Тёмный

phuzitsi wina wa school yosula aphuzitsi wapeza nkazi emwenso ndi phuzitsi akupanga zadama. 

Balanço semanal CK & Govate
Подписаться 19 тыс.
Просмотров 79 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

11 авг 2022

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 65   
@AndrewPilliotmw
@AndrewPilliotmw Год назад
Vuto ndi mamunayo........ Anyway watching from Maputo (koma ndine mmalawi ndithu)
@helderdias5523
@helderdias5523 Год назад
Me too
@kelvinskada5619
@kelvinskada5619 4 месяца назад
Two bad, watching from malawi
@fineenemy2045
@fineenemy2045 Год назад
Language is clear komano zudabwisa mainawo koma mwat ndiku malawi uku?
@kairaruphan2639
@kairaruphan2639 Год назад
Akuti Mozambique osati malawiyi
@Envanceabwinobamusieli-sf9tt
Koma atolakhan ku Mozambique mukugwira ntchito yotamandika mpaka kutiwonesa stadium 😂😂😂😂
@zainabchikakuda8764
@zainabchikakuda8764 Год назад
Komatu. Kulakwa chommenyera mwamuna wako nchiyani nzimayi oipa ukupha mwana waeni 😭😭😭
@confidencebanda109
@confidencebanda109 Год назад
Mayi uyo ndiwolakwa bola akanathesa banja za uhule wake akanapangila pa nkhomo pa makolo ake fro malawi
@PaulokossimasiPaulo
@PaulokossimasiPaulo 24 дня назад
😂 hulem nkayo
@mayeserokaponya5196
@mayeserokaponya5196 Год назад
Man banja losagwirizira ili nawenso ndiwachibwezi basi zatherana Malo ndi awana
@MzikaPhiri
@MzikaPhiri Месяц назад
Akacheza amamwa eti kkkkk
@chicco2294
@chicco2294 Год назад
Mainawa akuti bwanji?? I didnt know ku mosco mumalankhula Chichewa choncho
@user-ez7th2rv7g
@user-ez7th2rv7g 7 месяцев назад
Thanks for the update
@ernestbwanalisauteni3483
@ernestbwanalisauteni3483 Год назад
Kkkkkkkkkk zosokonezeka kkkk
@chippiephiri4505
@chippiephiri4505 Год назад
Mamunayi ndiwopoyila
@westonnsulupi4056
@westonnsulupi4056 Год назад
From Malawi
@grantmachira9668
@grantmachira9668 Год назад
Mayiyo ndiwosalakwa amadzilimbikira ekha abambowa angothetsa banja basi but it seems mkaziyo ndi bread winner mkazi malo anagula yekha
@lamackbanda6869
@lamackbanda6869 Год назад
Olakwitsa ndi mamunayi zinthu zonsezo zimachitikazo opanda action kuonesa. Nkhani yamalilo inaliso yayikulu olo sanayithambasule. Komaso zimayiyu sanatenge ndalama ku bank koma zimuna akewo ndi amene amamanga nyumbayo. Naye mamunayo ofafusa kuti ndalama akuzithenga kuti zomangila nyumba kumangoyang'ana zimamutsangalasa
@victorsmbewe4816
@victorsmbewe4816 Год назад
Emotional damage 🤕🥴😜
@LimitedMolotali
@LimitedMolotali 2 месяца назад
Nkaziyo ndihule aphesa amuna
@zakeyophiri4308
@zakeyophiri4308 Год назад
Pls inuyo nkhani zina muziysa Kubisa nkhope kapena azalankhula atayang.ana kumbali chitsazo nkhani ya mnyamata akuti anapeleka mimba kwa mtsikana kapena mtsikana uja amene chifukwa media imapita patali tidzalephela kumufusila kapena kukwatiwa adzati ena anampatsa kale mimba
@ndazionaanastasiaannaphiri4843
Palibe chabwino zonse zolakwika mkazi yo nde worsen
@Xtar_deadlol1
@Xtar_deadlol1 Месяц назад
Za ziii kusowa zotola nkhani Chan
@josuahkachali1489
@josuahkachali1489 Год назад
From Malawi but am stay in Kuwait
@jamesselemani1003
@jamesselemani1003 Год назад
Oky
@peterbanda7003
@peterbanda7003 Год назад
Osamusiya bwanji
@lamackbanda6869
@lamackbanda6869 Год назад
Ntchito yapamwamba guys mumayitha♨♨♨♨
@chembachilemba7623
@chembachilemba7623 Год назад
Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi
@ngendahayososthene1398
@ngendahayososthene1398 Год назад
bambo inu ndi inu opoyira zedi.
