No matter how long you have gone the wrong road, turn back. Turning back isn't an offence
@HarlodAndrewbanda-vf2rd
@HarlodAndrewbanda-vf2rd 6 дней назад
We're still crawling to get there!! Rest in peace Dr SKC, UTM is a movement
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 6 дней назад
Amtambo...ngat mukufuna kut ife tikukhululukireni ...pitani ku mademo mutibwenzere dziko lathu...anthu akuopa mademo chifukwa alibe support...mabungwe onse chakwera adasiya abale ake mmaudindo
@LOKAMJ
@LOKAMJ 5 дней назад
Exactly
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 5 дней назад
DPP could have finished us . He did the right thing to rescue some of us from DPP. It was oppressing us
@InnocentMmanga
@InnocentMmanga 5 дней назад
😂😂😂
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 5 дней назад
@@ancientnkhata1137 oooooh ...May the curse of Almighty befall who is a lier...and make them the wood of hell fire
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx 6 дней назад
Mtambo thanks for the vital words. We now needs actions against these idiots in the government
@rexphiri6951
@rexphiri6951 5 дней назад
powerful words Mr Mtambo
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 5 дней назад
Only stupid people with commend the selfish and greedy Timothy Mtambo
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
@dhaoudhiabedinegomaseko2363 День назад
Mtambo mseu wa Rumphi Nyika Chitipa munawukana mesa munkaguba nkumaphwanya zinthu kuti musinthe utsogoleri
@SakanjiraRose
@SakanjiraRose 5 дней назад
I'm getting confused, he is the man who mobilized people to fight a government that was to me far much better than the this one he helped to form.
@chrisboyce2
@chrisboyce2 6 дней назад
SKC forever in our hearts 💔🔥 powerful words Comrade Mtambo Osafooka kms Osaopa Dziko ndi lanthu ife kuno Ku Ntcheu tili mbali yanu...
@user-te4ii6sz2v
@user-te4ii6sz2v 6 дней назад
We quote more political speeches than prayers. This was not a political rally
@JosephHill-fy1bb
@JosephHill-fy1bb 5 дней назад
Ntambo is not a pastor.... Just watch pastor's preaching time...
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 6 дней назад
Ndikakumbukila ifa yaathu amenewa mtima umawawa
@PatriciaMbewe-xn7ke
@PatriciaMbewe-xn7ke 6 дней назад
Kwambiritu
@YohanePatrick-lc2lq
@YohanePatrick-lc2lq 6 дней назад
Man ife amalawi tikufuna dpp enawa abodza ngati iweyo Timothy anakuchosa ku mcp chifukwa cha katangale
@user-zf9xs3zj9b
@user-zf9xs3zj9b 6 дней назад
Wakuba mtambo akutiona ngati amalawi ndife galu anthu mwa sandutsa ndale ndi maliro a Dr saulos chilima 😂😂😂
@MisheckAselo
@MisheckAselo 6 дней назад
That's true they is nothing to celebrate 60 years, it's like we help chakwera, kumkuyu ndi zikhale ng'oma kudya mitsonkho yanthu. Ayi momwemo 😂
@ChiletsoChembe
@ChiletsoChembe 3 дня назад
Amalawi please! Let's pray to God forgive us and punish those who mudder saulos chilima
@user-ub1mw7ce5p
@user-ub1mw7ce5p 6 дней назад
Well spoken, comrade Mtambo.
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 дня назад
He has missed the trail. Uyu watha. Ndipo akamati ngati wina amawona ngati wayimisa agenda, atanthawuza kuti munthu wina anachita kuphedwa? Kulankhula kopanda nzeru
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 дня назад
Nanga munthu angati anyamata oganiza bwino akumanena wena Lwarwa aaaah guys Mtambo anaganiza bwanji?
