Тёмный

BON KALINDO LERO PA 12 JULY 2024 | KUPITILIRA KUNG'ALURA | 

DZIWE TV
Подписаться 25 тыс.
Просмотров 32 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

10 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 148   
@ChikondiKachaso-ox5ng
@ChikondiKachaso-ox5ng 23 дня назад
Bon kalindo amalankhula zoona zokhazokha koma anthufe timangoti ndi wama comedy let's support him as malawians
@loycekachy3370
@loycekachy3370 22 дня назад
Wamisala anaona nkhondo,,lero Bon kalindo mukumuyamikila koma mmene munkamunyozela siizi😂😂😂😂
@StanleyChirwa-d6b
@StanleyChirwa-d6b 23 дня назад
Ati amakutengan ngat manyi😂😂😂😂 chi booooniiiiii kalindoooo
@stelladolizyi
@stelladolizyi 23 дня назад
Kuyankhula mopanda mantha ngati wakhalira mfuti Bon kalindo 😮😮
@OscarChizula-qr4bi
@OscarChizula-qr4bi 23 дня назад
Ndpo inu
@user-dn9mb9mb9o
@user-dn9mb9mb9o 23 дня назад
Thanks sir for ur update
@KhondanKhondan
@KhondanKhondan 23 дня назад
Kalindo amatha kwambili❤
@DarlingtonKamando
@DarlingtonKamando 22 дня назад
Your the best the DC bon kalindo❤
@JonesMwera
@JonesMwera 23 дня назад
Uyu ndiye activits yemwe timamudziwa, Bon kalindooooooo!! Mwana owopsa kwambiri.
@TaongaChibuwu
@TaongaChibuwu 22 дня назад
Zikomo bwana DC UTM yitulukedi kumeneko iyime pa yokha basi
@AubreyTrust
@AubreyTrust 23 дня назад
God bless you Kalindo
@BlessingsPhiri-fv5gs
@BlessingsPhiri-fv5gs 23 дня назад
Umakwana
@user-ss4se9hf7x
@user-ss4se9hf7x 23 дня назад
Always your the best all the time mr president Bonie Kalindo
@MaxWell-d7o
@MaxWell-d7o 22 дня назад
Yomweyo fadaa🎉
@fosternyirenda-wo4eb
@fosternyirenda-wo4eb 23 дня назад
Good advice sir.
@PatrickSomanje
@PatrickSomanje 23 дня назад
U always stand in true mr Bon l love u more than
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 23 дня назад
Utm siingatuluke mugwilizano ngakhaleso atatuluka palibe chazelu chomwe angapeze
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v 23 дня назад
Komatu bon kalindo amayakhula ngati wamisa koma ndizoonadi zimene amayakhula anhtu inu muzichenjera
@ellensambo6323
@ellensambo6323 22 дня назад
Uyu ndiye ❤
@TamalaMwamlima-gk5im
@TamalaMwamlima-gk5im 23 дня назад
Chilungamo chimamasula go ahead the DC
@KondwaniMwasinga-rs6kv
@KondwaniMwasinga-rs6kv 22 дня назад
Born kalindo🔥🔥🔥🎷🎷
@OscarChizula-qr4bi
@OscarChizula-qr4bi 23 дня назад
Salute
@user-eu4ud2qc6p
@user-eu4ud2qc6p 22 дня назад
Mr Kalindo mukutitsegula mmaso kwabasi keep it up
@anicakandiado
@anicakandiado 23 дня назад
Kulankhula mwachilungamo. UTM tsegulani maso. Tulukani mu tonse alliance monga akunenela Bon Kalindo please. A MCP asakupusitseni ife tili mbali yanu ndi SKC osaopa, osatopa, osafooka 💪
@BlessingsMpondaphiri
@BlessingsMpondaphiri 22 дня назад
Good advise Mr born kalindo thank you 😅
@antiepogba1534
@antiepogba1534 23 дня назад
The DC mwana ohopya kwambili
@AlbertEngelbercht
@AlbertEngelbercht 23 дня назад
Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
@greymasha838
@greymasha838 23 дня назад
Bwana DC mumatiimilira
@HawaHussein-d4l
@HawaHussein-d4l 22 дня назад
Mumaitha bwana d c ndi more pachilungamo😊
@GoodsonfahardMaganga-qc2qk
@GoodsonfahardMaganga-qc2qk 23 дня назад
Big up to you 🎉🎉🎉🎉🎉 umatha kung'alura
@user-cd4df3vg4y
@user-cd4df3vg4y 23 дня назад
President wathu wathu,Mr Kalindo lero ndilomwe tidziwedi kuti UTM ipitilira ndipo SKC waphera chilungamo.
