Тёмный

ANTHU AYANKHULA ZOSAOPA AWA 🙌🙌🙌 

HOT 265
Подписаться 62 тыс.
Просмотров 95 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

20 май 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 140   
@Blessings-td4cr
@Blessings-td4cr Месяц назад
Zomatchula aleluya andale musiye!! Zikumatinyasa mulungu sapanga ndale.
@user-vl5on2lj8b
@user-vl5on2lj8b Месяц назад
Ambuye mulungu amphavu zonse tipaseni mfumu yotikonda mutisankhire ndiinu poti mfumu yomwe iripoyi zikuchukuluka nkhadza kuba kupha kuononga amen
@AndrewKwalingana
@AndrewKwalingana Месяц назад
Maloto achumba. Aford will never be the ruling party in Malawi. Mark my words
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q 15 дней назад
Ndare sitimadya we need good leaders that can serve the people Malawi is the poorest country in the world lacking good leadership.
@edsonndalama2334
@edsonndalama2334 Месяц назад
Mpaka kunena kuti "ndi inu ndani akanyimbi inu?"
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole Месяц назад
Fantastic speech guys ❤
@4tune07
@4tune07 Месяц назад
Aaaaaaaaa !!!! Zonama izi ngat chakwera mukuona kt akuononga dziko ndie kt inuso mukuon muli mgulu lowonga coz inuo muli momo mu TONSE ALLIANCE
@UthmanKapungu
@UthmanKapungu Месяц назад
Moto ngati umenewo ndi umene tikufuna kuchokera Ku zipani zosusa fire!!!!!!!!!
@user-ti4yu6ob1e
@user-ti4yu6ob1e Месяц назад
AFORD you deserve 2 points👍
@alfredkanyawire3524
@alfredkanyawire3524 Месяц назад
We are now fighting for democracy in a Democratic state kkkk embarrassing indeed
@MrMwambananji-tx8jt
@MrMwambananji-tx8jt Месяц назад
Sindimayembekezela, awo ndiye mau zabwino zonse more fire!!!
@stevendachuva1443
@stevendachuva1443 19 дней назад
Sure
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk Месяц назад
Powerful!!!! 💪💪💪
@ReubenGama
@ReubenGama Месяц назад
Mcp sidawinepo chisankho, boma iliri ndilatonse . Eee koma kuwaulatu
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
More fireeeeeee sister mwayankhula bwino kwabasi Mulungu akudalitseni❤
@PeterChilombo-ou2cd
@PeterChilombo-ou2cd Месяц назад
zoona wazuru sakwatira mkhonde yomweyo kkk
@clalesschisale3792
@clalesschisale3792 12 дней назад
Vuto lake amalawi sitimaiwala tiannyoza DPP kuti imatizunza osaziwa kuti omwe timawaika pampandowo ndiomwe akutizunza kuposa DPP
@user-bq5ev7de1l
@user-bq5ev7de1l Месяц назад
Apm my vote ✊
@georgemoffat5143
@georgemoffat5143 11 дней назад
aaaaa MCP moto🔊🔊
@blessingskutchuwi8635
@blessingskutchuwi8635 Месяц назад
Uku ndye kuwawanyaaaa kwekweniiii....🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@StevenMbama
@StevenMbama Месяц назад
Anthu a afodi iiiii amatha mbalume eishiii
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Месяц назад
Simbiyamoto number one ❤
@user-nb2zz9ih1v
@user-nb2zz9ih1v Месяц назад
From Capetown chakwera must go
@superiormoses4802
@superiormoses4802 Месяц назад
Eee apa Moto walavulidwa hvy kugagada 🔥🔥🔥🔥
@user-vu6ec1le2b
@user-vu6ec1le2b Месяц назад
DPP + AFORD more fireeee!!!❤
@macdonaldblack3727
@macdonaldblack3727 22 дня назад
Amayakhula ngati sanapiteko kusukulu kmnso akhangati sakudziwa zomwe zikuchitika muno Malawi zimvereni chisoni
@amoschataika7440
@amoschataika7440 Месяц назад
Big up Afford kuswa kuswa basi.