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 6 дней назад
Mtanbo akuyakhula za ndale zikugwilizana bwanji ndi mwambowu
@ErickIssah
@ErickIssah 6 дней назад
Ndipo inu
@JohnSingano-f1p
@JohnSingano-f1p 6 дней назад
The voice of a lion always brings confusions
@ConfidenceBanda-g8k
@ConfidenceBanda-g8k 6 дней назад
Koma ndipo poletsa kupepherapo ndie nduchitsiludi,mobwereza amene amaletsa kupepherayo nchitsiru
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 5 дней назад
Well spoken comrade mtambo criticism singalephere as Malawian we were born like that, keep it up comrade
@jonathanmalanda7742
@jonathanmalanda7742 5 дней назад
A Mtambo ikani za mapemphero kuti mzimu wa skc uuse mumtendere
@TnmMpamba
@TnmMpamba 6 дней назад
Watching live from Salima, Khombedza
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 6 дней назад
mtambo walankhula za mzeru kuposa namachende chakwera
@ChifundoWillard
@ChifundoWillard 6 дней назад
😂😂😂😂😂
@tingamasi106
@tingamasi106 6 дней назад
😂😂😂😂😂😂
@LukeMkandawire-cr7en
@LukeMkandawire-cr7en 2 дня назад
😅😅😅
@AndrewLanken-v3u
@AndrewLanken-v3u 5 дней назад
He has got nothing to give malawians never
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 6 дней назад
Koma tizikukhulupirirani ndithu a Timothy???
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 6 дней назад
My question too 😢😢
@MagretIdimu-u7w
@MagretIdimu-u7w 2 дня назад
We're heart broken 💔 SKC still remains in our hearts 😢😢😢
@DannielOnions-fy3dc
@DannielOnions-fy3dc 5 дней назад
Thanks so much 🙏 keep it up please we need people like 👍 u
@SteveKumwenda-t3d
@SteveKumwenda-t3d 6 дней назад
Chitsiru ichi, ndiponso uku sikumapemphero
@abwinoamatani4921
@abwinoamatani4921 6 дней назад
A ndale ndabodza kumene. Ndi chifukwa chake olo akuba ndalama zambiri-mbiri akavala amangokhala ngati avala chithumba chaku chigayo
@user-io2uw2me9f
@user-io2uw2me9f 5 дней назад
😂😂😂😂😂😂😂
@AndersonChiponola
@AndersonChiponola 2 дня назад
Mtambo ndamene anapangitsa zonse izi palibe chomwe angayankhule Mutu wake sumayenda bwino ameneyo chifukwa anamuchotsa unduna wagwa nayo Mbuzi iyi
@user-ie5pc4ox8i
@user-ie5pc4ox8i День назад
Ada awawa bwenz Ali MUNTHU wapamwamba kwambir kma Anapanga zausiru ngat akufuna timukhulukire ayambise mademo
@RitaKainga
@RitaKainga 5 дней назад
Zikomo Inu nonse amene mwalimbabe mtima kupanga mwambo uwu though asatana akutchinga,Mulungu wathu ndwabwino,sanalepherepo,imfa iyi ndyovuta kuiiwala
@JohnAsendi
@JohnAsendi 6 дней назад
Antambo vuto chinthu chimozi mumafuna ndalama Chonde muzikhala ngati Born Kalindo chifukwa amati pavute pasavute asayimira amalawi ndipo akuti imila amangidwa amangidwanso pomwe enanu mumatifuna pomwe zakuvutani tikukukuwerenganitu INEYO NDIKUCHALENJA zoti wina aliyese aime payekha kuyambira Apita. Tupele. Raz. Nankhumwa. Shahana. Osati Chakwera Amayi Joyce banda ndi phulezdent Kalindo. Ndiye tikavote masankho mawa mwachilungamo mopanda kubela angawine ndi Kalindo chifukwa ndi amene akuoneka kuti angatithandize osati Ena inu 😁😁😁😁😁😁😁😁😁
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 6 дней назад
Inuyo
@user-ww4ei5fb7d
@user-ww4ei5fb7d 5 дней назад
Kalindo ndiolimba mtima, ofunika kumuvotera. 😂
@JohnAsendi
@JohnAsendi 5 дней назад
@@user-ww4ei5fb7d zoonadi sister osati enawa akuoneka ngati akuti konda koma mmitima mulibe chikondi
@LulezLele
@LulezLele 6 дней назад
Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 дня назад
Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa
@user-bq5ev7de1l
@user-bq5ev7de1l 6 дней назад
Apm my vote ✊
@JosephJosab
@JosephJosab 6 дней назад
Mtambo ndi kape
@surgeon1621
