Тёмный

A DPP Ku Parliament Mupite Okonzeka - Bon Kalindo 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 24 тыс.
Просмотров 16 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo continues warning the Democratic Progressive Party (DPP) ahead of Parliament meeting this week in Lilongwe.
Ku Nyasa Voicebox, Bon Kalindo apitiliza kuchenjeza chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) pamene Nyumba ya Malamulo ikukumana sabata ino ku Lilongwe.
#malawi

Опубликовано:

 

10 фев 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 52   
@ChikumbutsoJohn-rs4tt
@ChikumbutsoJohn-rs4tt 5 месяцев назад
This is reality the first thing is leader of opposition do not allow parliament to Biggin without the leader of opposition if it is so postpone the meeting of parliament until the leader have elected the second thing, make sure the DPP party have a diolegue between them to hit the nail on there head because you're the eyes of Malawian may good God be with you and protect you during the meetings thank you
@JosephMwenyali
@JosephMwenyali 5 месяцев назад
Dpp,mps u need to stand strong
@user-qm1qb2jp4s
@user-qm1qb2jp4s 5 месяцев назад
Dccccccc 🔥 nankhumwa ndi chakwera watikwana ambuye tichotseleni
@oliviamphande1900
@oliviamphande1900 5 месяцев назад
The only one freedom fighter Mr bon kalindo
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 5 месяцев назад
Rest in peace Kondwani Nankhumwa
@user-hw9gg9nd9u
@user-hw9gg9nd9u 5 месяцев назад
Ndizoona aphuzitsi asavomele kumasonkha ndalama
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d 5 месяцев назад
I totally agree with Bon Kalindo's advice.please DPP, do not accept Nankhumwa, to lead delegation in the house otherwise adjourn the house and get injunction.we want better Malawi
@user-dk6yc8pl2m
@user-dk6yc8pl2m 5 месяцев назад
❤❤❤ the DC
@clintonnyirongo438
@clintonnyirongo438 5 месяцев назад
Zaziii munthu aziyakhula mawu akuti ndine wowopsya wokhwima kkkkk
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 5 месяцев назад
Akalindo ndalama zikupwetekesani nthawi zina mulungu azakwiya nanu chifukwa anthu amene mkuwanyozawo alibe nanu chifukwa
@user-gx5ht9gm3z
@user-gx5ht9gm3z 5 месяцев назад
Ngiwe galu kwambil nyamak
@user-sr2gq3rb9b
@user-sr2gq3rb9b 5 месяцев назад
Mboleyake
@FelixBMcdonard
@FelixBMcdonard 5 месяцев назад
Koma ngati a DPP mungokhara chete dzikoli lithapo Mr chihana mulikuti
@hendrymasina4014
@hendrymasina4014 5 месяцев назад
Bon kalindo akunena zoona DPP, UDF,and AFORD segulani maso ndimbava zakuzungulilanizo segulani maso chifukwa zomwe akunenazo akalindo ndizoona ndinayamba kumusatila kale zose zimene amaya nkhula akalindo zimankhala zoti akuziwa zimene akunena zosezi zikuchitikazi anaziyankhula kale kale komano poti timamusatila bwino sizimatizizimusa kwambiri a DPP segulani maso
@user-qd2uy9fp9v
@user-qd2uy9fp9v 5 месяцев назад