@jollylunda4034
@jollylunda4034 21 день назад
Achewa kuyerekedwa wakubvutani chakwerawanu
@abdulazeezchapita2159
@abdulazeezchapita2159 Месяц назад
Anthu amayakhura eeeeee wandare usazamudelere
@samchibenene4458
@samchibenene4458 Месяц назад
Mwayankhura mwamphamvu mayi
@user-it5zv2nz7f
@user-it5zv2nz7f Месяц назад
Koma ine ndawusa manja anthu chilungamo akuchisata🙌🙌🙌🙌
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 Месяц назад
Mai chilungamo muyakhuladi ulemu wanu. Zowona Ndithu
@nafejonga972
@nafejonga972 29 дней назад
Utm my vote
@SteveChirwa-ne9nt
@SteveChirwa-ne9nt Месяц назад
Nthawi yakwana Afford Moto !!!
@user-dl6ly7kk1y
@user-dl6ly7kk1y 27 дней назад
Ndikanakhala olemera bomali ndikalanda mwaupandu, Anthufe tanzuzika kokwana palibe chikusintha
@chrisboyce2
@chrisboyce2 Месяц назад
Ndagwira mau amodzi akuti athu mu katopa simuyang'anaso za munthu kuti anali ndani zimenezi ndi zomwe zichitika 2025 DPP MY VOTE 💙
@AdamsMsosa
@AdamsMsosa Месяц назад
More fire
@user-nc6cz4jn9r
@user-nc6cz4jn9r Месяц назад
🔥 📛
@victor998vabatanazio3
@victor998vabatanazio3 Месяц назад
Don't trust in politicians you will get disappointed.
@gracemaluwa4674
@gracemaluwa4674 4 дня назад
AFFORD YOMWEYO KUTI WAAAAAAA!!!!
@AngelaTsekula
@AngelaTsekula 8 дней назад
Andale in mukafuna boma mumakhala ngati muli kumbali ya ife anthu ovutika. Mukatenga boma kuyamba kukhala mmoyo ozikonda munthu akakususani kumuphano
@user-by4vy9hb6m
@user-by4vy9hb6m 8 дней назад
Pajatu munkafuna boma lero ndi izi 😂😂 l quote MCP siinawineko boma, boma iliri nd la tonse alliance eeee anthu mwatopa ndi chilungamo😂😂😂
@ishmaeldama8906
@ishmaeldama8906 Месяц назад
Malawi is the best in Africa, Aford mwayankhula, i think chakwera he must resine he failed, all the way from johannesburg cbd
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Месяц назад
Kkkķkk Zoona ❤
@user-el8to1te3l
@user-el8to1te3l Месяц назад
Tikufuna anthu olankhila chochi osati kumaopa agalu mbava za mcp
@mavmsusa1310
@mavmsusa1310 Месяц назад
Anthu anawawata tu ku Mponela!!! Eish!!!
@MrBone-zj1wq
@MrBone-zj1wq 18 дней назад
Dpp is only my last hope not Aford
@MosesNyalugwe-ll8hh
@MosesNyalugwe-ll8hh 15 дней назад
Zoona MCP sinavoteredwepo
@ronaldharawa
@ronaldharawa Месяц назад
Aford is not our hope. The first president comes from my home area but nothing cannot be shown they did even after being given 2nd vice presidency
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад
Koma chakwera Ufa ndi mtima Athu atopa nawe payakhulidwatu apa
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Ndipo kwambiri
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
2025 tiona zinthu
@user-oq7hi3hd4p
@user-oq7hi3hd4p Месяц назад
Madam menya menya chilungamo chioneke.
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl Месяц назад
Aford atha kugwesa mcp anthu atopa ndi mcp
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl Месяц назад
Bola achewa mazindikila 😂😂😂😂😂
@MonicatimanyeShaba
@MonicatimanyeShaba Месяц назад
Chihana yomweyo 😂😂😂❤
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Месяц назад
Apm my vote
@masterchitabwino898
@masterchitabwino898 28 дней назад
Chilima my vote 2025
@JonathanMlongoti-wf6wi
@JonathanMlongoti-wf6wi Месяц назад
Following
@amoschataika7440
@amoschataika7440 Месяц назад
😂😂😂 Koma Mdala uyu waswa Mr Chihana ndi a Ntambo yendani limodzi ndi Mdala ameneyu akudziwa kuyankhula.
