Лучшее на RU-vid
Кино
Авто/Мото
Видеоклипы
Животные
Спорт
Игры
Приколы
Развлечения
Хобби
Наука
Авторизоваться
Зарегистрироваться
ACB LAPEZA KUTI BOMA LA MCP MWACHULUKA KATANGALE 🙌🙌🙌
26:42
Nyimbo iyiyi mwainvera koma?
6:48
FARUX RAIMOV AVJIGA CHIQDI - JAVOHIR🔥
01:01
He styled ME in HIS clothes 💗🥺 What do you think? Subscribe for #fashion ✨
00:18
I WAS TAKEN OVER 😱👀🫢 #shorts | Amalia Triple Charm
00:10
ВОЗВРАЩЕНИЕ В ДОМ ИЗ ПЛЕНКИ НА ДЕРЕВЕ 👻 | Элли Ди
29:31
ANTHU AYANKHULA ZOSAOPA AWA 🙌🙌🙌
HOT 265
Подписаться 62 тыс.
Просмотров 95 тыс.
50%
1
Видео
Поделиться
Скачать
Добавить в
Опубликовано:
20 май 2024
Поделиться:
Ссылка:
Скачать:
Готовим ссылку...
Добавить в:
Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии :
140
@Blessings-td4cr
Месяц назад
Zomatchula aleluya andale musiye!! Zikumatinyasa mulungu sapanga ndale.
@user-vl5on2lj8b
Месяц назад
Ambuye mulungu amphavu zonse tipaseni mfumu yotikonda mutisankhire ndiinu poti mfumu yomwe iripoyi zikuchukuluka nkhadza kuba kupha kuononga amen
@AndrewKwalingana
Месяц назад
Maloto achumba. Aford will never be the ruling party in Malawi. Mark my words
@user-uv5rf4zt5q
15 дней назад
Ndare sitimadya we need good leaders that can serve the people Malawi is the poorest country in the world lacking good leadership.
@edsonndalama2334
Месяц назад
Mpaka kunena kuti "ndi inu ndani akanyimbi inu?"
@SolomonNjolomole
Месяц назад
Fantastic speech guys ❤
@4tune07
Месяц назад
Aaaaaaaaa !!!! Zonama izi ngat chakwera mukuona kt akuononga dziko ndie kt inuso mukuon muli mgulu lowonga coz inuo muli momo mu TONSE ALLIANCE
@UthmanKapungu
Месяц назад
Moto ngati umenewo ndi umene tikufuna kuchokera Ku zipani zosusa fire!!!!!!!!!
@user-ti4yu6ob1e
Месяц назад
AFORD you deserve 2 points👍
@alfredkanyawire3524
Месяц назад
We are now fighting for democracy in a Democratic state kkkk embarrassing indeed
@MrMwambananji-tx8jt
Месяц назад
Sindimayembekezela, awo ndiye mau zabwino zonse more fire!!!
@stevendachuva1443
19 дней назад
Sure
@LysonMtalika-tb6fk
Месяц назад
Powerful!!!! 💪💪💪
@ReubenGama
Месяц назад
Mcp sidawinepo chisankho, boma iliri ndilatonse . Eee koma kuwaulatu
@user-do2cs8nf4b
Месяц назад
More fireeeeeee sister mwayankhula bwino kwabasi Mulungu akudalitseni❤
@PeterChilombo-ou2cd
Месяц назад
zoona wazuru sakwatira mkhonde yomweyo kkk
@clalesschisale3792
12 дней назад
Vuto lake amalawi sitimaiwala tiannyoza DPP kuti imatizunza osaziwa kuti omwe timawaika pampandowo ndiomwe akutizunza kuposa DPP
@user-bq5ev7de1l
Месяц назад
Apm my vote ✊
@georgemoffat5143
11 дней назад
aaaaa MCP moto🔊🔊
@blessingskutchuwi8635
Месяц назад
Uku ndye kuwawanyaaaa kwekweniiii....🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@StevenMbama
Месяц назад
Anthu a afodi iiiii amatha mbalume eishiii
@user-nf3ik3ff6y
Месяц назад
Simbiyamoto number one ❤
@user-nb2zz9ih1v
Месяц назад
From Capetown chakwera must go
@superiormoses4802
Месяц назад
Eee apa Moto walavulidwa hvy kugagada 🔥🔥🔥🔥
@user-vu6ec1le2b
Месяц назад
DPP + AFORD more fireeee!!!❤
@macdonaldblack3727
22 дня назад
Amayakhula ngati sanapiteko kusukulu kmnso akhangati sakudziwa zomwe zikuchitika muno Malawi zimvereni chisoni
@amoschataika7440
Месяц назад
Big up Afford kuswa kuswa basi.