@surgeon1621 3 дня назад
Malawi has become a very sad country. Everyone is just fighting for their own stomach. A person like Mtambo shouldnt be applauded like that as if he wasnt a minister in this government. What achievement can he show malawians to prove he is a better man for malawians. A lot of people want to use Chilimas death to gain points for themselves and yet they have no substance themselves. Too much sentimentalism without constructive knowledge
@emmanuelmukondia3568
@emmanuelmukondia3568 6 дней назад
Idol worship
@user-jx8us9bc1o
@user-jx8us9bc1o 6 дней назад
I totally agree with you
@user-nj1pv8hj2x
@user-nj1pv8hj2x 6 дней назад
Ndipo live i agree with you big time 👍👍👍
@amourvido8027
@amourvido8027 5 дней назад
And they don't realize it, they blindly do it💔
@hendrixchimalizeni750
@hendrixchimalizeni750 5 дней назад
Usaweluze pakuti kuweluza ndikwake namalenga
@blessingskutchuwi8635
@blessingskutchuwi8635 4 дня назад
Take it if it was your DAD.... 😔 Bwez iliso Idol worshipping
@kamangamathias2001
@kamangamathias2001 6 дней назад
What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 дня назад
Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise
@MaggieCement
@MaggieCement 3 дня назад
Iyeyu anali boma momwemonwapanga chani atinyase apa chifukwa anamuthothamo modzi mwa anthu okhutisa mimba iyeyo aligulu lomwelo hiya zokuba basi😊
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 6 дней назад
More fire mtambo chakwera machende ako😂
@PhillspicJere
@PhillspicJere 6 дней назад
You will gain nothing bro potukwana munthu wankulu, matsoka agwa pakutu panu
@LukeMkandawire-cr7en
@LukeMkandawire-cr7en 2 дня назад
Watan😅
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 4 дня назад
Only God is our rest not this politicians. God help Malawi
@arthurmanyozo1289
@arthurmanyozo1289 6 дней назад
Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus
@LunnahMtambo
@LunnahMtambo 6 дней назад
More fire bro ,love from ccter namtambo cp
@LloydLuwis
@LloydLuwis 6 дней назад
Keep morefire mr tman
@WiscotDzombe
@WiscotDzombe 13 часов назад
Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 5 дней назад
Osaoopa ai......ku Malawi kulibe president
@edsonnyasulu5394
@edsonnyasulu5394 5 дней назад
Exactly Andale akale achoke boma achinyamata alamulire dziko nkhalamba ndi mfiti komaso ndiankhaza
@VincentAndrew-jz2gf
@VincentAndrew-jz2gf 5 дней назад
Atambo ,Ulibe Zelu unaphetsa Athu Ambili
@AustinBornface
@AustinBornface 5 дней назад
Malawi timakhala ngati tili pa stage tupanga drama kma ayi ndithu ndi action
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 дня назад
Munayambira kukonaza dziko mudzamaliza liti komanso palibe chimasintha mumaona ngati umphawi wamalawi ndiye podyera panu komanso polemerera panu palibe chanzeru chkmwe wayankhula mtambo apa
@PeterThomas-lw3io
@PeterThomas-lw3io 6 дней назад
Rest in peace 🕊️ chilima anagwira chito yaikulu DPP mu 2014 ikanafela giya komano chilima anapanga zotheka kuti Peter akhale tsogoleri muchomwechotso mu 2020 wayigwira ntchito yathangata kumuyika Crazy Chakwera akulamulila koma njilu ndikupanga mission plane yakumupha yooohhh Chakwera ngoyipa
@markjames-v1f
@markjames-v1f 20 часов назад
Chomwe mkukanikila kutiyimilira ndichan boss wanga
@anoldkapolo4493
@anoldkapolo4493 День назад
Kkkkkkkk aMtambo mabodza ndipo zikatere timati zawo zinaona kungolo, bwanji Mtambo osango gawa chakudya kwa anthuwo kapena muwamangira nyumbazo. . Kufuna ndalama kumeneko , osangopita kukapanga dimba . Chakwera akumenyera nkhondo ife alimi ndipo 2025 ndiboma choncho A Mtambo akunama
@AngellachifundoMwale