@owenskabazanechiumia3543
@owenskabazanechiumia3543 Месяц назад
Zowona M'dala ameneyu amapalula mbalume, No mantha or Manyadzi iai ayende naye M'dala ameneyu pa Campaign imeneyi.
@YASSANWADO-jk4xp
@YASSANWADO-jk4xp 20 дней назад
Km kumeneko kwachako bwino 😢😢😢😢
@decemberjonathan3001
@decemberjonathan3001 13 дней назад
KKKKK kuililira mitsonkho yanthu kumeneku tiye nazoni vote ili mumtima mwanga kkkkkkkk
@isabelfatch1517
@isabelfatch1517 Месяц назад
EKC my vote
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o Месяц назад
Koma sister wake wa Ntambo zikomo
@ClementZintula-wi4tz
@ClementZintula-wi4tz Месяц назад
Malawi true meaning of dziko lapasi
@user-gd3jx7tr1p
@user-gd3jx7tr1p Месяц назад
Ana inu
@JerryChain-cz8ru
@JerryChain-cz8ru Месяц назад
Mkazi walankhula mawu
@MayamikoKalimapadzala-sw7yp
@MayamikoKalimapadzala-sw7yp 23 дня назад
Sitikuso mawu achionvwe ayi tikuna fudo zabwino achimwene ndale zonyozana zinatha kale kale
@maxwellmajawa6091
@maxwellmajawa6091 Месяц назад
Tamvanan nd Dpp ma guy muyatsa moto
@ThomasShuga
@ThomasShuga Месяц назад
Very true brPlease
@DOLOTHYMAKINA
@DOLOTHYMAKINA Месяц назад
Zoona zake
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Месяц назад
Ndipo ndizoonadi akulimbana ndi kukhapa athu m,malo mokoza zithu zitsilu za wathu achoke atikwana
@user-sr6hc3pv8o
@user-sr6hc3pv8o Месяц назад
Waitha ase ma speach enawa sitimaaziwa
@ChikupizgaKajawaMkandawire
@ChikupizgaKajawaMkandawire Месяц назад
Kkkkkkkkkkkkkkkk Afford ikutenga boma boma lake litii azalamulira ku Rumphi konko ngati analephela Chakufwa chihana awa ndi andani
@ZahnJrBlack
@ZahnJrBlack Месяц назад
🤣 🤣 🤣 Koma afford nde yayaka moto DPP my vote APM
@SageSkeva-nr7kr
@SageSkeva-nr7kr Месяц назад
andale awa musatitole n tinatopa nazo kagwelen
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Месяц назад
Zoona achoke ameneyu kwakwana watizunza kwambili
@LeahNundwe-wh6vz
@LeahNundwe-wh6vz Месяц назад
Maloto a chumba aford kulowa my boma
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Месяц назад
Kuyankhula kwa phamvu.. 🔥🔥🔥
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel Месяц назад
Malizan chuma chachihanacho
@decemberjonathan3001
@decemberjonathan3001 13 дней назад
Aaa nde inu mudzakoza. Nde afford ndi chani? aaaaaa mudyereni enock
@samdiverson9733
@samdiverson9733 Месяц назад
Apm hope for Malawians
@jollylunda4034
@jollylunda4034 21 день назад
Wapenga
@ChawasoMlotha-ys6bf
@ChawasoMlotha-ys6bf Месяц назад
Zabvuta ndizo 😂😂😂😂
@ChikupizgaKajawaMkandawire
@ChikupizgaKajawaMkandawire Месяц назад
Awa oro atakiwa chotani sangawine ndipo sizizatheka
@lovesikwese
@lovesikwese 25 дней назад
Mwan'galula kkkk
@user-rg4du4vu9r
@user-rg4du4vu9r Месяц назад
Tell them the truth guys amarawi asukusura eya muzipanga choncho kuno kujoni anthu ndiwomwe amaramura boma osat boma kuramura anthu rimbani ntima amarawi chosani mantha timawopa murungu osat munthu nzako ayi
@BlessingsBanda-oh9kn
@BlessingsBanda-oh9kn 17 дней назад
Dpp boma limawakhara
@berthamigodi6529
@berthamigodi6529 Месяц назад
Kuyesa madzitu kumeneko kkkkk mcp ikuwinaso or tisafune
@WilfredYekha
@WilfredYekha 6 дней назад
Kkkk koma achewa muli m'madzi
@Johnybegood260
@Johnybegood260 Месяц назад
Mbava izi zimene zakamba ndit za nzeru
@khumalonyirenda4437
@khumalonyirenda4437 Месяц назад
Never Afford will not rule malawi unless otherwise, keep on dreaming
@YohanePatrick-lc2lq
@YohanePatrick-lc2lq Месяц назад
Achewa opusa awa atisawukisa amalawi sitdzakuvelani ayi
@muyabasamson
@muyabasamson Месяц назад
Kkkkkkk kk auzechilungamo
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel Месяц назад
Ndieno muli Kwa lukwa!?