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r 23 дня назад
DC Huma kwana
@SmileMalanda
@SmileMalanda 22 дня назад
The DC🔥🔥🔥
@SanudiKambona
@SanudiKambona 22 дня назад
I love you so much
@fahadmilanzi
@fahadmilanzi 22 дня назад
Kalindo amalankhula zoona uyu ndi mpulutsi.
@valenceemmanuel74
@valenceemmanuel74 22 дня назад
Like this guy or not , but he is very sharp
@ChristopherChimbalanga-ez5he
@ChristopherChimbalanga-ez5he 23 дня назад
Kmat uyu tiyen Tzimuvela zimene amayankhulaz
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 23 дня назад
President wathu Mr DC
@user-hc8gr4pg4g
@user-hc8gr4pg4g 22 дня назад
In short Utm ibwerere ku DDP....tigwetse vinyau tikinze dziko
@macfordmbama7862
@macfordmbama7862 23 дня назад
Good advice
@WestonGawaza
@WestonGawaza 23 дня назад
Bon kalindo akunena zowona lelo muchoke ku mcp mukapitiliza ndiye kuti mukusangalala ndi ife ya chilima chipani chimene chingawine ndi UTM kampeni wake zikolose lapasi lipanga saport
@user-oq8uv9xi5s
@user-oq8uv9xi5s 22 дня назад
🎉🎉🎉 following
@LenoMvula
@LenoMvula 23 дня назад
My vote kalindo umatha umatiimirila
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 23 дня назад
Koma Mai kaliyati ndi kagulu kanu choonde nvelani kulira kwa anthu ngati ku UTM kuli anthu olimba nde ndinuyo mumakhala chifupi ndi Chilima musakomedwe ndi ndalama mukwiitsa anthu ochuluka nthawi yatha kale iyi musanvere MCP kukunyengeleleni ndi ndalama misozi ili manso ndithu mutenga tsoka
@MathewsChitambe
@MathewsChitambe 23 дня назад
Zoona mb'ale
@AlinafeSolomoni
@AlinafeSolomoni 23 дня назад
True
@ListonFrancis
@ListonFrancis 22 дня назад
Mbambande Bon Kalindo
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 23 дня назад
Musapusisidwe a utm mcp sichipani .muzifunse kuti kodi chilima chamupha ndichani kodi mukugona a utm, tsegulani mumaso
@AhmadShariff-bk3rr
@AhmadShariff-bk3rr 23 дня назад
Tiyeni tiyeni tiyeni Mr DC
@WestonGawaza
@WestonGawaza 23 дня назад
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
@PempheroAlufandika
@PempheroAlufandika 22 дня назад
Mumatiimilira a bon
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s 23 дня назад
A UTM uthenga ndiumeneo zili ndiinu kunyalanyaza kapena kutengapo kanthu km mawa pangatalike muzawakumbukira mau a Bon sadutsa pachabe
@AndreaSignala-hk2yg
@AndreaSignala-hk2yg 23 дня назад
It's true bwana president woyamba wa anthu osauka muno Malawi
@willardkajalika-m8g
@willardkajalika-m8g 22 дня назад
😹😹😹 iwe umakwana aaa nilinje mau
@MerryWayson
@MerryWayson 23 дня назад
Na pa Bone Kalindo palibeso same same Mtanyiwa anthu awa amanena chilungamo chokhachokha
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 23 дня назад
Ndipo a mcp ndi athu ochenjela ndi kuipa komwe ndipo chilima amusasa lelo akuyanja otsalao mukapusa akumezani
@HassaniHassani-yr2rf
@HassaniHassani-yr2rf 23 дня назад
THE DC PANGOLINI 💪💪💪💪💪
@MaxwellMakoka
@MaxwellMakoka 22 дня назад
Mr DC 2025 woyyeee.
@MaxwellumbiriLumbiri
@MaxwellumbiriLumbiri 22 дня назад
Bon kalindo umakamba zoona
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl 23 дня назад
Chilungamo ndimwano❤ The DC pick up man
@jeladiaustain
@jeladiaustain 22 дня назад
❤❤❤❤❤❤❤
@ArnoldKamanga-r6k
@ArnoldKamanga-r6k 22 дня назад
Tikumupemphani a Born kalindo bwelelani ku UTM please
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage 22 дня назад
Ndipo president akakhale iyeyu ndimunthu wamaso mphenya❤❤we love him❤
@SolomonMbewe
@SolomonMbewe 23 дня назад
DPP+UTM+UDF+AFORD.... MCP out 2025..
