The problem is Malawians make decision during anger, and 2025 will do the same similar choice because of anger. Others they are speaking as if they are wise but the true sense these people if they happen to be chosen they will also worsen this country
Vc president ameneyo ngamene agulitsa Chilima amene amakonza zothetsa Tonse Aliance. Iye, pamwambo anati; Chakwera ndi wake komanso Chilima ndi wake. Kodi pamene amanena izi, Chilima ali kuti?