Kalindo wumakwana ndipo chipani zotsusa ukuziwiza zoona zokhazokha
@user-od8gi6mj1d
@user-od8gi6mj1d 5 месяцев назад
Ndizoona akunena the DC able a DPP akugonana analanditsa Boma 2019 panopa Adina arhetse chipanichi
@user-fp5qn5ci2v
@user-fp5qn5ci2v 5 месяцев назад
Iwe bon kalindo usamayankhule mau ochita frustrate anthu ndi maganizo ako opusawo wamva nkhani zotembelera DPP timadana nazo kaya amachita kukutuma izo ndi zako
@thomasmalupi6624
@thomasmalupi6624 5 месяцев назад
Bon Kalindo only the last standing man in Malawi. Mwana wa kwathu ku Mulanje kwa T/A Mabuka
@user-bq5ev7de1l
@user-bq5ev7de1l 5 месяцев назад
Apm my vote ✊
@user-vc4kz3yk8p
@user-vc4kz3yk8p 5 месяцев назад
Zoonaditu koma ofunika akonzekere bwino zochita a dpp
@user-mg1gu3ec6n
@user-mg1gu3ec6n 5 месяцев назад
Akunena zoona palibe chimene akulakwa akalindo mcp Akuma khalila Kuna miza anthu bas achoke Siti kuwa funaso feteleza panopa tikuma Gula 85000 thawi ya Peter tima Gula 22 ,500 chakwela asiye udindo
@user-ko1lk3br4r
@user-ko1lk3br4r 5 месяцев назад
imilani DPP KT zikhozeke coz khoti simuiopa mkulu
@mcdonaldchirwa3182
@mcdonaldchirwa3182 5 месяцев назад
Keep on fighting Malawian Mr Bon Fighter Kalindooooo
@JumaAlli-vf6jp
@JumaAlli-vf6jp 5 месяцев назад
Kalindo akunena dzoona ndithu a d.p.p. asamale ndikuchenjera komwe
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v 5 месяцев назад
Komano amavera DPP
@mchipengule
@mchipengule 5 месяцев назад
DPP mwayithetsa nokha, nanga kumangouyambana? MCP 2025 Woyeee!! Mwachitaya basi kutukwana chonchi? Mulungu sakudalitsani inu!!!
@user-hd7wq2yc6m
@user-hd7wq2yc6m 5 месяцев назад
ADPP choyamba musanayambe zokamborana zanu munyumba ya malamulo muyambe kaye mwakhala pansi mu nyumba yanuyo ya DPP kuuzana kapena kukambirana zokachita ku parliament ko leader of opposition first budget second ndizimene anthu amene tilikumodzi kuno tizizamva chifukwa ndipamene tizawonere kiti ndinudi opposition ya mphamvu asakutoleni a mca ndi yonse allaoance yawo yo iyayi.chonde chondr chonde ndipamene tizakikhulupitilani amayi Navitcha mukawonese uzimayi wanu ndipamenepa chonde kuno ku Muzi chikhulupiliro chathu chili mwa inu a DPP
@mchipengule
@mchipengule 5 месяцев назад
Zaziiii, moti anthu apange adjourn Pariament chifukwa cha uve wanu? Pariament ndi ya anthu.
@ConfusedAtv-bs4gc
@ConfusedAtv-bs4gc 5 месяцев назад
Kodi Mesa Ben longwe Ali kumalawi tatifunsilekoni Kuti zokoka zamayi yolamu zija amazinena zija wayamba kuzikoka pano chifukwa alinazo pafupi muja anali kutali
@chisomochavula
@chisomochavula 5 месяцев назад
Koma avunva a DPP wo? Ifetu tikuyembekeza iwowo apulumutse amalawi
@abdul-rasheedsalika
@abdul-rasheedsalika 5 месяцев назад
Zikt Bwanji kd pamenepo????
@wellingtonmtoso2074
@wellingtonmtoso2074 5 месяцев назад
Za parliament zithela ku parliament. Za chipani zithela ku chipani.Otuminidwa amathela kwa omutuma.