@floramtiwa211
@floramtiwa211 Год назад
Koma ma statement akusiyana mwamunayu akuyankhula mosiyana ndiazimayi aja
@smithelectro-plumb2994
@smithelectro-plumb2994 Год назад
Kodi akulankhula chilankhulo chanji guys
@joebrown1158
@joebrown1158 Год назад
In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?
@balancosemanalckgovate8464
@balancosemanalckgovate8464 Год назад
of cause
@chifundoalfred14
@chifundoalfred14 Год назад
Mozambique
@chancyutekakayala2445
@chancyutekakayala2445 Год назад
May someone assist me Kodi zikuchitika ku dziko lanji izii komanso nchiyankhulo chanji
@Envanceabwinobamusieli-sf9tt
It's chichewa in Mozambique 🙄
@promise3693
@promise3693 Год назад
Kulakwa🤔
@bosconthandala9905
@bosconthandala9905 Год назад
👀 from malawi
@zecamariosandifolo8535
@zecamariosandifolo8535 Год назад
Malowo ngakhale atakhala kuti nyumbayo anagula ndi iwowo komabe ali pa banja nyumbayo ndiyawose basi
@luciajames604
@luciajames604 Год назад
It's Mozambique
@balancosemanalckgovate8464
@balancosemanalckgovate8464 Год назад
Yes
@tadalaimwa394
@tadalaimwa394 Год назад
Ndemwati ndinu amalawi? I really wish to visit and learn more about this place
@zexndaomba3011
@zexndaomba3011 4 месяца назад
Samalawi this is angonia
@zaithwachiwaya8885
@zaithwachiwaya8885 Год назад
Kom nkhaniyo mamunai zikuoneka kut malo sanagule nao.Komaso zimaiyo ndi uhule lothelatu zochitisa manyanzi zed
@zaithwachiwaya8885
@zaithwachiwaya8885 Год назад
Kom saname nkhaniyi kadakonda mukanamuonesa mzimai wa chigololo yo timuone kkkkkkk
@simangodickson1794
@simangodickson1794 Год назад
Mahule , Mabanja oyambila mvitsamba
@paulmgombebanda-mr19sate
@paulmgombebanda-mr19sate Год назад
Zovuta izi
@DelcidioDiogoPedro-ir9ni
@DelcidioDiogoPedro-ir9ni Год назад
Nkazio ntanbuali
@osamabinraden9391
@osamabinraden9391 Год назад
Mabanja akenso ndendi achi'chainatu
@eliasfaunteni6849
@eliasfaunteni6849 Год назад
Mchifukwa chake timanena kuti akaziwa tikawamphunzitsa amachuluca mzelu zovetsa chisoni kwambiri
@jessienkhoma2492
@jessienkhoma2492 Год назад
Koma ndi ku Malawi kapena Mozambique?
@kalimawandale7161
@kalimawandale7161 Год назад
Mozambique
@lucysimbani3971
@lucysimbani3971 Год назад
Zosankhala bwino ayi
@nemamoleni3041
@nemamoleni3041 Год назад
Ati agulitse malo ndalama agawane?? Zosakhala bho
@memorymalikita3628
@memorymalikita3628 Год назад
Where exactly is this sad news happened
@mtimbasonjojailos5106
@mtimbasonjojailos5106 Год назад
Mozambique iyi
@joebrown1158
@joebrown1158 Год назад
So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?
@joegibsonzulu2599
@joegibsonzulu2599 Год назад
It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.
@shariffalick796
@shariffalick796 Год назад
Kodi mayina akuchulidawa ndi ku malawi ?
@balancosemanalckgovate8464
@balancosemanalckgovate8464 Год назад
ayi, koma kalipentalayo
@chifundoalfred14
@chifundoalfred14 Год назад
Mozambique
@chifundoalfred14
@chifundoalfred14 Год назад
Mozambique
@user-gu4kk2bt4h
@user-gu4kk2bt4h 9 месяцев назад
Penço nr d BS de Whatsapp
@balancosemanalckgovate8464
@balancosemanalckgovate8464 7 месяцев назад
865112269
Далее
🎙СТРИМ на 4 МИЛЛИОНА🍋
3:12:45
Просмотров 1,3 млн
УРА! Я КУПИЛ МЕЧТУ 😃
00:11
Просмотров 810 тыс.
Bon Kalindo 28 JULY 2024 KUNYENYA KWA PA SUNDAY
14:57
ANA NDI  ACHIBALE A ZIMAYI WADZUKA KUMANDA KULONGOSOLA
10:02
ZAMALOVE   Episode 25 FINALE
37:28
Просмотров 35 тыс.
🎙СТРИМ на 4 МИЛЛИОНА🍋
3:12:45
Просмотров 1,3 млн