@AngellachifundoMwale 4 дня назад
Mumatipangisa ndinu omwe muli ndikuthekela kolamula dzikoli koma chonsecho simutithandiza and iwee ntambo uli nkuyankhula koma osakwanilisa mxiii unduna uja unali pheeeee ife tikuvutika pano fukwa cha nzerru zomwe unatilimbikisa ife kuti tikavotere mcp yet lero ukuti usintha ziko mub 2025 yet wakanika zaziii
@AbdulKhan-j2h
@AbdulKhan-j2h 6 дней назад
Mpava iyi atidye bawo bwanji Sumatuluka uli nduna pano abakuchosa ukufuna kodwela amalawi timaiwala
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 6 дней назад
LUWALA ANGASINTHE CHANI MBAVA YA MNTHU
@user-ok7bq9es3y
@user-ok7bq9es3y 5 дней назад
Timothy unali ndi molaro kale iwe because of Msundwe barracks, size yako ndi Chimwendo. Ulibe faz iwe
@MACKDADFFDANIEL
@MACKDADFFDANIEL 2 дня назад
Vuto athu kumalawi safuna kumenyela athu ovutika kom mimba zawo zomwe akuyakhula uyu ntambo ngati Ali ndi nzeru chonsecho momwe anali nduna samayakhula PAno anamuchotsa wayamba kuwalalatila athu omwe anawasiya a kugwila ntchito mbuzi ya muthu uyu ndipo ndipo ndiyemwe anapangitsa kut athu azivutika mpaka lelo
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 6 дней назад
Akulesa bwanji ma pephelo akuopa chani tiyeni nazo pephelo ndi chida
@MarriamBakalie
@MarriamBakalie 4 дня назад
Mtambo ndiwe galu kwabasi usamawapusise a 🇲🇼 anthu anakuona kale galu iwe zako zinada kale machende ako osavinidwa mbudzi
@taombeedward5026
@taombeedward5026 3 дня назад
The biggest problem mtamboyu
@user-wz1or9ud9i
@user-wz1or9ud9i 5 дней назад
Mzimu wa chilima awasowetse mtendere anthuwa mpaka anfe amene anapha chilima.
@GoodluckMwenifumbo-dk8jk
@GoodluckMwenifumbo-dk8jk 5 дней назад
Anthu ambiri osutsa pano ndi a MCP Zoona mpaka kuwaopseza amipingo,a MCP mwafikapotu
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 5 дней назад
Good Messnge Mr Mutambo
@AngellachifundoMwale
@AngellachifundoMwale 4 дня назад
I feel hurt mukamaimabr apaa nkumafuna kutinamiza kuti tikuvotereni sibwino unduna wanu inuyo munapangapo chani antambo nde lero muzinena ngati inu anzeru ??? Kutiona kupusa Malawi sichoncho
@abwinoamatani4921
@abwinoamatani4921 6 дней назад
Nanunsotu mukutichitsa manyazi, 60 eyes ndekuti chani?
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 6 дней назад
😂😂😂😂😂
@LimbikaniMakwandu
@LimbikaniMakwandu 5 дней назад
Only chilima not you mtambo RIP CHILIMA
@user-lz4kc5ob1t
@user-lz4kc5ob1t 5 дней назад
inetu ndimangokuveran anyamata a mcp ndimaziwa kt simunakumane nazo uyo mtambo ngat ndinu madolo kkkkk
@AlinafeMuleso
@AlinafeMuleso 3 дня назад
Mtambo mtima wake ndi wadyera mmene wachoka ku MCP akufuna apeze not adzidyera kudzera kwachihanna ndiye in leronso asabwere ndimabodza ake ofuna podyera watipwetekesa ngati dzikoli Lili pamoto nfichifukwa Cha iyeyu ndi galu kwabasi
@MorrisMapiri-d6z
@MorrisMapiri-d6z 4 дня назад
It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.
@nicholasshema9016
@nicholasshema9016 4 дня назад
Awawa anachoka value cz iyeyi akusapota Chihana Athu akuwauza apa kuti apite chitsogoro ndi achipani chinaso so he z speek speechles
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 5 дней назад
Amtambo naye ine ndinakhumudwa naye ndipo ndinataya chikhulupiriro mwaino mwatulukirano nthawi yonseyi munali momwemotu mu Timbaland wakudayo ndiye pano mukutinamizaso chani apaa iyaaa😊
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 6 дней назад
no no anthu mzimvetsa zinthu u know very well kuti 6 july ndisiku la padara kumalawi ufulu omwe mkulankhupa lero nkhani yake ndi 6july nde mmafuna asiye za 6july apange za ma candle aa imfa si ya chilima yekha ati anthu akufa dairy .
