Тёмный
No video :(

Zomwe wayankhula Michael Usi Lero atangofika mu Mzinda wa Blantyre 

Makosana
Подписаться 80 тыс.
Просмотров 21 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

25 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 125   
@benardisaac1986
@benardisaac1986 Месяц назад
Nyengo ndizosintha manvuto sankha moyo wose wamunthu koma Dr usi all the best
@user-zs6qc9dx8s
@user-zs6qc9dx8s Месяц назад
We all know kut anthu omwe avala makaka a UTM nd a MCP. Eni eni a UTM sitikupanga nawo zopusazo.
@JonesSiliya
@JonesSiliya Месяц назад
Zoona akufuna kupusitsa
@JonesSiliya
@JonesSiliya Месяц назад
Chilima nzake amane amakambilana naye ndi ndani nanga nthawi imene amakusekani pakamwa ndindani
@giftmasenti5732
@giftmasenti5732 Месяц назад
Manganya ndi wa MCP kuchokera kalekale
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 Месяц назад
Michael usi is a matured intellectual who doesn't entertain nosense.
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 Месяц назад
Wachepa nao u vice president.waiwala imfa ya skc.
@LukeKalima
@LukeKalima Месяц назад
@@paulnyondo7572 aaaaaaaaaaa imfa ya skc ndiyotani anthu samamwalira kodi kapena munamuphera dala kuti muzipangira ndale imfa yake, kodi maliro akwanzanutu amaphweka chomchi akadzakhala akwanu zidzakuwawa kuti anthu azidzaseweretsa dzina la malemuwo
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 Месяц назад
Ndimaona ngati adziyankhula zogwira mtima
@moyowrobert3331
@moyowrobert3331 Месяц назад
zoti akumanga thumba ngati Mphaka sukuziwa
@hastingskalambo8502
@hastingskalambo8502 Месяц назад
Ndekuti zoti UTM yatuluka ku alliance iyeyo sakudziwa
@JacobKasalika
@JacobKasalika Месяц назад
UTM ndimaikonda komano tikudzibalalitsa yokhatu.Uyu ndinthu ndinyamata wa SCK
@LukeKalima
@LukeKalima Месяц назад
Wandisangalatsa usi sakupanga nawo za mtopola ena achita manyanzi kumeneko ndiye kulankhulatu ambuye akudalitseni dr usi
@sanddaniweck2703
@sanddaniweck2703 Месяц назад
Zangongole ife tilibenazo ntchito nkhani musise zinthu zakwela kwambili coz za Neef zo anthu ena akumamizi kwina salandila koma mukasisa zinthu anthu onse athandizika
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o Месяц назад
Mbuz yamunthu iyi yudasi ife a Utm zopusazo ayi sitikupanga nawo
@LeviBlackson
@LeviBlackson Месяц назад
Anthu sakumudziwa Kodi ku Blantyre kapana amapanga sewero
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j Месяц назад
Ngongole imeneyi udzabweza ndiwe . Fataleza udula konseko
@samchibenene4458
@samchibenene4458 Месяц назад
Seriously
@Jane-qb5qf
@Jane-qb5qf Месяц назад
Amalawi look sharp amalawi tilindivuto akati uku komweko uku komweko lekani timapemphera kukhala ndi chiganizo chokhazikika zimandimvesa chisoni kwambiri tisinthe mindset plz plz tizagwa chagada ndikati ndione amazayesa zida kuti kuli bwanji uku aaaa kaya Malawi
@SifatiMoses
@SifatiMoses Месяц назад
Muli mbali iti kodi Fada
@user-nu1dj3jh7b
@user-nu1dj3jh7b Месяц назад
Palibe azalande m'dalitso wamunthu, Dr usi ndiodalitsika muzonse komanso olimbika.
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi Месяц назад
Koma bwanji sanavale makaka
@footballhighlightsofficial7248
@footballhighlightsofficial7248 Месяц назад
​@@FrancisNyayiamugula a MCP
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 Месяц назад
​@@FrancisNyayitikufuna chitukuko osati makaka
@user-dv6rt6vb6e
@user-dv6rt6vb6e Месяц назад
Kusangalalila imfa ya mzawo
@joeldaniel-pc3ij
@joeldaniel-pc3ij Месяц назад
Mwapatsa anthu a MCP ma uniform a UTM kuti aziti chani?