@CyprianoSandalamu
@CyprianoSandalamu Месяц назад
Zabodza tu izi moti afford mungagwetse mcp?mwakhuta gagatu inu😅😅😅😅😅😅😅😅
@thomluciouss7360
@thomluciouss7360 Месяц назад
Ponyelani kwa Kuya a Malawi akuphula njelwa zamoto
@PeterChilombo-ou2cd
@PeterChilombo-ou2cd Месяц назад
aford yomweyo. moto bhooo
@AdamYas-ec9oc
@AdamYas-ec9oc Месяц назад
Kulangula muveka
@thamsonyusuf5789
@thamsonyusuf5789 Месяц назад
Chakwera mbuzi ya munthu sazalowanso komanso afford ili kutali ndi Boma
@mikesangano6624
@mikesangano6624 Месяц назад
Iwe Mangochi, usatinyase ndi chizungu chako choola chothyokatyhokacho... Iwe tilibe nawe ntchito ndipo sungatithandize. Ife ndi The DC's followers...wadya chisikono galu iwe ungotithera data bundle wopanda phindu iwe.
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 Месяц назад
Maloto a chumba kkkkk
@christophergibson72
@christophergibson72 Месяц назад
Afford muli kutali kwambiri
@YohanePatrick-lc2lq
@YohanePatrick-lc2lq Месяц назад
Dpp moto my vote is dpp
@spargomw
@spargomw Месяц назад
Ali nd maloto achumba awa, Afford ingawine? Hahahahaha akudzinyenga kwambiri
@spargomw
@spargomw Месяц назад
DPP woyeeeeeeeeeeeeeee❤❤
@innocentmusuli7380
@innocentmusuli7380 Месяц назад
Koma chaka chamawa kuli zinthu tandipitisireni uthenga kwa mzimayi wavala dress 👗 ya AFD ayambe kutumikira mulungu muli utumiki mwayiye
@SemionYotamu
@SemionYotamu Месяц назад
Kodi Aforld ndi chipani kapena club?? Fundo mukulankhuladi koma ku Malawi kuno sitikudziwani ndiye kaya mutani
@NilaGondwe
@NilaGondwe 12 дней назад
Malawi poison party tonse alliance ingotha
@AjeliMw
@AjeliMw Месяц назад
Sikut anthu alibe mantha ayi bro koma zonsezi ndi zoona coz sakuwanamizira zinthuzo zikuziyankhula zokha
Далее
Nyimbo iyiyi mwainvera koma?
6:48
Просмотров 270 тыс.
FARUX RAIMOV AVJIGA CHIQDI - JAVOHIR🔥
01:01
Просмотров 1,5 млн
Zaululuka kuti Chakwera wapha Chilima
7:56
Просмотров 70 тыс.
Ching'aning'ani comedy, ft Ngiringande
6:53
Просмотров 299 тыс.
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Просмотров 140 тыс.
ZOMWE AYANKHULA MAI KALIATI ndi MWANA WA LUCIUS BANDA
24:39
FARUX RAIMOV AVJIGA CHIQDI - JAVOHIR🔥
01:01
Просмотров 1,5 млн