@SajeFurniture-wj1ue
@SajeFurniture-wj1ue День назад
Nkulu wake yemweyu anatibweretsera mavuto, how can we trust him
@GibsonBakha
@GibsonBakha 5 дней назад
Andale inu musamatiwawitsemutu muma gofuna ndalama agalu inu
@KenChitete-pg3ws
@KenChitete-pg3ws 6 дней назад
Vote yanga yikupita kwa afford
@vinceynyone6693
@vinceynyone6693 5 дней назад
Viva mtambo Viva🔥👏👏
@WilliamTemboh
@WilliamTemboh 6 дней назад
Km tkukhulupilileniso amtambo kapena mukufuna tindalama plz tell me coz munatpweteketsa
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 6 дней назад
Apitenso pansewu atibwenzere dziko lathu...ndiyemweyu adatipereka
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 6 дней назад
Ndipo ndi yemweyu analisiya dziko ku anthu otamba akewa, apa angotibwenzerapo dziko lathu lakale lomwelija
@HenriqKwilasi2022
@HenriqKwilasi2022 5 дней назад
Iwenso ndi mfiti chifukwa ukupanga za ndale mtambo
@SylvesterHarry-n7c
@SylvesterHarry-n7c 6 дней назад
Timothy mtambo adali momwemo adagwiramo ntchito palibe chimene adapanga nduwadyera uyu
@user-qs2tx7wt6g
@user-qs2tx7wt6g 5 дней назад
Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa
@promisegregory8397
@promisegregory8397 5 дней назад
Amalawi wake up Mtambo ndi kape this guy he is after Money ndi kape machende Ake,amangofuna Ku watenga amalawi ngati makape
@nafejonga972
@nafejonga972 6 дней назад
Rest in peace, my president .. we are still fighting
@YahayaUndiya
@YahayaUndiya 6 дней назад
Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo
@jelsonmlowoka8611
@jelsonmlowoka8611 5 дней назад
Anali momwemo mu galawundi bwanji zinamukanika
@user-uk3bz1hr5t
@user-uk3bz1hr5t 5 дней назад
Mtambo you are a reason behind all this problems malawians are passing through,You escalated demoz that paved a way for MCP to get in power,see now where we are now.😢
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 дня назад
Mtambo was a Minister anapangapo chani? Amuchosa lero azioneka wanzeru? Ndale zopusa izi. 6 July mapemphero anali ku BICC basi.
@ChilangoNdalama
@ChilangoNdalama 6 дней назад
Big mtambo timakunyadiran
@CharityKangulero
@CharityKangulero 6 дней назад
❤❤❤ Exactly
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 6 дней назад
Politics will never transform Malawi. I suggest,all party presidents,some traditional and religious leaders should jointly accost the H E and matters of philanthropy and patriotism concerning current national teasers.Neither invective nor censure wll bring democratic solidarity in our beloved nation.There is need for deliberation with the HE and his Vice President.Avoid self centredness,power hunger, political chauvinism and cupidity.We are no longer ease!
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 4 дня назад
But we needs people who can at least change something in this country 😢😢apart from this government that we have now😢😢
@henryphiri6100
@henryphiri6100 4 дня назад
Chilima anaphedwa ndi Zikhale Ngoma,Chimwendo,ndi Kunkuyu.
@georgenundwe
@georgenundwe 5 дней назад
Why do we choose kusadziwa pamene everybody knows pretty well kut kuli global crisis ya economy.....and one expects milakuli that we do best than the lest ....lets.be the champion of telling Malawians the.truth
@estherkambewa7791
@estherkambewa7791 4 дня назад
Eeesh zoopsya, taking advantage on poor people.
@KondananiNjakwa
@KondananiNjakwa 4 дня назад
Kodi zoti nsewu ukulimidwa pano sakudziwabe Mtambo? Kapena anatuluka mdziko muno? Anthu ndale mumapanga mosaganiza sure. Mapemphero adasanduka nsonkhano wa ndale? Useless politicians with no future
Далее
Who Can Break Most Walls? Ep.2 | Brawl Stars
00:26
Просмотров 777 тыс.
Dora’s Tyla Dance is Everywhere 😨 #shorts
00:14
Просмотров 2,3 млн
KAMLEPO KALUA KUYANKHULA MOSANYENGELERA
29:23
Просмотров 35 тыс.
Mbiri ya Mama Cecilia Kadzamira
29:43
Просмотров 209 тыс.
kumalawi kuno ndani wandale angamake??
1:01:32
Просмотров 67 тыс.
ARRIVAL OF LUCIUS BANDA'S REMAINS😢
1:22:27
Просмотров 91 тыс.
Who Can Break Most Walls? Ep.2 | Brawl Stars
00:26
Просмотров 777 тыс.