@LeniaJosophat
@LeniaJosophat Месяц назад
Mukutipatsirazi ndizabwino zeedi koma you need to fix the sound kuti zizikomabe( this is the VP)
@user-vb1iq5un5p
@user-vb1iq5un5p Месяц назад
Kodi Usi ulimbali iti?. Koma umphawi luMalawi ukupepeletsa azibambo...
@VeronicaYohane
@VeronicaYohane Месяц назад
Mudyelen bambo wasikono akabwela osadziwa kuyankhula odvala madiresiyo
@JuniorKalipinde-gy7dx
@JuniorKalipinde-gy7dx Месяц назад
Usaone ngati ndi bugwe LA adla limenelo akupweteka
@johnbakali27
@johnbakali27 Месяц назад
Kodi iwe ukumenyera kampeni ya mco kapena UTM?
@user-hh4xg4hf2k
@user-hh4xg4hf2k Месяц назад
Enafe tisayankhire
@JonesSiliya
@JonesSiliya Месяц назад
Mwachedwa ndi chilima simunapange chifukwa chiyani
@FrankidEugenio
@FrankidEugenio Месяц назад
Ndale zayambika,Malawi ayiwale zambuyo.😂
@user-dv6rt6vb6e
@user-dv6rt6vb6e Месяц назад
Umbuli suzatha anthu munayambila kunamizidwa muja zilero changamukani
@constancemkandawire7378
@constancemkandawire7378 Месяц назад
You can't say that you love God if you don't love your nearby that's a total lie.You have failed to come together with your fellow utm members mukuti phala lomwe likudumpha mu mpoto lidumphe meaning you don't care ,ayi zikomo
@user-ni4nw1ee2f
@user-ni4nw1ee2f Месяц назад
Mwschedwa nayo ngongoleyo bwana kkkkkkk nyimbo ikhale ya mpaka malilo vinyo watha
@user-yq1mc3nm1f
@user-yq1mc3nm1f Месяц назад
Dziko la Malawi lafika pa uchitsiru weni weni
@JuniorKalipinde-gy7dx
@JuniorKalipinde-gy7dx Месяц назад
Ndipo live
@CHRISSYBALALIKA
@CHRISSYBALALIKA Месяц назад
Tasisani fertilizer zinthu zisike agalu inu muona muwina mosavuta
@RossanaMitha-tl9in
@RossanaMitha-tl9in Месяц назад
Kodi akuti kwabwela ndani ?😂😂😂😂
@lumbaninyirenda8223
@lumbaninyirenda8223 Месяц назад
tamangopitani muzikapanga ma drama,mfundo palibe apa
@ChrisjuZiyaya
@ChrisjuZiyaya Месяц назад
Chizindikiro choti Usi siwa utm onani zomwe zavalidwazo , zomwe Malemu Sks sadapangepo. Tikufuna m'tsogoleri wa serious not this gys.
@user-kg5lf6bd1g
@user-kg5lf6bd1g Месяц назад
Lelo akunamizila chilima lelo ndi mbuzi yamunthu
@genesismbewe
@genesismbewe Месяц назад
genius
@jedoforsure2842
@jedoforsure2842 Месяц назад
Umakwana us
@joekamphulusa4767
@joekamphulusa4767 Месяц назад
Chitsilu chenicheni ichi watenga athu a mcp kumati a utm 🚮🚮🚮
@footballhighlightsofficial7248
@footballhighlightsofficial7248 Месяц назад
Missing Chilima Already😢
@MlecheFatch
@MlecheFatch Месяц назад
A manganya mmmh
@enockharry8039
@enockharry8039 Месяц назад
koma izi wina aziona
@joma5327
@joma5327 Месяц назад
champhamvu kopasa kale kuthanthauza chani
@KondwaniNdobvie-f4v
@KondwaniNdobvie-f4v Месяц назад
Komatu adzake afanazo
@user-qu9ww1cd1y
@user-qu9ww1cd1y Месяц назад
Anamizana zokuti akope Southern Region
@ellahmvula
@ellahmvula Месяц назад
Hahaha awa a mcp achina Eliza avala za utm
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Месяц назад
Wakupha iwe manganya
@AbdulrahimoMassamba
@AbdulrahimoMassamba Месяц назад
Satan ndiyemwe ali kutsogolo kwakoyo
@RobertChisenga-ci2mq
@RobertChisenga-ci2mq Месяц назад
BT chitsilu2 paja
@MerySaid-uw3cm
@MerySaid-uw3cm Месяц назад
Tikufelanji
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Месяц назад
Iweyo ukuti ukufuna ulongo sole, ndimaesa UTM yatuluka mungwirizano ukufuna kupusisanso Wanthu
@user-rs7vx6hc1k
@user-rs7vx6hc1k Месяц назад
Basi tizingokhalira ma handouts mpaka liti abale?