@jollylunda4034
21 день назад
Achewa kuyerekedwa wakubvutani chakwerawanu
@abdulazeezchapita2159
Месяц назад
Anthu amayakhura eeeeee wandare usazamudelere
@samchibenene4458
Месяц назад
Mwayankhura mwamphamvu mayi
@user-it5zv2nz7f
Месяц назад
Koma ine ndawusa manja anthu chilungamo akuchisata🙌🙌🙌🙌
@paulpaseli6310
Месяц назад
Mai chilungamo muyakhuladi ulemu wanu. Zowona Ndithu
@nafejonga972
29 дней назад
Utm my vote
@SteveChirwa-ne9nt
Месяц назад
Nthawi yakwana Afford Moto !!!
@user-dl6ly7kk1y
27 дней назад
Ndikanakhala olemera bomali ndikalanda mwaupandu, Anthufe tanzuzika kokwana palibe chikusintha
@chrisboyce2
Месяц назад
Ndagwira mau amodzi akuti athu mu katopa simuyang'anaso za munthu kuti anali ndani zimenezi ndi zomwe zichitika 2025 DPP MY VOTE 💙
@AdamsMsosa
Месяц назад
More fire
@user-nc6cz4jn9r
Месяц назад
🔥 📛
@victor998vabatanazio3
Месяц назад
Don't trust in politicians you will get disappointed.
@gracemaluwa4674
4 дня назад
AFFORD YOMWEYO KUTI WAAAAAAA!!!!
@AngelaTsekula
8 дней назад
Andale in mukafuna boma mumakhala ngati muli kumbali ya ife anthu ovutika. Mukatenga boma kuyamba kukhala mmoyo ozikonda munthu akakususani kumuphano
@user-by4vy9hb6m
8 дней назад
Pajatu munkafuna boma lero ndi izi 😂😂 l quote MCP siinawineko boma, boma iliri nd la tonse alliance eeee anthu mwatopa ndi chilungamo😂😂😂
@ishmaeldama8906
Месяц назад
Malawi is the best in Africa, Aford mwayankhula, i think chakwera he must resine he failed, all the way from johannesburg cbd
@user-nf3ik3ff6y
Месяц назад
Kkkķkk Zoona ❤
@user-el8to1te3l
Месяц назад
Tikufuna anthu olankhila chochi osati kumaopa agalu mbava za mcp
@mavmsusa1310
Месяц назад
Anthu anawawata tu ku Mponela!!! Eish!!!
@MrBone-zj1wq
18 дней назад
Dpp is only my last hope not Aford
@MosesNyalugwe-ll8hh
15 дней назад
Zoona MCP sinavoteredwepo
@ronaldharawa
Месяц назад
Aford is not our hope. The first president comes from my home area but nothing cannot be shown they did even after being given 2nd vice presidency
@DONNEXKhama-bk1gy
Месяц назад
Koma chakwera Ufa ndi mtima Athu atopa nawe payakhulidwatu apa
@user-ky4ce9gb6j
Месяц назад
Ndipo kwambiri
@user-ky4ce9gb6j
Месяц назад
2025 tiona zinthu
@user-oq7hi3hd4p
Месяц назад
Madam menya menya chilungamo chioneke.
@RobertLuka-wy9cl
Месяц назад
Aford atha kugwesa mcp anthu atopa ndi mcp
@RobertLuka-wy9cl
Месяц назад
Bola achewa mazindikila 😂😂😂😂😂
@MonicatimanyeShaba
Месяц назад
Chihana yomweyo 😂😂😂❤
@user-ky4ce9gb6j
Месяц назад
Apm my vote
@masterchitabwino898
28 дней назад
Chilima my vote 2025
@JonathanMlongoti-wf6wi
Месяц назад
Following
@amoschataika7440
Месяц назад
😂😂😂 Koma Mdala uyu waswa Mr Chihana ndi a Ntambo yendani limodzi ndi Mdala ameneyu akudziwa kuyankhula.
