chabwino born kalindo akupanga ndale komano fact zomwe akunena zikuchtika en ambiri tikuona koma mantha kuyakhula hahah salute to yuh the DC born kalindo
Nkhani zonse zamveka ndipo Ambuye azikusungani ndi moyo wautali. Dzikoli likuonongeka ndi anthu ophunzira komanso opembedza osaiwala amaudindo. Anthu ochuluka ali mu umphawi wa nyoooo koma sangalankhule chifukwa alibenso ufulu wolankhulawo. This is why Christ is to come adzapereke makofi ndi mateche plus mambama kwa anthu tonse oipa, ozunza, ankhanza. Akubweratu ndipo si kale owowo
Mmatiuza zoona , izi ndi zeni- zeni maka za ku mapasipoti mukutiuza chilunga. Komatu Chakwela nda agulu anzakewo azafera kutulo , boma lankhaza ndi kuba, Chakwela must gooooo!
Nde maganizo amneoo mudachedwa nawo coz pakatipa pa dutsa anthu awiri peter nd ndi mzake nde mukalakhula lero chifukwa Cha chakwera aaaaa muzikhla nd umunthu osangoti kukhla nd Kwa ulere ai