@NkosDysonNkosDyson
@NkosDysonNkosDyson Месяц назад
Tangotsitsani fertilizer muonanso mudzawina mosavuta ife amalawi sititichedwa kuiwala
@charlesmasauko4651
@charlesmasauko4651 Месяц назад
Wosokoneza uyu
@macdonaldchaonekera834
@macdonaldchaonekera834 Месяц назад
Kodi akupanga sewero la tikuferanji et?
@frankwilliam9844
@frankwilliam9844 Месяц назад
There's contradictory in his mind,chomwe amalawi akufuna singongole,tsitsani zinthu,chepetsani kudalira ngongole za IMF...koma ndithu 60yrs independent Malawi yukanikabe kudalira payokha pa nkhani ya zachuma? so sad...Kodi maiko amzathuwa amatani Kodi ..adatukuka bwanji atalandila ufulu???
@NELSONMULIMAH-fv6ub
@NELSONMULIMAH-fv6ub Месяц назад
Zauchisilu zaziii
@user-lu8px7td6p
@user-lu8px7td6p Месяц назад
Aaaaaaaaaaaaaaaaaaa chitsiru mbuzi garu nyani mfiti iwe
@jeymulima9664
@jeymulima9664 Месяц назад
Zaziiiiii
@user-kg5lf6bd1g
@user-kg5lf6bd1g Месяц назад
Anthu 4 okha bs
@florenceharawa519
@florenceharawa519 Месяц назад
Uku wapita uku wapita punsi anagwa chada😂😂😂😂
@user-rs7vx6hc1k
@user-rs7vx6hc1k Месяц назад
Koma zimenezi zitithandiza izi????
@user-ep7gu2td6y
@user-ep7gu2td6y Месяц назад
Sakudziwa zomwe a makawi akukumana nazo ....,
@MuhammadNyambalo
@MuhammadNyambalo Месяц назад
😅😮😢😅😅😅😅😂 patumbo pako iwe nyo
@NathanMaunda-dz8gc
@NathanMaunda-dz8gc Месяц назад
Awa sakuyankhula zotigwira mtima kodi nd wa chipani chanji ameneyi
@LottiAffati
@LottiAffati Месяц назад
kod akuyankhula kut chan apa guys aaaaaa, komanso amalawi ngoputsadi ndithu
@MarthaChintolo
@MarthaChintolo Месяц назад
Aaaaaa chifukwa chani Chilima unalakwitsa ee
@AbdullCassim
@AbdullCassim Месяц назад
Iweso ndiye kayatu
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r Месяц назад
Ayakhura ali pat?
@chikondiyovita7210
@chikondiyovita7210 Месяц назад
My data hu!