@owenskabazanechiumia3543
Месяц назад
Zowona M'dala ameneyu amapalula mbalume, No mantha or Manyadzi iai ayende naye M'dala ameneyu pa Campaign imeneyi.
@YASSANWADO-jk4xp
20 дней назад
Km kumeneko kwachako bwino 😢😢😢😢
@decemberjonathan3001
13 дней назад
KKKKK kuililira mitsonkho yanthu kumeneku tiye nazoni vote ili mumtima mwanga kkkkkkkk
@isabelfatch1517
Месяц назад
EKC my vote
@user-tb6yh1kx3o
Месяц назад
Koma sister wake wa Ntambo zikomo
@ClementZintula-wi4tz
Месяц назад
Malawi true meaning of dziko lapasi
@user-gd3jx7tr1p
Месяц назад
Ana inu
@JerryChain-cz8ru
Месяц назад
Mkazi walankhula mawu
@MayamikoKalimapadzala-sw7yp
23 дня назад
Sitikuso mawu achionvwe ayi tikuna fudo zabwino achimwene ndale zonyozana zinatha kale kale
@maxwellmajawa6091
Месяц назад
Tamvanan nd Dpp ma guy muyatsa moto
@ThomasShuga
Месяц назад
Very true brPlease
@DOLOTHYMAKINA
Месяц назад
Zoona zake
@user-eh1mg3ww6d
Месяц назад
Ndipo ndizoonadi akulimbana ndi kukhapa athu m,malo mokoza zithu zitsilu za wathu achoke atikwana
@user-sr6hc3pv8o
Месяц назад
Waitha ase ma speach enawa sitimaaziwa
@ChikupizgaKajawaMkandawire
Месяц назад
Kkkkkkkkkkkkkkkk Afford ikutenga boma boma lake litii azalamulira ku Rumphi konko ngati analephela Chakufwa chihana awa ndi andani
@ZahnJrBlack
Месяц назад
🤣 🤣 🤣 Koma afford nde yayaka moto DPP my vote APM
@SageSkeva-nr7kr
Месяц назад
andale awa musatitole n tinatopa nazo kagwelen
@user-oc9vl9xz8e
Месяц назад
Zoona achoke ameneyu kwakwana watizunza kwambili
@LeahNundwe-wh6vz
Месяц назад
Maloto a chumba aford kulowa my boma
@eliffagondewe8214
Месяц назад
Kuyankhula kwa phamvu.. 🔥🔥🔥
@ChrifordBiziel
Месяц назад
Malizan chuma chachihanacho
@decemberjonathan3001
13 дней назад
Aaa nde inu mudzakoza. Nde afford ndi chani? aaaaaa mudyereni enock
@samdiverson9733
Месяц назад
Apm hope for Malawians
@jollylunda4034
21 день назад
Wapenga
@ChawasoMlotha-ys6bf
Месяц назад
Zabvuta ndizo 😂😂😂😂
@ChikupizgaKajawaMkandawire
Месяц назад
Awa oro atakiwa chotani sangawine ndipo sizizatheka
@lovesikwese
25 дней назад
Mwan'galula kkkk
@user-rg4du4vu9r
Месяц назад
Tell them the truth guys amarawi asukusura eya muzipanga choncho kuno kujoni anthu ndiwomwe amaramura boma osat boma kuramura anthu rimbani ntima amarawi chosani mantha timawopa murungu osat munthu nzako ayi
@BlessingsBanda-oh9kn
17 дней назад
Dpp boma limawakhara
@berthamigodi6529
Месяц назад
Kuyesa madzitu kumeneko kkkkk mcp ikuwinaso or tisafune
@WilfredYekha
6 дней назад
Kkkk koma achewa muli m'madzi
@Johnybegood260
Месяц назад
Mbava izi zimene zakamba ndit za nzeru
@khumalonyirenda4437
Месяц назад
Never Afford will not rule malawi unless otherwise, keep on dreaming
@YohanePatrick-lc2lq
Месяц назад
Achewa opusa awa atisawukisa amalawi sitdzakuvelani ayi
@muyabasamson
Месяц назад
Kkkkkkk kk auzechilungamo
@ChrifordBiziel
Месяц назад
Ndieno muli Kwa lukwa!?