@AndrewMbewe-yp7kg
@AndrewMbewe-yp7kg 23 дня назад
Usazafe kalindo uzangotsowa ngati eliya
@LottiAffati
@LottiAffati 22 дня назад
kalindo umakwana ase
@alexmkolongo3089
@alexmkolongo3089 23 дня назад
Koma manganya asamuwelengele ndiwa MCP kuyambila kale
@yamikanikamboyi8686
@yamikanikamboyi8686 23 дня назад
The DC
@FrankAndsen
@FrankAndsen 23 дня назад
Khan nd yoona
@MuhammadSamson-yz1kl
@MuhammadSamson-yz1kl 23 дня назад
A UTM mukapanda unvera za bon kalindo muzalira moyo wanu onse
@InnocentMatemba-y1k
@InnocentMatemba-y1k 23 дня назад
Big up de DC our pool p
@MathewsChilenje
@MathewsChilenje 22 дня назад
Umaitha bon
@TalazanGamah
@TalazanGamah 23 дня назад
Powerful spetch
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem 23 дня назад
Our freedom fighter ndiwe kawawa ndithu
@user-fz3gu2ez1o
@user-fz3gu2ez1o 23 дня назад
Tidziwe basi. Ma traitor tiwadziwa lero
@OwamiSimeon
@OwamiSimeon 23 дня назад
Kalindo more 🔥 ❤
@PeterMalizan
@PeterMalizan 23 дня назад
The DC mulomwe wathuwathu odziwa zinsinsi
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel 23 дня назад
Palibepo zomwe mukulusapo zazelu zimodz modzi zosavekaso mkomwe
@BlessingsMikeyasi
@BlessingsMikeyasi 23 дня назад
The DC ,lankhula chilungamo bas
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 23 дня назад
The DC agogo anga akufuna azakuoneni
@user-bf1sz6pu1n
@user-bf1sz6pu1n 23 дня назад
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
@BlessingsMaheya
@BlessingsMaheya 22 дня назад
Sanena boza uyu
@PachaloShaba-pf5vw
@PachaloShaba-pf5vw 23 дня назад
Umakwana winiko
@Martha-m6e
@Martha-m6e 23 дня назад
Mzimu wa bwana Chilima uwavuta.mukaone maruwa ngati akukanika kufa .musamale kwambilitu.
@user-qq1uj7ct6n
@user-qq1uj7ct6n 22 дня назад
boooooon kalindo!
@khuzenigunya
@khuzenigunya 23 дня назад
Kalindo good advice
@chifundobuledi
@chifundobuledi 23 дня назад
🎉More fire!!!!!!!!!!!
@AgnessMzengo
@AgnessMzengo 23 дня назад
Wise man
@amfanamane
@amfanamane 23 дня назад
My vote umakwana
@Moses51
@Moses51 23 дня назад
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉
@WestonGawaza
@WestonGawaza 23 дня назад
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 23 дня назад
Gwilizano a mcp adayedzeka amamukana chilima dzuwa likuswa mtengo achakwera kumayankhula zonyazitsa chilima Ali pompo chilima sanapuse sanayambane ndi munthu ndie lero zatani RIP chilima.
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 23 дня назад
Ndipo ndizoonadi amamukanadi chilungamo ndiye lelo ayanja otsalao
@MaryPanje
@MaryPanje 23 дня назад
Makwana mr keep it up
@Mussa-qs7km
@Mussa-qs7km 23 дня назад
Good Good news
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 23 дня назад
The Dc bon kalindo ❤
@Zamwano
@Zamwano 23 дня назад
Kd zimenez zitithandiza osapita pa galaundi kukapanga ma demo ngati tikuona kuti zithu sizilibwino,, Timakunyadilan mr DC,Km please dziko ndilathu tiyeni tipange zaku Kenya 🇰🇪 basi
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 22 дня назад
Mmm
@BensonChakalamba-db7uf
@BensonChakalamba-db7uf 23 дня назад
The problem is anthu akumudz unthengawu suwapeza cz of social media
@user-ei2yt3kf4x
@user-ei2yt3kf4x 22 дня назад
The DC kkkk konda u ife
@MussaAmadu-o9f
@MussaAmadu-o9f 23 дня назад
Very true
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 23 дня назад
The DC mwana oopsa kwambiri satekeseka ndi Uniform ya a police,ingankhale Unyolo. Tell them 😅😅😅😅
@OsumaniJaffali
@OsumaniJaffali 23 дня назад
Amakwana koma ❤
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 23 дня назад
Mbuzi iwe takudziwa akutuma adpp chitsilu chamunthu DPP UDF aford zonse izo palibe ndimakampani amabanja
@KelvinNamowa
@KelvinNamowa 23 дня назад
The DC😊
@3FinerDachudua
@3FinerDachudua 23 дня назад
Mumakwana bwana born kalindo
Далее
BON KALINDO  LERO PA 3 AUGUST  2024 |
16:32
Просмотров 34 тыс.
БАТЯ И СОСЕД😂#shorts
00:59
Просмотров 1,3 млн
Schoolboy - Часть 2
00:12
Просмотров 1,8 млн
ACHAKWERA AWAPANA KUTI ATULUTSE REPORT  YA NDEGE |
8:51
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 58 тыс.
NKHANI  MADZULO APA 3 AUGUST  2024 |
20:47
Просмотров 9 тыс.