@Vascomw
@Vascomw Месяц назад
Ïn̈ë n̈d̈ïm̈än̈g̈än̈ïz̈ä k̈üẗ äÿäk̈ḧür̈ä z̈äz̈ël̈üüü k̈m̈ ääää b̈ün̈d̈l̈ë ÿän̈g̈ä amayo
@momuumro
@momuumro Месяц назад
Situfuna kunva zimenezo Ife tufuna nkhani yotuluka mu tonse alliance
@charlesmasauko4651
@charlesmasauko4651 Месяц назад
Akufuna kugulitsa UTM KU MCP
@user-lu6nq9bs6w
@user-lu6nq9bs6w Месяц назад
Nde ku MCP' ko akuti chani kkkk 😂😂😂
@elizabethnkhata3438
@elizabethnkhata3438 Месяц назад
It's lik people are not happy
@MaryTchapo-py4hh
@MaryTchapo-py4hh Месяц назад
Ndimwana uyu alibe fundo
@QuotienieMw
@QuotienieMw Месяц назад
Tikufilanji episode 10
@user-ou4md5ud1u
@user-ou4md5ud1u Месяц назад
Sizikuveka ai komas sizikugwilizana ayi
@MaryTchapo-py4hh
@MaryTchapo-py4hh Месяц назад
Kupusa
@SifatiMoses
@SifatiMoses Месяц назад
Palibe kunyengelerana ndi ngongore nbuzi za anthu.
@ElizabethMwakamogho-x7j
@ElizabethMwakamogho-x7j Месяц назад
Sukuziwa make awo find alimbe
@user-zl1xz9kt5s
@user-zl1xz9kt5s Месяц назад
Amalawi mitu sigwiradi sure
@Vascomw
@Vascomw Месяц назад
Hhhhhhh
@user-lu8px7td6p
@user-lu8px7td6p Месяц назад
Palibe chanzeru waywnkhula
@FysonKaliba
@FysonKaliba Месяц назад
Kod ati Ali Mbali iti??????????
@SmithLikoswe
@SmithLikoswe Месяц назад
Zamasewelo bac
@jeymulima9664
@jeymulima9664 Месяц назад
Kkkkk ngabule moyo,thetsa,uthetsa suthetsa kkk yathayi kkk
@WindowSomanje
@WindowSomanje Месяц назад
Za ziii
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Месяц назад
Km malawi ndfe anthu opusa kwambiri tinakali kuvutika
@smartchitimbe2450
@smartchitimbe2450 Месяц назад
Za ziii tu
@MECChiona
@MECChiona Месяц назад
wamisara uyu 😂😂
@NATASHAChimtolo
@NATASHAChimtolo Месяц назад
Opepela uyu malemu amavala makaka achipani chake
@RighteousMhone
@RighteousMhone Месяц назад
Shimeyi atukwane😂😂😂
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j Месяц назад
Emeneyi si dyera koma
@ChrisNkhoma-i8m
@ChrisNkhoma-i8m Месяц назад
Mcp BOMA labwino kwamunthu woganiza mwazelu tiwone komwe tachoka .
@user-px6kt8rx2p
@user-px6kt8rx2p Месяц назад
Yes
@user-uq4hn4rp2j
@user-uq4hn4rp2j Месяц назад
Nice
@thokofodya1583
@thokofodya1583 Месяц назад
😢
@user-hl3vl9nt1b
@user-hl3vl9nt1b Месяц назад
Aaaa zazi bas
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko Месяц назад
Sanje bac amalawi eeee
@FlorenceKamtema-kw5ru
@FlorenceKamtema-kw5ru Месяц назад
Jealousy siumuna
@sonkieleymanni6312
@sonkieleymanni6312 Месяц назад
ndiopusatu awawa,,,,,,,,,,,,,,,palibepo chanzeru anena apa
@LukeKalima
@LukeKalima Месяц назад
😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu
@LukeKalima
@LukeKalima Месяц назад
😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu
@SiphiweTonnyChidumayo
@SiphiweTonnyChidumayo Месяц назад
Anthu sakusangalaratu😂😂
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 Месяц назад
Ndizawo zimenezo komanso musawapangire Zochita anthuwo . ngati inuyo simukusangalala basi
@SiphiweTonnyChidumayo
@SiphiweTonnyChidumayo Месяц назад
@@ancientnkhata1137 eh eh iwe im commenting according ndimmene zuonekera nsiye ine
Далее
Oh No! My Doll Fell In The Dirt🤧💩
00:17
Просмотров 2 млн
CRUISE 5 with Deborah Mbale MAI MBAMBANDE
57:16
Просмотров 34 тыс.