@CyprianoSandalamu
Месяц назад
Zabodza tu izi moti afford mungagwetse mcp?mwakhuta gagatu inu😅😅😅😅😅😅😅😅
@thomluciouss7360
Месяц назад
Ponyelani kwa Kuya a Malawi akuphula njelwa zamoto
@PeterChilombo-ou2cd
Месяц назад
aford yomweyo. moto bhooo
@AdamYas-ec9oc
Месяц назад
Kulangula muveka
@thamsonyusuf5789
Месяц назад
Chakwera mbuzi ya munthu sazalowanso komanso afford ili kutali ndi Boma
@mikesangano6624
Месяц назад
Iwe Mangochi, usatinyase ndi chizungu chako choola chothyokatyhokacho... Iwe tilibe nawe ntchito ndipo sungatithandize. Ife ndi The DC's followers...wadya chisikono galu iwe ungotithera data bundle wopanda phindu iwe.
@inessmsiyambiri8517
Месяц назад
Maloto a chumba kkkkk
@christophergibson72
Месяц назад
Afford muli kutali kwambiri
@YohanePatrick-lc2lq
Месяц назад
Dpp moto my vote is dpp
@spargomw
Месяц назад
Ali nd maloto achumba awa, Afford ingawine? Hahahahaha akudzinyenga kwambiri
@spargomw
Месяц назад
DPP woyeeeeeeeeeeeeeee❤❤
@innocentmusuli7380
Месяц назад
Koma chaka chamawa kuli zinthu tandipitisireni uthenga kwa mzimayi wavala dress 👗 ya AFD ayambe kutumikira mulungu muli utumiki mwayiye
@SemionYotamu
Месяц назад
Kodi Aforld ndi chipani kapena club?? Fundo mukulankhuladi koma ku Malawi kuno sitikudziwani ndiye kaya mutani
@NilaGondwe
12 дней назад
Malawi poison party tonse alliance ingotha
@AjeliMw
Месяц назад
Sikut anthu alibe mantha ayi bro koma zonsezi ndi zoona coz sakuwanamizira zinthuzo zikuziyankhula zokha
Далее
26:42
ACB LAPEZA KUTI BOMA LA MCP MWACHULUKA KATANGALE 🙌🙌🙌
Просмотров 11 тыс.
6:48
Nyimbo iyiyi mwainvera koma?
Просмотров 270 тыс.
01:01
FARUX RAIMOV AVJIGA CHIQDI - JAVOHIR🔥
Просмотров 1,5 млн
00:18
He styled ME in HIS clothes 💗🥺 What do you think? Subscribe for #fashion ✨
Просмотров 1,4 млн
00:10
I WAS TAKEN OVER 😱👀🫢 #shorts | Amalia Triple Charm
Просмотров 2,9 млн
29:31
ВОЗВРАЩЕНИЕ В ДОМ ИЗ ПЛЕНКИ НА ДЕРЕВЕ 👻 | Элли Ди
Просмотров 131 тыс.
9:27
Tikati Munthu Waphedwa , Tima Tanthauza Izi | Katswiri Wina Wamalamulo Atambasula bwino .
Просмотров 58 тыс.
7:56
Zaululuka kuti Chakwera wapha Chilima
Просмотров 70 тыс.
8:45
Mafabi and Amuriat Fire Up Mbale Crowd as They Kick-Off Party Membership Registration
Просмотров 286
6:53
Ching'aning'ani comedy, ft Ngiringande
Просмотров 299 тыс.
5:19
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
Просмотров 140 тыс.
24:39
ZOMWE AYANKHULA MAI KALIATI ndi MWANA WA LUCIUS BANDA
Просмотров 17 тыс.
30:46
SHOCKING! Watch how Ruto Apologize On Behalf Of Murkomen and Ichungwa On X SPACE Twitter
Просмотров 499
11:56
Timothy Mtambo wapita ku AFFORD; Wadzudzula Chakwera kwa Chinsapo; 1 May 2024
Просмотров 35 тыс.
35:04
Abagenze Enamibia Bakatutemye! Tetumanyi Oba Kabaka Mulamu
Просмотров 15 тыс.
30:03
Fr, Elizeo Nthalika:::wa mpingo wakatolika akupitiliza kung'alula MCP_ _Ana okula ntima
Просмотров 15 тыс.
01:01
FARUX RAIMOV AVJIGA CHIQDI - JAVOHIR🔥
Просмотров 1,5 млн