@user-xn2dt2eu8x
@user-xn2dt2eu8x 5 месяцев назад
anthu opusa m'maganizidwe inu
@ChristopherKabanga
@ChristopherKabanga 5 месяцев назад
ukumva kuwawa sunati kalindo ukumva peni wen weni
@tafawakawonga6275
@tafawakawonga6275 5 месяцев назад
Kkkkkk kuganiza ngati nkhuku
@user-od8gi6mj1d
@user-od8gi6mj1d 5 месяцев назад
Rubish people s are supporting MCP anthu adyera
@muhammadjuma3317
@muhammadjuma3317 5 месяцев назад
Ukhaula iwe udzakhala kunja kwa boma mpakana kale kale . President wa amphawi alipo kale ndi mkasa. Adzako adakutuluka kale chifukwa chakuti ndalama umangodya wekha
@user-xn2dt2eu8x
@user-xn2dt2eu8x 5 месяцев назад
akulu mukulankhula palibe chipani cha MCP zikupanga iwo zikukutsangalani anthu opusa amene mukuyikira kumbuyo MCP the DC ndi omenyera ufulu ku mtunda wa amalawi osauka
@ChristopherKabanga
@ChristopherKabanga 5 месяцев назад
paja adayambira kugura lweyotu usaiware
@jomochirwa
@jomochirwa 5 месяцев назад
Katundu kapena zinthu zakwela mtengo kumayiko onse makamakaso mayiko amene ali ndi chuma.chitsanzo kuno ku southafrica katundu akudula zeedi koma chikhalile katunduyo akupangidwila kuno.ku mozambique anthu wogwila ntchito za boma maka police ,asilikali pano 4 month no salaries.kukwela ntengo sikumalawi kokha ayi.koma mtsogoleli wathu akayesa kupeza njila zabwino zochepetsela mavuto komanso katangale.anthu sitingavomeleze zakudula kwa zinthu pamene atsogoleli anthu akungokhalila kuba komanso ma alawasi akulandila ,masalale awo sadadulidwe.
@user-hu5su2ys7k
@user-hu5su2ys7k 5 месяцев назад
Kalindo mbuli
@user-xn2dt2eu8x
@user-xn2dt2eu8x 5 месяцев назад
achisilu inu oganiza mopusa inu
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 5 месяцев назад
Kusakuyankhani pazimene mkuyankhula sikut ndiwopusa ayi koma anawona uchisilu wanuwo ugalu
@user-qv4ko6ps4j
@user-qv4ko6ps4j 5 месяцев назад
Ugalu opose wakowo mwana hule iwe.mwana oleledwa ndi agogo mai ako ali ku bar,chitsilu, mbuzi ya munthu ngati mkotero bwanji ukawafunse agogo akowo kut kodi dziko likuyenda bwanji,,,,,,, umve iwo mkutheka za bon kalindo siukumva ndipo ngati ndi chamba or tindalama tonyenyekato ta MCP m'phwanga tikupweteketsa ukalimbana ndi bon kalindo ulidziwano dziko ndipo choti udziwe ma bwana ako a MCP onse ndi ana kwa kalindo, iwe mantha ai ,monse adayambila kulimbana ndi boma muja akutaninae? Wamba wamba bwenzi ataphedwa kale koma uwu ndi mtunda,,,,,, dikila akayamba misonkhano tiwagenda mapwala awo!
@user-gx5ht9gm3z
@user-gx5ht9gm3z 5 месяцев назад
Sugayakhe coz ndiwe mwana wangon buzi sml boy 😊
@user-qv4ko6ps4j
@user-qv4ko6ps4j 5 месяцев назад
Cjay lucky,,,,,,, chitsilu cha MCP ndipo nonse munya 2025
@user-mx3rw2dt4z
@user-mx3rw2dt4z 5 месяцев назад
Ndimwana oti anaphulika chishango patumbo pa make akanyoze the DC wachilungamo
@user-qv4ko6ps4j
@user-qv4ko6ps4j 5 месяцев назад
The DC machine original than all
@henryhenry6632
@henryhenry6632 5 месяцев назад
Nonsense dzimaphwala dzanu alomwe
@user-nw6ie3xx8b
@user-nw6ie3xx8b 5 месяцев назад
This man is hopeless, and u can see from far this man is hungry now he has joined dpp
@user-gx5ht9gm3z
@user-gx5ht9gm3z 5 месяцев назад
Ndiwe sml boy ndiye chifukwa ukunganizil zolakwa
Далее
We Are In The Age of Politics of Ideas - Kamlepo Kalua
38:12
MFUMUKAZI COMEDY  SERIES 21/12/2022
27:04
Просмотров 127 тыс.
Ku MCP Kuli Nkhanza - Samuel Lwara
25:39
Просмотров 10 тыс.