Mr president anthu awuphawi palibwino ayimile u president waziko pasogolopa tizawona kusitha ulemu Mr president born kalindo chonena chimandisow mulungu azikudalisani thawi zose
Koma kodi kodi chakwera ndi munthu kapena chiwanda Malawians gather here to help me...akuoneka kut satana uja Mulungu anamusiya kut malawi...apa Mulungu watiyesa mayeso ....zoona maiko onsewa ,satana akagwere kwathu kuno..Allah transfer this devil please...throw it in a country which does not prays You...as for malawians..we pray
Ngati kuli munthu upusa chisilu chindere chizereza ndimunthu amene akudya zaulele koma akuzuza amamene amamudyesa chaulerezo. Nyumba galimoto petrol magesi school fees ya ana zose zaulele koma anthu amene apakupasa zimenezo mdikuwatenga ngati zisilu atsogoleri atundu anji mra mukuputa chiteze dala chizakuyabwani ndi boma lanulo
NDIPO sinaone duna za bomadi zikulipira misokho olo amalowetsa zithu ulele ndipo Mr DC mau Anu ndi moto km amalawi akupusa masiku ano bwanji apa boma likuonjezatu
Kwacha yagwa kangati? Katundu tikugura pa rate yopoira ,win palibepo timapanga business kungoti nanga titani poti ntchito zikusowa.tiganizireni a business 😢chonde.